Jeremiah 42 (BOGWICC)

1 Atsogoleri onse a ankhondo pamodzi ndi Yohanani mwana wa Kareya ndi Azariya mwana wa Hosayia, ndiponso anthu onse, ana ndi akuluakulu omwe, anapita 2 kwa mneneri Yeremiya ndipo anamuwuza kuti, “Chonde imvani dandawulo lathu ndipo mutipempherere anthu otsalafe kwa Yehova Mulungu wanu. Pakuti monga tsopano mukuona, ngakhale kuti kale tinalipo ambiri, koma tsopano ochepa okha ndiye amene atsala. 3 Mupemphere kuti Yehova Mulungu wanu atiwuze kumene tiyenera kupita ndi chimene tiyenera kuchita.” 4 Mneneri Yeremiya anawayankha kuti, “Ndamva zimene mwanenazi. Ndithu ndidzapemphera kwa Yehova Mulungu wanu monga momwe mwandipemphera. Ndidzakuwuzani chilichonse chimene Yehova anene ndipo sindidzakubisirani kanthu kalikonse.” 5 Ndipo iwo anawuza Yeremiya kuti, “Yehova akhale mboni yoona ndi yokhulupirika yodzatitsutsa ife ngati sitichita mogwirizana ndi chilichonse chimene Yehova Mulungu adzakutumani kuti mutiwuze. 6 Kaya ndi zotikomera kapena zosatikomera, ife tidzamvera Yehova Mulungu wathu, amene takutumaniko. Tidzamvera Yehova Mulungu wathu kuti zinthu zidzatiyendere bwino.” 7 Patapita masiku khumi, Yehova anayankhula ndi Yeremiya. 8 Choncho Yeremiya anayitana Yohanani mwana wa Kareya pamodzi ndi atsogoleri onse a ankhondo amene anali naye ndiponso anthu onse, ana ndi akulu omwe. 9 Yehova, Mulungu wa Israeli amene munanditumako kuti ndikapereke madandawulo mʼdzina lanu akuti, 10 “Ngati mukhala mʼdziko muno, ndiye kuti ndidzakukhazikitsani, osakuchotsani. Inde ndidzakudzalani osakuchotsani pakuti ndi kumva chisoni kwambiri chifukwa cha mavuto amene ndabweretsa pa inu. 11 Musayiope mfumu ya ku Babuloni, imene mukuyiopa tsopano. Musachite nayo mantha, akutero Yehova, pakuti Ine ndili nanu ndipo ndidzakupulumutsani ndi kukulanditsani mʼmanja mwake. 12 Ndidzakuchitirani chifundo, ndipo mfumuyonso idzakuchitirani chifundo ndi kukulolani kuti mukhale mʼdziko mwanumwanu. 13 “Koma mwina simudzamvera Yehova Mulungu wanu nʼkumanena kuti, ‘Ayi ife sitidzakhala mʼdziko muno, 14 ndipo ngati mukunena kuti, ‘Ayi, koma tidzapita ku Igupto kumene sitidzaonako nkhondo kapena kumva kulira kwa lipenga kapenanso kusowa chakudya.’ 15 Tsono, inu otsala a ku Yuda, imvani mawu a Yehova. Iye akuti, ngati mutsimikiza zopita ku Igupto, nʼkupitadi kukakhala kumeneko, 16 ndiye nkhondo imene mukuyiopayo idzakugonjetsani ku Igupto komweko. Njala imene mukuyiopayo idzakupezani ku Igupto komweko ndipo mudzafera kumeneko. 17 Kunena zoona, onse amene atsimikiza zopita ku Igupto kuti akakhale kumeneko adzafa ndi nkhondo njala ndi mliri. Palibe ndi mmodzi yemwe amene adzapulumuke kapena kuthawa mavuto amene ndidzawagwetsera.’ 18 Yehova Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israeli akuti, ‘Momwe ndinawakwiyira mwaukali anthu okhala mu Yerusalemu, koteronso ndidzakukwiyirani mukapita ku Igupto. Mudzasanduka chinthu chotembereredwa ndi chochititsa mantha, choseketsa ndi chonyozeka. Malo ano simudzawaonanso.’ 19 “Inu otsala a ku Yuda, Yehova wakuwuzani kuti, ‘Musapite ku Igupto.’ Dziwani chinthu ichi: Ine lero ndikukuchenjezani 20 kuti munalakwitsa kwambiri. Inu munandituma kwa Yehova Mulungu wanu nʼkumati ‘Mukatipempherere kwa Yehova Mulungu wathu, nʼkudzatiwuza chimene afuna kuti tichite, ndipo ife tidzachita.’ 21 Ine lero ndakuwuzani, koma inu simukumverabe zonse zimene Yehova Mulungu anandituma kuti ndikuwuzeni. 22 Tsono dziwani ichi: mudzafadi ndi nkhondo, njala ndi mliri kumalo kumene mukufuna mukakhaleko.”

