Psalms 103 (BOGWICC)
undefined Salimo la Davide. 1 Tamanda Yehova, iwe moyo wanga;ndi zonse zamʼkati mwanga zitamande dzina lake loyera. 2 Tamanda Yehova, iwe moyo wanga,ndipo usayiwale zabwino zake zonse. 3 Amene amakhululuka machimo ako onsendi kuchiritsa nthenda zako zonse, 4 amene awombola moyo wako ku dzenjendi kukuveka chikondi ndi chifundo chake ngati chipewa chaufumu, 5 amene akwaniritsa zokhumba zako ndi zinthu zabwino,kotero kuti umakhala wamphamvu zatsopano ngati mphungu. 6 Yehova amachita chilungamondipo amaweruza molungama onse opsinjika. 7 Iye anadziwitsa Mose njira zake,ntchito zake kwa Aisraeli. 8 Yehova ndi wachifundo ndi wokoma mtima,wosakwiya msanga ndi wachikondi chochuluka. 9 Iye sadzatsutsa nthawi zonse,kapena kusunga mkwiyo wake kwamuyaya; 10 satichitira molingana ndi machimo athu,kapena kutibwezera molingana ndi mphulupulu zathu. 11 Pakuti monga kumwamba kuli kutali ndi dziko lapansi,koteronso chikondi chake nʼchachikulu kwa iwo amene amamuopa; 12 monga kummawa kutalikirana ndi kumadzulo,koteronso Iye watichotsera mphulupulu zathu kuti zikhale kutali nafe. 13 Monga bambo amachitira chifundo ana ake,choncho Yehova ali ndi chifundo ndi iwo amene amamuopa; 14 pakuti Iye amadziwa momwe tinawumbidwira,amakumbukira kuti ndife fumbi. 15 Kunena za munthu, masiku ake ali ngati udzu,amaphuka ngati duwa la mʼmunda; 16 koma mphepo imawombapo ndipo silionekansondipo malo ake sakumbukirikanso. 17 Koma kuchokera muyaya mpaka muyayachikondi cha Yehova chili ndi iwo amene amamuopa,ndi chilungamo chake chili ndi ana a ana awo; 18 iwo amene amasunga pangano lakendi kukumbukira kumvera malangizo ake. 19 Yehova wakhazikitsa mpando wake waufumu mmwambandipo ufumu wake umalamulira onse. 20 Tamandani Yehova, inu angelo ake,amphamvu inu amene mumachita zimene amalamula,amene mumamvera mawu ake. 21 Tamandani Yehova, zolengedwa zonse zakumwamba,inu atumiki ake amene mumachita chifuniro chake. 22 Tamandani Yehova, ntchito yake yonsekulikonse mu ulamuliro wake. Tamanda Yehova, iwe moyo wanga.
In Other Versions
Psalms 103 in the ANGEFD
Psalms 103 in the ANTPNG2D
Psalms 103 in the AS21
Psalms 103 in the BAGH
Psalms 103 in the BBPNG
Psalms 103 in the BBT1E
Psalms 103 in the BDS
Psalms 103 in the BEV
Psalms 103 in the BHAD
Psalms 103 in the BIB
Psalms 103 in the BLPT
Psalms 103 in the BNT
Psalms 103 in the BNTABOOT
Psalms 103 in the BNTLV
Psalms 103 in the BOATCB
Psalms 103 in the BOATCB2
Psalms 103 in the BOBCV
Psalms 103 in the BOCNT
Psalms 103 in the BOECS
Psalms 103 in the BOHCB
Psalms 103 in the BOHCV
Psalms 103 in the BOHLNT
Psalms 103 in the BOHNTLTAL
Psalms 103 in the BOICB
Psalms 103 in the BOILNTAP
Psalms 103 in the BOITCV
Psalms 103 in the BOKCV
Psalms 103 in the BOKCV2
Psalms 103 in the BOKHWOG
Psalms 103 in the BOKSSV
Psalms 103 in the BOLCB
Psalms 103 in the BOLCB2
Psalms 103 in the BOMCV
Psalms 103 in the BONAV
Psalms 103 in the BONCB
Psalms 103 in the BONLT
Psalms 103 in the BONUT2
