Psalms 51 (BOGWICC)

undefined Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Pamene Mneneri Natani anabwera kwa iye atachita chigololo ndi Batiseba. 1 Mundichitire chifundo, Inu Mulungu,molingana ndi chikondi chanu chosasinthika;molingana ndi chifundo chanu chachikulumufafanize mphulupulu zanga. 2 Munditsuke zolakwa zanga zonsendipo mundiyeretse kuchotsa tchimo langa. 3 Pakuti ndikudziwa mphulupulu zanga,ndipo tchimo langa lili pamaso panga nthawi zonse. 4 Motsutsana ndi Inu, Inu nokha, ndachimwandipo ndachita zoyipa pamaso panu,Kotero kuti inu mwapezeka kuti ndinu wolungamapamene muyankhula ndi pamene muweruza. 5 Zoonadi ine ndinali wochimwa pomwe ndimabadwa,wochimwa kuyambira pa nthawi imene amayi anga anakhala woyembekezera ine. 6 Zoonadi inu mumafuna choonadi mu ziwalo zamʼkati mwanga;mumandiphunzitsa nzeru mʼkati mwanga mwenimweni. 7 Mundiyeretse ndi hisope ndipo ndidzayera,munditsuke ndipo ndidzayera kuposa matalala 8 Mundilole ndimve chimwemwe ndi chisangalalo,mulole kuti mafupa amene mwawamphwanya akondwere. 9 Mufulatire machimo angandi kufafaniza zolakwa zanga zonse. 10 Mulenge mʼkati mwanga mtima woyera Inu Mulungundi kukonzanso mzimu wokhazikika mwa ine. 11 Musandichotse pamaso panukapena kuchotsa Mzimu wanu Woyera mwa ine. 12 Bwezeretsani mwa ine chimwemwe cha chipulumutso chanundipo mundipatse mzimu wofuna kumvera kuti undilimbitse. 13 Pamenepo ndidzaphunzitsa anthu amphulupulu njira zanukuti ochimwa adzabwerere kwa inu. 14 Mundipulumutse ku tchimo lokhetsa magazi, Inu Mulungu,Mulungu wa chipulumutso changa,ndipo lilime langa lidzayimba zachilungamo chanu. 15 Inu Ambuye tsekulani milomo yanga,ndipo pakamwa panga padzalengeza matamando anu. 16 Inu simusangalatsidwa ndi nsembe wamba.Ndikanapereka nsembe yopsereza, Inu simukondwera nayo. 17 Nsembe za Mulungu ndi mzimu wosweka;mtima wosweka ndi wachisoniInu Mulungu simudzawunyoza. 18 Mwa kukoma mtima kwanu mupange Ziyoni kuti alemere;mumange makoma a Yerusalemu. 19 Kotero kudzakhala nsembe zachilungamo,nsembe yonse yopsereza yokondweretsa Inu;ndipo ngʼombe zazimuna zidzaperekedwa pa guwa lanu la nsembe.

