Leviticus 5 (BOGWICC)

1 “ ‘Ngati munthu anayitanidwa ku bwalo kuti akachitire umboni pa zimene anaziona kapena kuzimva koma iye nʼkukana kuchitira umboni, munthu ameneyo wachimwa ndipo ayenera kulangidwa. 2 “ ‘Munthu akakhudza chinthu chilichonse chodetsedwa, monga nyama yakufa ya mʼthengo, kapena chiweto chakufa kapenanso chokwawa chakufa, ngakhale iyeyo wachikhudza mosadziwa, wasanduka wodetsedwa ndipo wachimwa. 3 “ ‘Munthu akakhudza choyipitsa munthu cha mtundu uliwonse, ndipo pochikhudzapo ndi kuyipitsidwa nacho mosadziwa, munthuyo adzakhala wopalamula akangodziwa chimene wachitacho. 4 “ ‘Munthu akalumbira mofulumira kapena mosasamala kuti adzachita chinthu, choyipa kapena chabwino, ngakhale kuti wachita izi mosadziwa kuti nʼkulakwa, pamene wazindira kulakwa kwake, iye adzakhalabe wopalamula akangodziwa chimene wachitacho. 5 “ ‘Pamene munthu wazindikira kuti wachimwa motere, awulule tchimo limene wachitalo. 6 Pambuyo pake, munthuyo abwere kwa Yehova ndi mwana wankhosa wamkazi kapena mbuzi kuti ikhale chopereka chopepesera tchimo ndipo wansembe achite mwambo wopepesera tchimo lomwe wachitalo. Tsono wansembe achite mwambo wopepesera tchimo la munthuyo. 7 “ ‘Ngati munthuyo alibe mwana wankhosa, abweretse njiwa ziwiri kapena nkhunda ziwiri kwa Yehova ngati chopereka chopepesera tchimo lake. Imodzi ikhale nsembe yopepesera tchimo, ndipo inayo ikhale nsembe yopsereza. 8 Tsono abwere nazo kwa wansembe, ndipo wansembeyo ayambe wapereka mbalame imodzi ngati yopepesera tchimo. Apotole khosi koma osayidula mutu, 9 kenaka awaze magazi a chopereka chopepesera tchimocho mʼmbali mwa guwa. Magazi ena onse awathire pa tsinde la guwa. Imeneyi ndi nsembe yopepesera tchimo. 10 Pambuyo pake wansembe apereke mbalame inayo kuti ikhale chopereka chopsereza potsata mwambo wake. Wansembe atatha kupereka nsembe yopepesera tchimo limene munthu uja wachita, wochimwayo adzakhululukidwa. 11 “ ‘Koma ngati munthuyo alibe njiwa ziwiri kapena nkhunda ziwiri, abweretse ufa wosalala wokwanira kilogalamu imodzi kuti ukhale chopereka chopepesera tchimo limene wachita. Asathiremo mafuta kapena lubani chifukwa ndi chopereka chopepesera tchimo. 12 Abweretse ufawo kwa wansembe ndipo wansembeyo atapeko dzanja limodzi kuti ukhale ufa wachikumbutso ndi kuwutentha pa guwa pamodzi ndi chopereka chopsereza kwa Yehova. Imeneyi ndi nsembe yopepesera tchimo. 13 Umu ndi mmene wansembe adzachitire mwambo wopepesera machimo ena aliwonse amene munthu wachita, ndipo munthuyo adzakhululukidwa. Zopereka zonse zotsala zidzakhala za wansembeyo monga momwe amachitira ndi chopereka chachakudya.’ ” 14 Yehova anawuza Mose kuti, 15 “Munthu akachita zinthu mosakhulupirika, nachimwa mosadziwa posapereka zinthu zopatulika zofunika kwa Yehova, munthuyo apereke kwa Yehova nsembe yopepesera machimo ake. Nsembeyo ikhale nkhosa yayimuna yopanda chilema ndipo mtengo wake ukhale wokwana masekeli oyenera a siliva pakawerengedwe ka ku Nyumba ya Mulungu. Imeneyi ndi nsembe yopepesera kupalamula. 16 Munthuyo ayenera kubweza zinthu zopatulika zimene sanaperekezo. Awonjezepo chimodzi mwa zigawo zisanu zilizonse ndi kuzipereka zonsezo kwa wansembe amene adzachita mwambo wopepesera machimo a munthuyo, popereka nkhosa yayimuna ija ngati nsembe yopepesera ndipo wochimwayo adzakhululukidwa. 17 “Ngati munthu wachimwa mosadziwa pochita chilichonse chimene Yehova salola, munthuyo ndi wopalamula ndithu, ndipo ayenera kulangidwa. 18 Abwere kwa wansembe ndi chopereka chopepesera kupalamula kwake. Chopereka chikhale nkhosa yayimuna yopanda chilema ndipo mtengo wake ukhale woyenera nsembe yopepesera kupalamula kumene anachimwa mosadziwako, ndipo munthuyo adzakhululukidwa. 19 Imeneyi ndi nsembe yopepesera kupalamula popeza munthuyo wapezeka wolakwa pamaso pa Yehova.”

