Micah 6 (BOGWICC)

1 Tamverani zimene Yehova akunena:“Nyamukani, fotokozani mlandu wanu pamaso pa mapiri;zitunda zimve zimene inu muti muyankhule. 2 Imvani mlandu wa Yehova, inu mapiri;tamverani, maziko amuyaya a dziko lapansi.Pakuti Yehova ali ndi mlandu ndi anthu ake;Iye akutsutsa Aisraeli. 3 “Anthu anga, kodi ndakuchitirani chiyani?Kodi ndakutopetsani bwanji? Ndiyankheni. 4 Ine ndinakutulutsani ku dziko la Iguptondi kukuwombolani ku nyumba ya ukapolo.Ndinatuma Mose kuti akutsogolereni,pamodzi ndi Aaroni ndi Miriamu. 5 Anthu anga, kumbukiranizimene Balaki mfumu ya ku Mowabu inafuna kukuchitiranindiponso zimene Balaamu mwana wa Beori anayankha.Kumbukirani zomwe zinachitika pa ulendo wochoka ku Sitimu kupita ku Giligala,kuti mudziwe machitidwe olungama a Yehova.” 6 Kodi ndidzatenga chiyani kupita nacho pamaso pa Yehovandi kukagwada pamaso pa Mulungu wakumwamba?Kodi ndidzabwera pamaso pake ndi nsembe yopsereza,ndi ana angʼombe a chaka chimodzi? 7 Kodi Yehova adzakondwera ndi nkhosa zazimuna 1,000,kapena ndi mitsinje yosalekeza ya mafuta?Kodi ndipereke nsembe mwana wanga woyamba kubadwa chifukwa cha zolakwa zanga?Chipatso cha thupi langa chifukwa cha tchimo la moyo wanga? 8 Munthu iwe, Yehova wakuonetsa kale chimene chili chabwino.Tsono kodi Yehova akuyembekezera chiyani kwa iwe?Uzichita zolungama ndi kukonda chifundondiponso kuyenda modzichepetsa pamaso pa Mulungu wako. 9 Tamverani! Yehova akuyitana anthu okhala mu mzindandi nzeru kuopa dzina lanu.“Mverani mfumu ndi Iye amene anayikhazikitsa. 10 Inu anthu oyipa, kodi Ine nʼkuyiwalachuma chanu chimene munachipeza mwachinyengo,ndiponso muyeso wanu woperewera umene ndi wotembereredwa? 11 Kodi ndimutenge ngati wosalakwa munthu amene ali ndi sikelo yachinyengo,ndiponso miyeso yabodza mʼthumba lake? 12 Anthu ake olemera amachita zachiwawa;anthu ake ndi abodzandipo pakamwa pawo pamayankhula zachinyengo. 13 Choncho, ndayamba kukuwonongani,kukusakazani chifukwa cha machimo anu. 14 Mudzadya, koma simudzakhuta;mudzakhalabe ndi njala.Mudzasunga zinthu, koma sizidzasungika,chifukwa zimene mudzasunga zidzawonongedwa ndi lupanga. 15 Mudzadzala, koma simudzakolola.Mudzayenga mafuta a olivi, koma simudzawagwiritsa ntchito.Mudzaponda mphesa, koma simudzamwa vinyo wake. 16 Inu mwatsatira malangizo a Omurindiponso machitidwe onse a banja la Ahabu,ndi khalidwe lawo lonse.Choncho Ine ndidzakuperekani kuti muwonongedwendiponso anthu anu kuti azunguzike mitu;mudzanyozedwa ndi anthu a mitundu ina.”