In Other Versions

Jeremiah 42 in the ANGEFD

Jeremiah 42 in the ANTPNG2D

Jeremiah 42 in the AS21

Jeremiah 42 in the BAGH

Jeremiah 42 in the BBPNG

Jeremiah 42 in the BBT1E

Jeremiah 42 in the BDS

Jeremiah 42 in the BEV

Jeremiah 42 in the BHAD

Jeremiah 42 in the BIB

Jeremiah 42 in the BLPT

Jeremiah 42 in the BNT

Jeremiah 42 in the BNTABOOT

Jeremiah 42 in the BNTLV

Jeremiah 42 in the BOATCB

Jeremiah 42 in the BOATCB2

Jeremiah 42 in the BOBCV

Jeremiah 42 in the BOCNT

Jeremiah 42 in the BOECS

Jeremiah 42 in the BOHCB

Jeremiah 42 in the BOHCV

Jeremiah 42 in the BOHLNT

Jeremiah 42 in the BOHNTLTAL

Jeremiah 42 in the BOICB

Jeremiah 42 in the BOILNTAP

Jeremiah 42 in the BOITCV

Jeremiah 42 in the BOKCV

Jeremiah 42 in the BOKCV2

Jeremiah 42 in the BOKHWOG

Jeremiah 42 in the BOKSSV

Jeremiah 42 in the BOLCB

Jeremiah 42 in the BOLCB2

Jeremiah 42 in the BOMCV

Jeremiah 42 in the BONAV

Jeremiah 42 in the BONCB

Jeremiah 42 in the BONLT

Jeremiah 42 in the BONUT2

Jeremiah 42 in the BOPLNT

Jeremiah 42 in the BOSCB

Jeremiah 42 in the BOSNC

Jeremiah 42 in the BOTLNT

Jeremiah 42 in the BOVCB

Jeremiah 42 in the BOYCB

Jeremiah 42 in the BPBB

Jeremiah 42 in the BPH

Jeremiah 42 in the BSB

Jeremiah 42 in the CCB

Jeremiah 42 in the CUV

Jeremiah 42 in the CUVS

Jeremiah 42 in the DBT

Jeremiah 42 in the DGDNT

Jeremiah 42 in the DHNT

Jeremiah 42 in the DNT

Jeremiah 42 in the ELBE

Jeremiah 42 in the EMTV

Jeremiah 42 in the ESV

Jeremiah 42 in the FBV

Jeremiah 42 in the FEB

Jeremiah 42 in the GGMNT

Jeremiah 42 in the GNT

Jeremiah 42 in the HARY

Jeremiah 42 in the HNT

Jeremiah 42 in the IRVA

Jeremiah 42 in the IRVB

Jeremiah 42 in the IRVG

Jeremiah 42 in the IRVH

Jeremiah 42 in the IRVK

Jeremiah 42 in the IRVM

Jeremiah 42 in the IRVM2

Jeremiah 42 in the IRVO

Jeremiah 42 in the IRVP

Jeremiah 42 in the IRVT

Jeremiah 42 in the IRVT2

Jeremiah 42 in the IRVU

Jeremiah 42 in the ISVN

Jeremiah 42 in the JSNT

Jeremiah 42 in the KAPI

Jeremiah 42 in the KBT1ETNIK

Jeremiah 42 in the KBV

Jeremiah 42 in the KJV

