Psalms 72 (BOGWICC)

undefined Salimo la Solomoni. 1 Patsani mwana wa mfumu nzeru zanu zoweruzira mwa chilungamo,Inu Mulungu mupatseni mwana wa mfumu chilungamo chanu. 2 Iye adzaweruza anthu anu mwachilungamo,anthu anu ozunzika mosakondera. 3 Mapiri adzabweretsa chuma kwa anthu anu,timapiri tidzabweretsa zipatso zachilungamo. 4 Iye adzateteza ozunzika pakati pa anthundi kupulumutsa ana a anthu osowa;adzaphwanya ozunza anzawo. 5 Adzakhala ndi moyo pa mibado yonse,nthawi zonse pamene dzuwa ndi mwezi zikuwala. 6 Iye adzakhala kugwa kwa mvula pa minda yolimidwangati mivumbi yothirira dziko lapansi. 7 Mʼmasiku a munthu wolungama adzakhazikika;chuma chidzachuluka mpaka mwezi utaleka kuwala. 8 Iye adzalamulira kuchokera ku nyanja ina mpaka ku nyanja inandiponso kuchokera ku mtsinje mpaka ku malekezero a dziko lapansi. 9 Mafuko a mʼchipululu adzawerama pamaso pakendipo adani ake adzanyambita fumbi. 10 Mafumu a ku Tarisisi ndi a ku zilumba zakutaliadzabweretsa mitulo kwa iye,mafumu a ku Seba ndi Sebaadzapereka mphatso kwa iyeyo. 11 Mafumu onse adzamuweramirandipo mitundu yonse idzamutumikira. 12 Pakuti iye adzawombola wosowa amene akulira,wozunzika amene alibe wina womuthandiza. 13 Iye adzachitira chifundo anthu ofowoka ndi anthu osowandi kupulumutsa osowa ku imfa. 14 Iye adzalanditsa iwo ku mazunzo ndi chiwawapakuti magazi awo ndi amtengo wapatali pamaso pake. 15 Iye akhale ndi moyo wautali;golide ochokera ku Seba apatsidwe kwa iye.Anthu amupempherere nthawi zonsendi kumudalitsa tsiku lonse. 16 Mulole kuti tirigu achuluke mʼdziko lonse;pamwamba pa mapiri pakhale tirigu.Zipatso zake zichuluke ngati za ku Lebanoni;zichuluke ngati udzu wakuthengo 17 Dzina lake likhazikike kwamuyaya,lipitirire kukhala monga momwe limakhalira dzuwa. Mitundu yonse idzadalitsika kudzera mwa iyendipo iwo adzamutcha iye wodala. 18 Matamando akhale kwa Yehova Mulungu, Mulungu wa Israeliamene Iye yekha amachita ntchito zodabwitsa. 19 Matamando akhale ku dzina lake laulemerero kwamuyayadziko lonse lapansi lidzaze ndi ulemerero wake.Ameni ndi Ameni. 20 Uku ndiko kumaliza kwa mapemphero a Davide mwana wa Yese.

