Leviticus 18 (BOGWICC)

1 Yehova anawuza Mose kuti, 2 “Yankhula ndi Aisraeli ndipo uwawuze kuti, ‘Ine ndine Yehova Mulungu wanu. 3 Musamachite zomwe amachita anthu a ku Igupto kumene munkakhala kuja, ndiponso musamachite zomwe amachita anthu a ku Kanaani kumene ndikukupititsani. Musatsatire miyambo yawo. 4 Inu muzimvera malamulo anga ndipo muzisamalitsa kutsatira malangizo anga. Ine ndine Yehova Mulungu wanu. 5 Choncho sungani malangizo ndi malamulo anga, popeza munthu amene amvera zimenezi adzakhala ndi moyo. Ine ndine Yehova. 6 “ ‘Munthu aliyense asagonane ndi wachibale wake. Ine ndine Yehova. 7 “ ‘Usachititse manyazi abambo ako pogonana ndi amayi ako. Iwo ndi amayi ako. Usagonane nawo. 8 “ ‘Usagonane ndi mkazi wa abambo ako (osakhala amayi okubala). Ukatero ukuchititsa manyazi abambo ako. 9 “ ‘Usagonane ndi mlongo wako, mwana wamkazi wa abambo ako, kapena mwana wamkazi wa amayi ako, kaya anabadwira mʼnyumba mwanu kapena kwina. 10 “ ‘Usagonane ndi mdzukulu wako: mwana wa mwana wako wamwamuna kapena mwana wa mwana wako wamkazi. Kutero nʼkudzichotsa ulemu. 11 “ ‘Usagonane ndi mwana wamkazi wa mkazi wa abambo ako, amene abambo akowo anabereka; popeza ameneyo ndi mlongo wako. 12 “ ‘Usagonane ndi mlongo wa abambo ako; popeza ameneyo ndi thupi limodzi ndi abambo ako. 13 “ ‘Usagonane ndi mchemwali wa amayi ako chifukwa ameneyo ndi thupi limodzi ndi amayi ako. 14 “ ‘Usachititse manyazi mchimwene wa abambo ako pogonana ndi mkazi wake popeza amenewo ndi azakhali ako. 15 “ ‘Usagonane ndi mpongozi wako popeza ameneyo ndi mkazi wa mwana wako. Choncho usamuchititse manyazi. 16 “ ‘Usagonane ndi mkazi wa mchimwene wako popeza potero ukuchititsa manyazi mʼbale wakoyo. 17 “ ‘Usagonane ndi mkazi ndiponso mwana wake wamkazi. Usagonane ndi mwana wamkazi wa mwana wake wamwamuna, kapena mwana wamkazi wa mwana wake wamkazi. Amenewo ndi thupi limodzi ndi mkaziyo. Kutero ndikuchita chinthu choyipa kwambiri. 18 “ ‘Usakwatire mchemwali wa mkazi wako ndi kumagonana naye mkazi wakoyo ali moyo ngati wopikisana naye. 19 “ ‘Usamuyandikire mkazi kuti ugonane naye pa nthawi yake yosamba. 20 “ ‘Usagonane ndi mkazi wa mnzako ndi kudziyipitsa naye. 21 “ ‘Usapereke mwana wako aliyense kuti akhale nsembe yamoto kwa Moleki ndi kuyipitsa dzina la Yehova. Ine ndine Yehova. 22 “ ‘Usagonane ndi mwamuna ngati mkazi; chimenecho ndi chinthu chonyansa. 23 “ ‘Usagonane ndi nyama ndi kudziyipitsa nayo. Mkazi asadzipereke kwa nyama kuti agonane nayo. Chimenecho ndi chisokonezo. 24 “ ‘Musadzidetse ndi zinthu zimenezi chifukwa umo ndi mmene mitundu ina imene ndikuyithamangitsa pamaso panu inadzidetsera. 25 Choncho dziko linayipa ndipo ndinalilanga chifukwa cha tchimo lake. Motero dzikolo linasanza anthu ake okhalamo. 26 Koma inu mukasunge malangizo ndi malamulo anga. Mbadwa ndiponso alendo amene akukhala pakati panu asakachite china chilichonse cha zinthu zonyansazi, 27 pakuti zinthu zonsezi ndi zomwe ankachita anthu amene ankakhala mʼdzikomo inu musanafike, ndipo dziko linayipitsidwa. 28 Koma inu musachite zimenezi kuti dziko lingakusanzeni mutaliyipitsa monga linasanzira mitundu imene imakhalamo inu musanafike. 29 “ ‘Aliyense wochita zinthu zonyansa zimenezi achotsedwe pakati pa anthu anzake. 30 Choncho mverani malangizo anga oletsa kuchita miyambo yonyansayi imene ankatsatira anthu amene analipo inu musanafike ndi kudziyipitsa nayo. Ine ndine Yehova Mulungu wanu.’ ”