Jeremiah 42 in the KNFD

Jeremiah 42 in the LBA

Jeremiah 42 in the LBLA

Jeremiah 42 in the LNT

Jeremiah 42 in the LSV

Jeremiah 42 in the MAAL

Jeremiah 42 in the MBV

Jeremiah 42 in the MBV2

Jeremiah 42 in the MHNT

Jeremiah 42 in the MKNFD

Jeremiah 42 in the MNG

Jeremiah 42 in the MNT

Jeremiah 42 in the MNT2

Jeremiah 42 in the MRS1T

Jeremiah 42 in the NAA

Jeremiah 42 in the NASB

Jeremiah 42 in the NBLA

Jeremiah 42 in the NBS

Jeremiah 42 in the NBVTP

Jeremiah 42 in the NET2

Jeremiah 42 in the NIV11

Jeremiah 42 in the NNT

Jeremiah 42 in the NNT2

Jeremiah 42 in the NNT3

Jeremiah 42 in the PDDPT

Jeremiah 42 in the PFNT

Jeremiah 42 in the RMNT

Jeremiah 42 in the SBIAS

Jeremiah 42 in the SBIBS

Jeremiah 42 in the SBIBS2

Jeremiah 42 in the SBICS

Jeremiah 42 in the SBIDS

Jeremiah 42 in the SBIGS

Jeremiah 42 in the SBIHS

Jeremiah 42 in the SBIIS

Jeremiah 42 in the SBIIS2

Jeremiah 42 in the SBIIS3

Jeremiah 42 in the SBIKS

Jeremiah 42 in the SBIKS2

Jeremiah 42 in the SBIMS

Jeremiah 42 in the SBIOS

Jeremiah 42 in the SBIPS

Jeremiah 42 in the SBISS

Jeremiah 42 in the SBITS

Jeremiah 42 in the SBITS2

Jeremiah 42 in the SBITS3

Jeremiah 42 in the SBITS4

Jeremiah 42 in the SBIUS

Jeremiah 42 in the SBIVS

Jeremiah 42 in the SBT

Jeremiah 42 in the SBT1E

Jeremiah 42 in the SCHL

Jeremiah 42 in the SNT

Jeremiah 42 in the SUSU

Jeremiah 42 in the SUSU2

Jeremiah 42 in the SYNO

Jeremiah 42 in the TBIAOTANT

Jeremiah 42 in the TBT1E

Jeremiah 42 in the TBT1E2

Jeremiah 42 in the TFTIP

Jeremiah 42 in the TFTU

Jeremiah 42 in the TGNTATF3T

Jeremiah 42 in the THAI

Jeremiah 42 in the TNFD

Jeremiah 42 in the TNT

Jeremiah 42 in the TNTIK

Jeremiah 42 in the TNTIL

Jeremiah 42 in the TNTIN

Jeremiah 42 in the TNTIP

Jeremiah 42 in the TNTIZ

Jeremiah 42 in the TOMA

Jeremiah 42 in the TTENT

Jeremiah 42 in the UBG

Jeremiah 42 in the UGV

Jeremiah 42 in the UGV2

Jeremiah 42 in the UGV3

Jeremiah 42 in the VBL

Jeremiah 42 in the VDCC

Jeremiah 42 in the YALU

Jeremiah 42 in the YAPE

Jeremiah 42 in the YBVTP

Jeremiah 42 in the ZBP