In Other Versions

Psalms 51 in the ANGEFD

Psalms 51 in the ANTPNG2D

Psalms 51 in the AS21

Psalms 51 in the BAGH

Psalms 51 in the BBPNG

Psalms 51 in the BBT1E

Psalms 51 in the BDS

Psalms 51 in the BEV

Psalms 51 in the BHAD

Psalms 51 in the BIB

Psalms 51 in the BLPT

Psalms 51 in the BNT

Psalms 51 in the BNTABOOT

Psalms 51 in the BNTLV

Psalms 51 in the BOATCB

Psalms 51 in the BOATCB2

Psalms 51 in the BOBCV

Psalms 51 in the BOCNT

Psalms 51 in the BOECS

Psalms 51 in the BOHCB

Psalms 51 in the BOHCV

Psalms 51 in the BOHLNT

Psalms 51 in the BOHNTLTAL

Psalms 51 in the BOICB

Psalms 51 in the BOILNTAP

Psalms 51 in the BOITCV

Psalms 51 in the BOKCV

Psalms 51 in the BOKCV2

Psalms 51 in the BOKHWOG

Psalms 51 in the BOKSSV

Psalms 51 in the BOLCB

Psalms 51 in the BOLCB2

Psalms 51 in the BOMCV

Psalms 51 in the BONAV

Psalms 51 in the BONCB

Psalms 51 in the BONLT

Psalms 51 in the BONUT2

Psalms 51 in the BOPLNT

Psalms 51 in the BOSCB

Psalms 51 in the BOSNC

Psalms 51 in the BOTLNT

Psalms 51 in the BOVCB

Psalms 51 in the BOYCB

Psalms 51 in the BPBB

Psalms 51 in the BPH

Psalms 51 in the BSB

Psalms 51 in the CCB

Psalms 51 in the CUV

Psalms 51 in the CUVS

Psalms 51 in the DBT

Psalms 51 in the DGDNT

Psalms 51 in the DHNT

Psalms 51 in the DNT

Psalms 51 in the ELBE

Psalms 51 in the EMTV

Psalms 51 in the ESV

Psalms 51 in the FBV

Psalms 51 in the FEB

Psalms 51 in the GGMNT

Psalms 51 in the GNT

Psalms 51 in the HARY

Psalms 51 in the HNT

Psalms 51 in the IRVA

Psalms 51 in the IRVB

Psalms 51 in the IRVG

Psalms 51 in the IRVH

Psalms 51 in the IRVK

Psalms 51 in the IRVM

Psalms 51 in the IRVM2

Psalms 51 in the IRVO

Psalms 51 in the IRVP

Psalms 51 in the IRVT

Psalms 51 in the IRVT2

Psalms 51 in the IRVU

Psalms 51 in the ISVN

Psalms 51 in the JSNT

Psalms 51 in the KAPI

Psalms 51 in the KBT1ETNIK

Psalms 51 in the KBV

Psalms 51 in the KJV

Psalms 51 in the KNFD

Psalms 51 in the LBA

Psalms 51 in the LBLA

Psalms 51 in the LNT

Psalms 51 in the LSV

Psalms 51 in the MAAL

Psalms 51 in the MBV

Psalms 51 in the MBV2

Psalms 51 in the MHNT

Psalms 51 in the MKNFD

Psalms 51 in the MNG

Psalms 51 in the MNT

Psalms 51 in the MNT2

Psalms 51 in the MRS1T

Psalms 51 in the NAA

Psalms 51 in the NASB

Psalms 51 in the NBLA

Psalms 51 in the NBS

Psalms 51 in the NBVTP

Psalms 51 in the NET2

Psalms 51 in the NIV11

Psalms 51 in the NNT

Psalms 51 in the NNT2

Psalms 51 in the NNT3

Psalms 51 in the PDDPT

Psalms 51 in the PFNT

Psalms 51 in the RMNT

Psalms 51 in the SBIAS

Psalms 51 in the SBIBS

Psalms 51 in the SBIBS2

Psalms 51 in the SBICS

Psalms 51 in the SBIDS

Psalms 51 in the SBIGS

Psalms 51 in the SBIHS

Psalms 51 in the SBIIS

Psalms 51 in the SBIIS2

Psalms 51 in the SBIIS3

Psalms 51 in the SBIKS

Psalms 51 in the SBIKS2

Psalms 51 in the SBIMS

Psalms 51 in the SBIOS

Psalms 51 in the SBIPS

Psalms 51 in the SBISS

Psalms 51 in the SBITS

Psalms 51 in the SBITS2

Psalms 51 in the SBITS3

Psalms 51 in the SBITS4

Psalms 51 in the SBIUS

Psalms 51 in the SBIVS

Psalms 51 in the SBT

Psalms 51 in the SBT1E

Psalms 51 in the SCHL

Psalms 51 in the SNT

Psalms 51 in the SUSU

Psalms 51 in the SUSU2

Psalms 51 in the SYNO

Psalms 51 in the TBIAOTANT

Psalms 51 in the TBT1E

Psalms 51 in the TBT1E2

Psalms 51 in the TFTIP

Psalms 51 in the TFTU

Psalms 51 in the TGNTATF3T

Psalms 51 in the THAI

Psalms 51 in the TNFD

Psalms 51 in the TNT

Psalms 51 in the TNTIK

Psalms 51 in the TNTIL

Psalms 51 in the TNTIN

Psalms 51 in the TNTIP

Psalms 51 in the TNTIZ

Psalms 51 in the TOMA

Psalms 51 in the TTENT

Psalms 51 in the UBG

Psalms 51 in the UGV

Psalms 51 in the UGV2

Psalms 51 in the UGV3

Psalms 51 in the VBL

Psalms 51 in the VDCC

Psalms 51 in the YALU

Psalms 51 in the YAPE

Psalms 51 in the YBVTP

Psalms 51 in the ZBP