In Other Versions

Leviticus 5 in the ANGEFD

Leviticus 5 in the ANTPNG2D

Leviticus 5 in the AS21

Leviticus 5 in the BAGH

Leviticus 5 in the BBPNG

Leviticus 5 in the BBT1E

Leviticus 5 in the BDS

Leviticus 5 in the BEV

Leviticus 5 in the BHAD

Leviticus 5 in the BIB

Leviticus 5 in the BLPT

Leviticus 5 in the BNT

Leviticus 5 in the BNTABOOT

Leviticus 5 in the BNTLV

Leviticus 5 in the BOATCB

Leviticus 5 in the BOATCB2

Leviticus 5 in the BOBCV

Leviticus 5 in the BOCNT

Leviticus 5 in the BOECS

Leviticus 5 in the BOHCB

Leviticus 5 in the BOHCV

Leviticus 5 in the BOHLNT

Leviticus 5 in the BOHNTLTAL

Leviticus 5 in the BOICB

Leviticus 5 in the BOILNTAP

Leviticus 5 in the BOITCV

Leviticus 5 in the BOKCV

Leviticus 5 in the BOKCV2

Leviticus 5 in the BOKHWOG

Leviticus 5 in the BOKSSV

Leviticus 5 in the BOLCB

Leviticus 5 in the BOLCB2

Leviticus 5 in the BOMCV

Leviticus 5 in the BONAV

Leviticus 5 in the BONCB

Leviticus 5 in the BONLT

Leviticus 5 in the BONUT2

Leviticus 5 in the BOPLNT

Leviticus 5 in the BOSCB

Leviticus 5 in the BOSNC

Leviticus 5 in the BOTLNT

Leviticus 5 in the BOVCB

Leviticus 5 in the BOYCB

Leviticus 5 in the BPBB

Leviticus 5 in the BPH

Leviticus 5 in the BSB

Leviticus 5 in the CCB

Leviticus 5 in the CUV

Leviticus 5 in the CUVS

Leviticus 5 in the DBT

Leviticus 5 in the DGDNT

Leviticus 5 in the DHNT

Leviticus 5 in the DNT

Leviticus 5 in the ELBE

Leviticus 5 in the EMTV

Leviticus 5 in the ESV

Leviticus 5 in the FBV

Leviticus 5 in the FEB

Leviticus 5 in the GGMNT

Leviticus 5 in the GNT

Leviticus 5 in the HARY

Leviticus 5 in the HNT

Leviticus 5 in the IRVA

Leviticus 5 in the IRVB

Leviticus 5 in the IRVG

Leviticus 5 in the IRVH

Leviticus 5 in the IRVK

Leviticus 5 in the IRVM

Leviticus 5 in the IRVM2

Leviticus 5 in the IRVO

Leviticus 5 in the IRVP

Leviticus 5 in the IRVT

Leviticus 5 in the IRVT2

Leviticus 5 in the IRVU

Leviticus 5 in the ISVN

Leviticus 5 in the JSNT

Leviticus 5 in the KAPI

Leviticus 5 in the KBT1ETNIK

Leviticus 5 in the KBV

Leviticus 5 in the KJV

Leviticus 5 in the KNFD

Leviticus 5 in the LBA

Leviticus 5 in the LBLA

Leviticus 5 in the LNT

Leviticus 5 in the LSV

Leviticus 5 in the MAAL

Leviticus 5 in the MBV

Leviticus 5 in the MBV2

Leviticus 5 in the MHNT

Leviticus 5 in the MKNFD

Leviticus 5 in the MNG

Leviticus 5 in the MNT

Leviticus 5 in the MNT2

Leviticus 5 in the MRS1T

Leviticus 5 in the NAA

Leviticus 5 in the NASB

Leviticus 5 in the NBLA

Leviticus 5 in the NBS

Leviticus 5 in the NBVTP

Leviticus 5 in the NET2

Leviticus 5 in the NIV11

Leviticus 5 in the NNT

Leviticus 5 in the NNT2

Leviticus 5 in the NNT3

Leviticus 5 in the PDDPT

Leviticus 5 in the PFNT

Leviticus 5 in the RMNT

Leviticus 5 in the SBIAS

Leviticus 5 in the SBIBS

Leviticus 5 in the SBIBS2

Leviticus 5 in the SBICS

Leviticus 5 in the SBIDS

Leviticus 5 in the SBIGS

Leviticus 5 in the SBIHS

Leviticus 5 in the SBIIS

Leviticus 5 in the SBIIS2

Leviticus 5 in the SBIIS3

Leviticus 5 in the SBIKS

Leviticus 5 in the SBIKS2

Leviticus 5 in the SBIMS

Leviticus 5 in the SBIOS

Leviticus 5 in the SBIPS

Leviticus 5 in the SBISS

Leviticus 5 in the SBITS

Leviticus 5 in the SBITS2

Leviticus 5 in the SBITS3

Leviticus 5 in the SBITS4

Leviticus 5 in the SBIUS

Leviticus 5 in the SBIVS

Leviticus 5 in the SBT

Leviticus 5 in the SBT1E

Leviticus 5 in the SCHL

Leviticus 5 in the SNT

Leviticus 5 in the SUSU

Leviticus 5 in the SUSU2

Leviticus 5 in the SYNO

Leviticus 5 in the TBIAOTANT

Leviticus 5 in the TBT1E

Leviticus 5 in the TBT1E2

Leviticus 5 in the TFTIP

Leviticus 5 in the TFTU

Leviticus 5 in the TGNTATF3T

Leviticus 5 in the THAI

Leviticus 5 in the TNFD

Leviticus 5 in the TNT

Leviticus 5 in the TNTIK

Leviticus 5 in the TNTIL

Leviticus 5 in the TNTIN

Leviticus 5 in the TNTIP

Leviticus 5 in the TNTIZ

Leviticus 5 in the TOMA

Leviticus 5 in the TTENT

Leviticus 5 in the UBG

Leviticus 5 in the UGV

Leviticus 5 in the UGV2

Leviticus 5 in the UGV3

Leviticus 5 in the VBL

Leviticus 5 in the VDCC

Leviticus 5 in the YALU

Leviticus 5 in the YAPE

Leviticus 5 in the YBVTP

Leviticus 5 in the ZBP