Ecclesiastes 5 (BOGWICC)

1 Uzisamala mayendedwe ako pamene ukupita ku nyumba ya Mulungu. Upite pafupi kuti ukamvetsere mʼmalo mopereka nsembe ya zitsiru zimene sizizindikira kuti zikuchita zolakwa. 2 Usamafulumire kuyankhula,usafulumire mu mtima mwakokunena chilichonse pamaso pa Mulungu.Mulungu ali kumwambandipo iwe uli pa dziko lapansi,choncho mawu ako akhale ochepa. 3 Kuchuluka kwa mavuto mu mtima kumabweretsa maloto oyipa,ndipo kuchuluka kwa mawu kumadzetsa uchitsiru. 4 Pamene ulumbira kwa Mulungu usachedwe kukwaniritsa chimene walumbiracho. Iye sakondweretsedwa ndi chitsiru; kwaniritsa lumbiro lako. 5 Kuli bwino kusalumbira kusiyana ndi kulumbira koma osakwaniritsa lumbirolo. 6 Pakamwa pako pasakuchimwitse. Ndipo usanene kwa mthenga wa mʼNyumba ya Mulungu kuti, “Ndinalakwitsa polumbira.” Chifukwa chiyani ukufuna Mulungu akwiye ndi mawu ako ndiponso ntchito ya manja ako? 7 Maloto ochuluka ndi mawu ochuluka ndi zinthu zopandapake. Kotero lemekeza Mulungu. 8 Ngati uwona anthu osauka akuzunzika mʼdziko, ndiponso anthu ena akupsinja anzawo ndi kuwalanda ufulu wawo, usadabwe ndi zinthu zimenezi; pakuti woyangʼanira ali naye wina womuyangʼanira wamkulu, ndipo pamwamba pa awiriwa pali ena akuluakulu owaposa. 9 Anthu onse amatengako zokolola za mʼminda: koma ndi mfumu yokha imene imapeza phindu la mindayi. 10 Aliyense amene amakonda ndalama sakhutitsidwa ndi ndalamazo;aliyense amene amakonda chuma sakhutitsidwa ndi zimene amapeza.Izinso ndi zopandapake. 11 Chuma chikachulukaakudya nawo chumacho amachulukanso.Nanga mwini wake amapindulapo chiyanikuposa kumangochiyangʼana ndi maso ake? 12 Wantchito amagona tulo tabwinongakhale adye pangʼono kapena kudya kwambiri,koma munthu wolemera, chumasichimulola kuti agone. 13 Ine ndinaona choyipa chomvetsa chisoni pansi pano:chuma chokundikidwa chikupweteka mwini wake yemwe, 14 kapena chuma chowonongedwa pa nthawi yatsoka,kotero kuti pamene wabereka mwanaalibe kanthu koti amusiyire. 15 Munthu anabadwa wamaliseche kuchokera mʼmimba mwa amayi ake,ndipo monga iye anabadwira, adzapitanso choncho.Pa zonse zimene iye anakhetsera thukutapalibe nʼchimodzi chomwe chimene adzatenge mʼmanja mwake. 16 Izinso ndi zoyipa kwambiri:munthu adzapita monga momwe anabwerera,ndipo iye amapindula chiyani,pakuti amagwira ntchito yolemetsa yopanda phindu? 17 Masiku ake onse ndi odzaza ndi mdima,kukhumudwa kwakukulu, masautso ndi nkhawa. 18 Tsono ndinazindikira kuti nʼchabwino ndi choyenera kuti munthu azidya ndi kumwa, ndi kukhutitsidwa ndi ntchito yake yolemetsa imene amayigwira pansi pano pa nthawi yake yochepa imene Mulungu amamupatsa, poti ichi ndiye chake. 19 Komatu pamene Mulungu apereka chuma kwa munthu aliyense ndi zinthu zina, ndi kulola kuti akondwere ndi chumacho, munthuyo alandire chumacho ndi kusangalala ndi ntchito yake, imene ndi mphatso yochokera kwa Mulungu. 20 Munthu wotereyu saganizirapo za masiku a moyo wake, chifukwa Mulungu amamutanganidwitsa ndi chisangalalo cha mu mtima mwake.