In Other Versions

Psalms 72 in the ANGEFD

Psalms 72 in the ANTPNG2D

Psalms 72 in the AS21

Psalms 72 in the BAGH

Psalms 72 in the BBPNG

Psalms 72 in the BBT1E

Psalms 72 in the BDS

Psalms 72 in the BEV

Psalms 72 in the BHAD

Psalms 72 in the BIB

Psalms 72 in the BLPT

Psalms 72 in the BNT

Psalms 72 in the BNTABOOT

Psalms 72 in the BNTLV

Psalms 72 in the BOATCB

Psalms 72 in the BOATCB2

Psalms 72 in the BOBCV

Psalms 72 in the BOCNT

Psalms 72 in the BOECS

Psalms 72 in the BOHCB

Psalms 72 in the BOHCV

Psalms 72 in the BOHLNT

Psalms 72 in the BOHNTLTAL

Psalms 72 in the BOICB

Psalms 72 in the BOILNTAP

Psalms 72 in the BOITCV

Psalms 72 in the BOKCV

Psalms 72 in the BOKCV2

Psalms 72 in the BOKHWOG

Psalms 72 in the BOKSSV

Psalms 72 in the BOLCB

Psalms 72 in the BOLCB2

Psalms 72 in the BOMCV

Psalms 72 in the BONAV

Psalms 72 in the BONCB

Psalms 72 in the BONLT

Psalms 72 in the BONUT2

Psalms 72 in the BOPLNT

Psalms 72 in the BOSCB

Psalms 72 in the BOSNC

Psalms 72 in the BOTLNT

Psalms 72 in the BOVCB

Psalms 72 in the BOYCB

Psalms 72 in the BPBB

Psalms 72 in the BPH

Psalms 72 in the BSB

Psalms 72 in the CCB

Psalms 72 in the CUV

Psalms 72 in the CUVS

Psalms 72 in the DBT

Psalms 72 in the DGDNT

Psalms 72 in the DHNT

Psalms 72 in the DNT

Psalms 72 in the ELBE

Psalms 72 in the EMTV

Psalms 72 in the ESV

Psalms 72 in the FBV

Psalms 72 in the FEB

Psalms 72 in the GGMNT

Psalms 72 in the GNT

Psalms 72 in the HARY

Psalms 72 in the HNT

Psalms 72 in the IRVA

Psalms 72 in the IRVB

Psalms 72 in the IRVG

Psalms 72 in the IRVH

Psalms 72 in the IRVK

Psalms 72 in the IRVM

Psalms 72 in the IRVM2

Psalms 72 in the IRVO

Psalms 72 in the IRVP

Psalms 72 in the IRVT

Psalms 72 in the IRVT2

Psalms 72 in the IRVU

Psalms 72 in the ISVN

Psalms 72 in the JSNT

Psalms 72 in the KAPI

Psalms 72 in the KBT1ETNIK

Psalms 72 in the KBV

Psalms 72 in the KJV

Psalms 72 in the KNFD

Psalms 72 in the LBA

Psalms 72 in the LBLA

Psalms 72 in the LNT

Psalms 72 in the LSV

Psalms 72 in the MAAL

Psalms 72 in the MBV

Psalms 72 in the MBV2

Psalms 72 in the MHNT

Psalms 72 in the MKNFD

Psalms 72 in the MNG

Psalms 72 in the MNT

Psalms 72 in the MNT2

Psalms 72 in the MRS1T

Psalms 72 in the NAA

Psalms 72 in the NASB

Psalms 72 in the NBLA

Psalms 72 in the NBS

Psalms 72 in the NBVTP

Psalms 72 in the NET2

Psalms 72 in the NIV11

Psalms 72 in the NNT

Psalms 72 in the NNT2

Psalms 72 in the NNT3

Psalms 72 in the PDDPT

Psalms 72 in the PFNT

Psalms 72 in the RMNT

Psalms 72 in the SBIAS

Psalms 72 in the SBIBS

Psalms 72 in the SBIBS2

Psalms 72 in the SBICS

Psalms 72 in the SBIDS

Psalms 72 in the SBIGS

Psalms 72 in the SBIHS

Psalms 72 in the SBIIS

Psalms 72 in the SBIIS2

Psalms 72 in the SBIIS3

Psalms 72 in the SBIKS

Psalms 72 in the SBIKS2

Psalms 72 in the SBIMS

Psalms 72 in the SBIOS

Psalms 72 in the SBIPS

Psalms 72 in the SBISS

Psalms 72 in the SBITS

Psalms 72 in the SBITS2

Psalms 72 in the SBITS3

Psalms 72 in the SBITS4

Psalms 72 in the SBIUS

Psalms 72 in the SBIVS

Psalms 72 in the SBT

Psalms 72 in the SBT1E

Psalms 72 in the SCHL

Psalms 72 in the SNT

Psalms 72 in the SUSU

Psalms 72 in the SUSU2

Psalms 72 in the SYNO

Psalms 72 in the TBIAOTANT

Psalms 72 in the TBT1E

Psalms 72 in the TBT1E2

Psalms 72 in the TFTIP

Psalms 72 in the TFTU

Psalms 72 in the TGNTATF3T

Psalms 72 in the THAI

Psalms 72 in the TNFD

Psalms 72 in the TNT

Psalms 72 in the TNTIK

Psalms 72 in the TNTIL

Psalms 72 in the TNTIN

Psalms 72 in the TNTIP

Psalms 72 in the TNTIZ

Psalms 72 in the TOMA

Psalms 72 in the TTENT

Psalms 72 in the UBG

Psalms 72 in the UGV

Psalms 72 in the UGV2

Psalms 72 in the UGV3

Psalms 72 in the VBL

Psalms 72 in the VDCC

Psalms 72 in the YALU

Psalms 72 in the YAPE

Psalms 72 in the YBVTP

Psalms 72 in the ZBP