In Other Versions

Leviticus 18 in the ANGEFD

Leviticus 18 in the ANTPNG2D

Leviticus 18 in the AS21

Leviticus 18 in the BAGH

Leviticus 18 in the BBPNG

Leviticus 18 in the BBT1E

Leviticus 18 in the BDS

Leviticus 18 in the BEV

Leviticus 18 in the BHAD

Leviticus 18 in the BIB

Leviticus 18 in the BLPT

Leviticus 18 in the BNT

Leviticus 18 in the BNTABOOT

Leviticus 18 in the BNTLV

Leviticus 18 in the BOATCB

Leviticus 18 in the BOATCB2

Leviticus 18 in the BOBCV

Leviticus 18 in the BOCNT

Leviticus 18 in the BOECS

Leviticus 18 in the BOHCB

Leviticus 18 in the BOHCV

Leviticus 18 in the BOHLNT

Leviticus 18 in the BOHNTLTAL

Leviticus 18 in the BOICB

Leviticus 18 in the BOILNTAP

Leviticus 18 in the BOITCV

Leviticus 18 in the BOKCV

Leviticus 18 in the BOKCV2

Leviticus 18 in the BOKHWOG

Leviticus 18 in the BOKSSV

Leviticus 18 in the BOLCB

Leviticus 18 in the BOLCB2

Leviticus 18 in the BOMCV

Leviticus 18 in the BONAV

Leviticus 18 in the BONCB

Leviticus 18 in the BONLT

Leviticus 18 in the BONUT2

Leviticus 18 in the BOPLNT

Leviticus 18 in the BOSCB

Leviticus 18 in the BOSNC

Leviticus 18 in the BOTLNT

Leviticus 18 in the BOVCB

Leviticus 18 in the BOYCB

Leviticus 18 in the BPBB

Leviticus 18 in the BPH

Leviticus 18 in the BSB

Leviticus 18 in the CCB

Leviticus 18 in the CUV

Leviticus 18 in the CUVS

Leviticus 18 in the DBT

Leviticus 18 in the DGDNT

Leviticus 18 in the DHNT

Leviticus 18 in the DNT

Leviticus 18 in the ELBE

Leviticus 18 in the EMTV

Leviticus 18 in the ESV

Leviticus 18 in the FBV

Leviticus 18 in the FEB

Leviticus 18 in the GGMNT

Leviticus 18 in the GNT

Leviticus 18 in the HARY

Leviticus 18 in the HNT

Leviticus 18 in the IRVA

Leviticus 18 in the IRVB

Leviticus 18 in the IRVG

Leviticus 18 in the IRVH

Leviticus 18 in the IRVK

Leviticus 18 in the IRVM

Leviticus 18 in the IRVM2

Leviticus 18 in the IRVO

Leviticus 18 in the IRVP

Leviticus 18 in the IRVT

Leviticus 18 in the IRVT2

Leviticus 18 in the IRVU

Leviticus 18 in the ISVN

Leviticus 18 in the JSNT

Leviticus 18 in the KAPI

Leviticus 18 in the KBT1ETNIK

Leviticus 18 in the KBV

Leviticus 18 in the KJV

Leviticus 18 in the KNFD

Leviticus 18 in the LBA

Leviticus 18 in the LBLA

Leviticus 18 in the LNT

Leviticus 18 in the LSV

Leviticus 18 in the MAAL

Leviticus 18 in the MBV

Leviticus 18 in the MBV2

Leviticus 18 in the MHNT

Leviticus 18 in the MKNFD

Leviticus 18 in the MNG

Leviticus 18 in the MNT

Leviticus 18 in the MNT2

Leviticus 18 in the MRS1T

Leviticus 18 in the NAA

Leviticus 18 in the NASB

Leviticus 18 in the NBLA

Leviticus 18 in the NBS

Leviticus 18 in the NBVTP

Leviticus 18 in the NET2

Leviticus 18 in the NIV11

Leviticus 18 in the NNT

Leviticus 18 in the NNT2

Leviticus 18 in the NNT3

Leviticus 18 in the PDDPT

Leviticus 18 in the PFNT

Leviticus 18 in the RMNT

Leviticus 18 in the SBIAS

Leviticus 18 in the SBIBS

Leviticus 18 in the SBIBS2

Leviticus 18 in the SBICS

Leviticus 18 in the SBIDS

Leviticus 18 in the SBIGS

Leviticus 18 in the SBIHS

Leviticus 18 in the SBIIS

Leviticus 18 in the SBIIS2

Leviticus 18 in the SBIIS3

Leviticus 18 in the SBIKS

Leviticus 18 in the SBIKS2

Leviticus 18 in the SBIMS

Leviticus 18 in the SBIOS

Leviticus 18 in the SBIPS

Leviticus 18 in the SBISS

Leviticus 18 in the SBITS

Leviticus 18 in the SBITS2

Leviticus 18 in the SBITS3

Leviticus 18 in the SBITS4

Leviticus 18 in the SBIUS

Leviticus 18 in the SBIVS

Leviticus 18 in the SBT

Leviticus 18 in the SBT1E

Leviticus 18 in the SCHL

Leviticus 18 in the SNT

Leviticus 18 in the SUSU

Leviticus 18 in the SUSU2

Leviticus 18 in the SYNO

Leviticus 18 in the TBIAOTANT

Leviticus 18 in the TBT1E

Leviticus 18 in the TBT1E2

Leviticus 18 in the TFTIP

Leviticus 18 in the TFTU

Leviticus 18 in the TGNTATF3T

Leviticus 18 in the THAI

Leviticus 18 in the TNFD

Leviticus 18 in the TNT

Leviticus 18 in the TNTIK

Leviticus 18 in the TNTIL

Leviticus 18 in the TNTIN

Leviticus 18 in the TNTIP

Leviticus 18 in the TNTIZ

Leviticus 18 in the TOMA

Leviticus 18 in the TTENT

Leviticus 18 in the UBG

Leviticus 18 in the UGV

Leviticus 18 in the UGV2

Leviticus 18 in the UGV3

Leviticus 18 in the VBL

Leviticus 18 in the VDCC

Leviticus 18 in the YALU

Leviticus 18 in the YAPE

Leviticus 18 in the YBVTP

Leviticus 18 in the ZBP