In Other Versions

Ecclesiastes 5 in the ANGEFD

Ecclesiastes 5 in the ANTPNG2D

Ecclesiastes 5 in the AS21

Ecclesiastes 5 in the BAGH

Ecclesiastes 5 in the BBPNG

Ecclesiastes 5 in the BBT1E

Ecclesiastes 5 in the BDS

Ecclesiastes 5 in the BEV

Ecclesiastes 5 in the BHAD

Ecclesiastes 5 in the BIB

Ecclesiastes 5 in the BLPT

Ecclesiastes 5 in the BNT

Ecclesiastes 5 in the BNTABOOT

Ecclesiastes 5 in the BNTLV

Ecclesiastes 5 in the BOATCB

Ecclesiastes 5 in the BOATCB2

Ecclesiastes 5 in the BOBCV

Ecclesiastes 5 in the BOCNT

Ecclesiastes 5 in the BOECS

Ecclesiastes 5 in the BOHCB

Ecclesiastes 5 in the BOHCV

Ecclesiastes 5 in the BOHLNT

Ecclesiastes 5 in the BOHNTLTAL

Ecclesiastes 5 in the BOICB

Ecclesiastes 5 in the BOILNTAP

Ecclesiastes 5 in the BOITCV

Ecclesiastes 5 in the BOKCV

Ecclesiastes 5 in the BOKCV2

Ecclesiastes 5 in the BOKHWOG

Ecclesiastes 5 in the BOKSSV

Ecclesiastes 5 in the BOLCB

Ecclesiastes 5 in the BOLCB2

Ecclesiastes 5 in the BOMCV

Ecclesiastes 5 in the BONAV

Ecclesiastes 5 in the BONCB

Ecclesiastes 5 in the BONLT

Ecclesiastes 5 in the BONUT2

Ecclesiastes 5 in the BOPLNT

Ecclesiastes 5 in the BOSCB

Ecclesiastes 5 in the BOSNC

Ecclesiastes 5 in the BOTLNT

Ecclesiastes 5 in the BOVCB

Ecclesiastes 5 in the BOYCB

Ecclesiastes 5 in the BPBB

Ecclesiastes 5 in the BPH

Ecclesiastes 5 in the BSB

Ecclesiastes 5 in the CCB

Ecclesiastes 5 in the CUV

Ecclesiastes 5 in the CUVS

Ecclesiastes 5 in the DBT

Ecclesiastes 5 in the DGDNT

Ecclesiastes 5 in the DHNT

Ecclesiastes 5 in the DNT

Ecclesiastes 5 in the ELBE

Ecclesiastes 5 in the EMTV

Ecclesiastes 5 in the ESV

Ecclesiastes 5 in the FBV

Ecclesiastes 5 in the FEB

Ecclesiastes 5 in the GGMNT

Ecclesiastes 5 in the GNT

Ecclesiastes 5 in the HARY

Ecclesiastes 5 in the HNT

Ecclesiastes 5 in the IRVA

Ecclesiastes 5 in the IRVB

Ecclesiastes 5 in the IRVG

Ecclesiastes 5 in the IRVH

Ecclesiastes 5 in the IRVK

Ecclesiastes 5 in the IRVM

Ecclesiastes 5 in the IRVM2

Ecclesiastes 5 in the IRVO

Ecclesiastes 5 in the IRVP

Ecclesiastes 5 in the IRVT

Ecclesiastes 5 in the IRVT2

Ecclesiastes 5 in the IRVU

Ecclesiastes 5 in the ISVN

Ecclesiastes 5 in the JSNT

Ecclesiastes 5 in the KAPI

Ecclesiastes 5 in the KBT1ETNIK

Ecclesiastes 5 in the KBV

Ecclesiastes 5 in the KJV

