Jeremiah 11 (BOGWICC)

1 Yehova anayankhula ndi Yeremiya kuti, 2 “Imvani mawu a pangano ili, ndipo uwawuze anthu a ku Yuda ndi a ku Yerusalemu. 3 Awuze kuti Yehova, Mulungu wa Israeli akuti ‘adzakhala wotembereredwa munthu amene samvera mawu a pangano ili. 4 Awa anali mawu amene ndinalamulira makolo anu nditawatulutsa mu Igupto, kuchoka mʼngʼanjo yamoto.’ Ine ndinati, ‘Mverani Ine ndi kuchita chilichonse chimene ndakulamulirani. Mukatero mudzakhala anthu anga ndi Ine ndidzakhala Mulungu wanu. 5 Tsono Ine ndidzakwaniritsa lumbiro lomwe ndinalumbira kwa makolo anu kuti ndidzawapatsa dziko loyenda mkaka ndi uchi,’ dziko lomwe inu lero mukukhalamo.”Tsono Ine ndinayankha kuti, “Ameni, Yehova.” 6 Yehova anandiwuza kuti, “Lengeza mawu onsewa mʼmizinda yonse ya ku Yuda ndi mʼmisewu ya mu Yerusalemu: ‘Mverani mawu a pangano ili ndi kuzitsatira. 7 Kuyambira nthawi imene ndinatulutsa makolo anu ku Igupto mpaka lero, ndakhala ndi kuwachenjeza kawirikawiri kuti, ‘Mverani Ine.’ 8 Koma sanamvere kapena kulabadirako. Aliyense anawumirira kuchita zoyipa za mʼmitima yawo. Ngakhale ndinawalamulira kuti asunge pangano langa koma iwo sanasunge. Choncho ndinawalanga monga ndinaneneramo.’ ” 9 Kenaka Yehova anandiwuza kuti, “Anthu a ku Yuda ndi ku Yerusalemu andiwukira. 10 Abwereranso ku machimo a makolo awo, amene anakana kumvera mawu anga. Akutsata milungu ina ndi kumayitumikira. Aisraeli ndi Ayuda aphwanya pangano limene ndinachita ndi makolo awo. 11 Choncho Yehova akuti, ‘Ndidzawagwetsera mavuto amene sadzatha kuwalewa. Ngakhale adzandilirire, sindidzawamvera. 12 Anthu a mʼmizinda ya Yuda ndi anthu a ku Yerusalemu adzapita ndi kukalirira milungu imene ankayifukizira lubani, koma milunguyo sidzawathandiza ndi pangʼono pomwe mavuto akadzafika. 13 Iwe Yuda, uli ndi milungu yochuluka ngati chiwerengero cha mizinda yako; chiwerengero cha maguwa ansembe amene umafukizirapo lubani kwa Baala chili ngati misewu ya mu Yerusalemu.’ 14 “Tsono iwe Yeremiya usawapempherere anthu amenewa ngakhale kuwadandaulira kapena kuwapepesera, chifukwa sindidzawamvera akadzandiyitana pa nthawi ya mavuto awo. 15 “Kodi anthu anga okondedwa akudzachita chiyani mʼNyumba yanga?Kodi suja iwowa amachita zoyipa zambiri?Kodi mungathe kupulumuka,tsoka osakugweranichifukwa cha nsembe zanuzo?” 16 Kale Yehova ankakutchani mtengo wa olivi wa masamba obiriwira,wokhala ndi zipatso zokongola.Koma tsopano adzawutenthandi mkuntho wamkokomondipo nthambi zake zidzapserera. 17 Yehova Wamphamvuzonse, amene anakudzalani, walamula kuti mavuto akugwereni. Inu a banja la Yuda ndi a banja la Israeli munachitira Yehova zoyipa ndi kumukwiyitsa pamene munkapereka nsembe zanu kwa Baala. 18 Yehova anandiwululira ndipo ndinadziwa. Iye anatsekula maso anga kuti ndione chiwembu chawocho. 19 Ndinali ngati mwana wankhosa wofatsa amene akupita naye kukamupha; sindinkadziwa kuti chiwembu chimene ankakonzekeracho chinkaloza ine. Iwo amati:“Tiyeni timuphemunthu ameneyukuti dzina lake lisadzakumbukiridwenso.” 20 Koma, Inu Yehova Wamphamvuzonse, Inu amene mumaweruza molungamandi kuyesa mitima ndi maganizo,lolani kuti ine ndione kuti mwawalipsira,pakuti mlandu wanga ndawupereka mʼmanja mwanu. 21 “Nʼchifukwa chake Yehova akunena za anthu a ku Anatoti amene akufuna kuwononga moyo wako namanena kuti, ‘Usanenere mʼdzina la Yehova, ukatero ife tidzakupha ndi manja athu,’ 22 koma Yehova Wamphamvuzonse akuti, ‘Ine ndidzawalanga. Achinyamata awo adzaphedwa ndi lupanga, ana awo aamuna ndi aakazi adzafa ndi njala. 23 Sipadzakhala otsala ndi mmodzi yemwe, chifukwa ndidzalanga anthu a ku Anatoti chikadzafika chaka chawo cha chilango.’ ”