In Other Versions

Micah 6 in the ANGEFD

Micah 6 in the ANTPNG2D

Micah 6 in the AS21

Micah 6 in the BAGH

Micah 6 in the BBPNG

Micah 6 in the BBT1E

Micah 6 in the BDS

Micah 6 in the BEV

Micah 6 in the BHAD

Micah 6 in the BIB

Micah 6 in the BLPT

Micah 6 in the BNT

Micah 6 in the BNTABOOT

Micah 6 in the BNTLV

Micah 6 in the BOATCB

Micah 6 in the BOATCB2

Micah 6 in the BOBCV

Micah 6 in the BOCNT

Micah 6 in the BOECS

Micah 6 in the BOHCB

Micah 6 in the BOHCV

Micah 6 in the BOHLNT

Micah 6 in the BOHNTLTAL

Micah 6 in the BOICB

Micah 6 in the BOILNTAP

Micah 6 in the BOITCV

Micah 6 in the BOKCV

Micah 6 in the BOKCV2

Micah 6 in the BOKHWOG

Micah 6 in the BOKSSV

Micah 6 in the BOLCB

Micah 6 in the BOLCB2

Micah 6 in the BOMCV

Micah 6 in the BONAV

Micah 6 in the BONCB

Micah 6 in the BONLT

Micah 6 in the BONUT2

Micah 6 in the BOPLNT

Micah 6 in the BOSCB

Micah 6 in the BOSNC

Micah 6 in the BOTLNT

Micah 6 in the BOVCB

Micah 6 in the BOYCB

Micah 6 in the BPBB

Micah 6 in the BPH

Micah 6 in the BSB

Micah 6 in the CCB

Micah 6 in the CUV

Micah 6 in the CUVS

Micah 6 in the DBT

Micah 6 in the DGDNT

Micah 6 in the DHNT

Micah 6 in the DNT

Micah 6 in the ELBE

Micah 6 in the EMTV

Micah 6 in the ESV

Micah 6 in the FBV

Micah 6 in the FEB

Micah 6 in the GGMNT

Micah 6 in the GNT

Micah 6 in the HARY

Micah 6 in the HNT

Micah 6 in the IRVA

Micah 6 in the IRVB

Micah 6 in the IRVG

Micah 6 in the IRVH

Micah 6 in the IRVK

Micah 6 in the IRVM

Micah 6 in the IRVM2

Micah 6 in the IRVO

Micah 6 in the IRVP

Micah 6 in the IRVT

Micah 6 in the IRVT2

Micah 6 in the IRVU

Micah 6 in the ISVN

Micah 6 in the JSNT

Micah 6 in the KAPI

Micah 6 in the KBT1ETNIK

Micah 6 in the KBV

Micah 6 in the KJV

Micah 6 in the KNFD

Micah 6 in the LBA

Micah 6 in the LBLA

Micah 6 in the LNT

Micah 6 in the LSV

Micah 6 in the MAAL

Micah 6 in the MBV

Micah 6 in the MBV2

Micah 6 in the MHNT

Micah 6 in the MKNFD

Micah 6 in the MNG

Micah 6 in the MNT

Micah 6 in the MNT2

Micah 6 in the MRS1T

Micah 6 in the NAA

Micah 6 in the NASB

Micah 6 in the NBLA

Micah 6 in the NBS

Micah 6 in the NBVTP

Micah 6 in the NET2

Micah 6 in the NIV11

Micah 6 in the NNT

Micah 6 in the NNT2

Micah 6 in the NNT3

Micah 6 in the PDDPT

Micah 6 in the PFNT

Micah 6 in the RMNT

Micah 6 in the SBIAS

Micah 6 in the SBIBS

Micah 6 in the SBIBS2

Micah 6 in the SBICS

Micah 6 in the SBIDS

Micah 6 in the SBIGS

Micah 6 in the SBIHS

Micah 6 in the SBIIS

Micah 6 in the SBIIS2

Micah 6 in the SBIIS3

Micah 6 in the SBIKS

Micah 6 in the SBIKS2

Micah 6 in the SBIMS

Micah 6 in the SBIOS

Micah 6 in the SBIPS

Micah 6 in the SBISS

Micah 6 in the SBITS

Micah 6 in the SBITS2

Micah 6 in the SBITS3

Micah 6 in the SBITS4

Micah 6 in the SBIUS

Micah 6 in the SBIVS

Micah 6 in the SBT

Micah 6 in the SBT1E

Micah 6 in the SCHL

Micah 6 in the SNT

Micah 6 in the SUSU

Micah 6 in the SUSU2

Micah 6 in the SYNO

Micah 6 in the TBIAOTANT

Micah 6 in the TBT1E

Micah 6 in the TBT1E2

Micah 6 in the TFTIP

Micah 6 in the TFTU

Micah 6 in the TGNTATF3T

Micah 6 in the THAI

Micah 6 in the TNFD

Micah 6 in the TNT

Micah 6 in the TNTIK

Micah 6 in the TNTIL

Micah 6 in the TNTIN

Micah 6 in the TNTIP

Micah 6 in the TNTIZ

Micah 6 in the TOMA

Micah 6 in the TTENT

Micah 6 in the UBG

Micah 6 in the UGV

Micah 6 in the UGV2

Micah 6 in the UGV3

Micah 6 in the VBL

Micah 6 in the VDCC

Micah 6 in the YALU

Micah 6 in the YAPE

Micah 6 in the YBVTP

Micah 6 in the ZBP