Ecclesiastes 5 in the KNFD

Ecclesiastes 5 in the LBA

Ecclesiastes 5 in the LBLA

Ecclesiastes 5 in the LNT

Ecclesiastes 5 in the LSV

Ecclesiastes 5 in the MAAL

Ecclesiastes 5 in the MBV

Ecclesiastes 5 in the MBV2

Ecclesiastes 5 in the MHNT

Ecclesiastes 5 in the MKNFD

Ecclesiastes 5 in the MNG

Ecclesiastes 5 in the MNT

Ecclesiastes 5 in the MNT2

Ecclesiastes 5 in the MRS1T

Ecclesiastes 5 in the NAA

Ecclesiastes 5 in the NASB

Ecclesiastes 5 in the NBLA

Ecclesiastes 5 in the NBS

Ecclesiastes 5 in the NBVTP

Ecclesiastes 5 in the NET2

Ecclesiastes 5 in the NIV11

Ecclesiastes 5 in the NNT

Ecclesiastes 5 in the NNT2

Ecclesiastes 5 in the NNT3

Ecclesiastes 5 in the PDDPT

Ecclesiastes 5 in the PFNT

Ecclesiastes 5 in the RMNT

Ecclesiastes 5 in the SBIAS

Ecclesiastes 5 in the SBIBS

Ecclesiastes 5 in the SBIBS2

Ecclesiastes 5 in the SBICS

Ecclesiastes 5 in the SBIDS

Ecclesiastes 5 in the SBIGS

Ecclesiastes 5 in the SBIHS

Ecclesiastes 5 in the SBIIS

Ecclesiastes 5 in the SBIIS2

Ecclesiastes 5 in the SBIIS3

Ecclesiastes 5 in the SBIKS

Ecclesiastes 5 in the SBIKS2

Ecclesiastes 5 in the SBIMS

Ecclesiastes 5 in the SBIOS

Ecclesiastes 5 in the SBIPS

Ecclesiastes 5 in the SBISS

Ecclesiastes 5 in the SBITS

Ecclesiastes 5 in the SBITS2

Ecclesiastes 5 in the SBITS3

Ecclesiastes 5 in the SBITS4

Ecclesiastes 5 in the SBIUS

Ecclesiastes 5 in the SBIVS

Ecclesiastes 5 in the SBT

Ecclesiastes 5 in the SBT1E

Ecclesiastes 5 in the SCHL

Ecclesiastes 5 in the SNT

Ecclesiastes 5 in the SUSU

Ecclesiastes 5 in the SUSU2

Ecclesiastes 5 in the SYNO

Ecclesiastes 5 in the TBIAOTANT

Ecclesiastes 5 in the TBT1E

Ecclesiastes 5 in the TBT1E2

Ecclesiastes 5 in the TFTIP

Ecclesiastes 5 in the TFTU

Ecclesiastes 5 in the TGNTATF3T

Ecclesiastes 5 in the THAI

Ecclesiastes 5 in the TNFD

Ecclesiastes 5 in the TNT

Ecclesiastes 5 in the TNTIK

Ecclesiastes 5 in the TNTIL

Ecclesiastes 5 in the TNTIN

Ecclesiastes 5 in the TNTIP

Ecclesiastes 5 in the TNTIZ

Ecclesiastes 5 in the TOMA

Ecclesiastes 5 in the TTENT

Ecclesiastes 5 in the UBG

Ecclesiastes 5 in the UGV

Ecclesiastes 5 in the UGV2

Ecclesiastes 5 in the UGV3

Ecclesiastes 5 in the VBL

Ecclesiastes 5 in the VDCC

Ecclesiastes 5 in the YALU

Ecclesiastes 5 in the YAPE

Ecclesiastes 5 in the YBVTP

Ecclesiastes 5 in the ZBP