In Other Versions

Jeremiah 11 in the ANGEFD

Jeremiah 11 in the ANTPNG2D

Jeremiah 11 in the AS21

Jeremiah 11 in the BAGH

Jeremiah 11 in the BBPNG

Jeremiah 11 in the BBT1E

Jeremiah 11 in the BDS

Jeremiah 11 in the BEV

Jeremiah 11 in the BHAD

Jeremiah 11 in the BIB

Jeremiah 11 in the BLPT

Jeremiah 11 in the BNT

Jeremiah 11 in the BNTABOOT

Jeremiah 11 in the BNTLV

Jeremiah 11 in the BOATCB

Jeremiah 11 in the BOATCB2

Jeremiah 11 in the BOBCV

Jeremiah 11 in the BOCNT

Jeremiah 11 in the BOECS

Jeremiah 11 in the BOHCB

Jeremiah 11 in the BOHCV

Jeremiah 11 in the BOHLNT

Jeremiah 11 in the BOHNTLTAL

Jeremiah 11 in the BOICB

Jeremiah 11 in the BOILNTAP

Jeremiah 11 in the BOITCV

Jeremiah 11 in the BOKCV

Jeremiah 11 in the BOKCV2

Jeremiah 11 in the BOKHWOG

Jeremiah 11 in the BOKSSV

Jeremiah 11 in the BOLCB

Jeremiah 11 in the BOLCB2

Jeremiah 11 in the BOMCV

Jeremiah 11 in the BONAV

Jeremiah 11 in the BONCB

Jeremiah 11 in the BONLT

Jeremiah 11 in the BONUT2

Jeremiah 11 in the BOPLNT

Jeremiah 11 in the BOSCB

Jeremiah 11 in the BOSNC

Jeremiah 11 in the BOTLNT

Jeremiah 11 in the BOVCB

Jeremiah 11 in the BOYCB

Jeremiah 11 in the BPBB

Jeremiah 11 in the BPH

Jeremiah 11 in the BSB

Jeremiah 11 in the CCB

Jeremiah 11 in the CUV

Jeremiah 11 in the CUVS

Jeremiah 11 in the DBT

Jeremiah 11 in the DGDNT

Jeremiah 11 in the DHNT

Jeremiah 11 in the DNT

Jeremiah 11 in the ELBE

Jeremiah 11 in the EMTV

Jeremiah 11 in the ESV

Jeremiah 11 in the FBV

Jeremiah 11 in the FEB

Jeremiah 11 in the GGMNT

Jeremiah 11 in the GNT

Jeremiah 11 in the HARY

Jeremiah 11 in the HNT

Jeremiah 11 in the IRVA

Jeremiah 11 in the IRVB

Jeremiah 11 in the IRVG

Jeremiah 11 in the IRVH

Jeremiah 11 in the IRVK

Jeremiah 11 in the IRVM

Jeremiah 11 in the IRVM2

Jeremiah 11 in the IRVO

Jeremiah 11 in the IRVP

Jeremiah 11 in the IRVT

Jeremiah 11 in the IRVT2

Jeremiah 11 in the IRVU

Jeremiah 11 in the ISVN

Jeremiah 11 in the JSNT

Jeremiah 11 in the KAPI

Jeremiah 11 in the KBT1ETNIK

Jeremiah 11 in the KBV

Jeremiah 11 in the KJV