Psalms 103 in the BOPLNT
Psalms 103 in the BOSCB
Psalms 103 in the BOSNC
Psalms 103 in the BOTLNT
Psalms 103 in the BOVCB
Psalms 103 in the BOYCB
Psalms 103 in the BPBB
Psalms 103 in the BPH
Psalms 103 in the BSB
Psalms 103 in the CCB
Psalms 103 in the CUV
Psalms 103 in the CUVS
Psalms 103 in the DBT
Psalms 103 in the DGDNT
Psalms 103 in the DHNT
Psalms 103 in the DNT
Psalms 103 in the ELBE
Psalms 103 in the EMTV
Psalms 103 in the ESV
Psalms 103 in the FBV
Psalms 103 in the FEB
Psalms 103 in the GGMNT
Psalms 103 in the GNT
Psalms 103 in the HARY
Psalms 103 in the HNT
Psalms 103 in the IRVA
Psalms 103 in the IRVB
Psalms 103 in the IRVG
Psalms 103 in the IRVH
Psalms 103 in the IRVK
Psalms 103 in the IRVM
Psalms 103 in the IRVM2
Psalms 103 in the IRVO
Psalms 103 in the IRVP
Psalms 103 in the IRVT
Psalms 103 in the IRVT2
Psalms 103 in the IRVU
Psalms 103 in the ISVN
Psalms 103 in the JSNT
Psalms 103 in the KAPI
Psalms 103 in the KBT1ETNIK
Psalms 103 in the KBV
Psalms 103 in the KJV
Psalms 103 in the KNFD
Psalms 103 in the LBA
Psalms 103 in the LBLA
Psalms 103 in the LNT
Psalms 103 in the LSV
Psalms 103 in the MAAL
Psalms 103 in the MBV
Psalms 103 in the MBV2
Psalms 103 in the MHNT
Psalms 103 in the MKNFD
Psalms 103 in the MNG
Psalms 103 in the MNT
Psalms 103 in the MNT2
Psalms 103 in the MRS1T
Psalms 103 in the NAA
Psalms 103 in the NASB
Psalms 103 in the NBLA
Psalms 103 in the NBS
Psalms 103 in the NBVTP
Psalms 103 in the NET2
Psalms 103 in the NIV11
Psalms 103 in the NNT
Psalms 103 in the NNT2
Psalms 103 in the NNT3
Psalms 103 in the PDDPT
Psalms 103 in the PFNT
Psalms 103 in the RMNT
Psalms 103 in the SBIAS
Psalms 103 in the SBIBS
Psalms 103 in the SBIBS2
Psalms 103 in the SBICS
Psalms 103 in the SBIDS
Psalms 103 in the SBIGS
Psalms 103 in the SBIHS
Psalms 103 in the SBIIS
Psalms 103 in the SBIIS2
Psalms 103 in the SBIIS3
Psalms 103 in the SBIKS
Psalms 103 in the SBIKS2
Psalms 103 in the SBIMS
Psalms 103 in the SBIOS
Psalms 103 in the SBIPS
Psalms 103 in the SBISS
Psalms 103 in the SBITS
Psalms 103 in the SBITS2
Psalms 103 in the SBITS3
Psalms 103 in the SBITS4
Psalms 103 in the SBIUS
Psalms 103 in the SBIVS
Psalms 103 in the SBT
Psalms 103 in the SBT1E
Psalms 103 in the SCHL
Psalms 103 in the SNT
Psalms 103 in the SUSU
Psalms 103 in the SUSU2
Psalms 103 in the SYNO
Psalms 103 in the TBIAOTANT
Psalms 103 in the TBT1E
Psalms 103 in the TBT1E2
Psalms 103 in the TFTIP
Psalms 103 in the TFTU
Psalms 103 in the TGNTATF3T
Psalms 103 in the THAI
Psalms 103 in the TNFD
Psalms 103 in the TNT
Psalms 103 in the TNTIK
Psalms 103 in the TNTIL
Psalms 103 in the TNTIN
Psalms 103 in the TNTIP
Psalms 103 in the TNTIZ
Psalms 103 in the TOMA
Psalms 103 in the TTENT
Psalms 103 in the UBG
Psalms 103 in the UGV
Psalms 103 in the UGV2
Psalms 103 in the UGV3
Psalms 103 in the VBL
Psalms 103 in the VDCC
Psalms 103 in the YALU
Psalms 103 in the YAPE
Psalms 103 in the YBVTP
Psalms 103 in the ZBP