Jeremiah 11 in the KNFD

Jeremiah 11 in the LBA

Jeremiah 11 in the LBLA

Jeremiah 11 in the LNT

Jeremiah 11 in the LSV

Jeremiah 11 in the MAAL

Jeremiah 11 in the MBV

Jeremiah 11 in the MBV2

Jeremiah 11 in the MHNT

Jeremiah 11 in the MKNFD

Jeremiah 11 in the MNG

Jeremiah 11 in the MNT

Jeremiah 11 in the MNT2

Jeremiah 11 in the MRS1T

Jeremiah 11 in the NAA

Jeremiah 11 in the NASB

Jeremiah 11 in the NBLA

Jeremiah 11 in the NBS

Jeremiah 11 in the NBVTP

Jeremiah 11 in the NET2

Jeremiah 11 in the NIV11

Jeremiah 11 in the NNT

Jeremiah 11 in the NNT2

Jeremiah 11 in the NNT3

Jeremiah 11 in the PDDPT

Jeremiah 11 in the PFNT

Jeremiah 11 in the RMNT

Jeremiah 11 in the SBIAS

Jeremiah 11 in the SBIBS

Jeremiah 11 in the SBIBS2

Jeremiah 11 in the SBICS

Jeremiah 11 in the SBIDS

Jeremiah 11 in the SBIGS

Jeremiah 11 in the SBIHS

Jeremiah 11 in the SBIIS

Jeremiah 11 in the SBIIS2

Jeremiah 11 in the SBIIS3

Jeremiah 11 in the SBIKS

Jeremiah 11 in the SBIKS2

Jeremiah 11 in the SBIMS

Jeremiah 11 in the SBIOS

Jeremiah 11 in the SBIPS

Jeremiah 11 in the SBISS

Jeremiah 11 in the SBITS

Jeremiah 11 in the SBITS2

Jeremiah 11 in the SBITS3

Jeremiah 11 in the SBITS4

Jeremiah 11 in the SBIUS

Jeremiah 11 in the SBIVS

Jeremiah 11 in the SBT

Jeremiah 11 in the SBT1E

Jeremiah 11 in the SCHL

Jeremiah 11 in the SNT

Jeremiah 11 in the SUSU

Jeremiah 11 in the SUSU2

Jeremiah 11 in the SYNO

Jeremiah 11 in the TBIAOTANT

Jeremiah 11 in the TBT1E

Jeremiah 11 in the TBT1E2

Jeremiah 11 in the TFTIP

Jeremiah 11 in the TFTU

Jeremiah 11 in the TGNTATF3T

Jeremiah 11 in the THAI

Jeremiah 11 in the TNFD

Jeremiah 11 in the TNT

Jeremiah 11 in the TNTIK

Jeremiah 11 in the TNTIL

Jeremiah 11 in the TNTIN

Jeremiah 11 in the TNTIP

Jeremiah 11 in the TNTIZ

Jeremiah 11 in the TOMA

Jeremiah 11 in the TTENT

Jeremiah 11 in the UBG

Jeremiah 11 in the UGV

Jeremiah 11 in the UGV2

Jeremiah 11 in the UGV3

Jeremiah 11 in the VBL

Jeremiah 11 in the VDCC

Jeremiah 11 in the YALU

Jeremiah 11 in the YAPE

Jeremiah 11 in the YBVTP

Jeremiah 11 in the ZBP