Ecclesiastes 3 (BOGWICC)

1 Chinthu chilichonse chili ndi nthawi yake,ndi nyengo yake yomwe anayika Mulungu: 2 Nthawi yobadwa ndi nthawi yomwalira,nthawi yodzala ndi nthawi yokolola. 3 Nthawi yakupha ndi nthawi yochiritsa,nthawi yogwetsa ndi nthawi yomanga. 4 Nthawi yomva chisoni ndi nthawi yosangalala,nthawi yolira maliro ndi nthawi yovina. 5 Nthawi yotaya miyala ndi nthawi yokundika miyala,nthawi yokumbatirana ndi nthawi yoleka kukumbatirana. 6 Nthawi yofunafuna ndi nthawi yoleka kufunafuna,nthawi yosunga ndi nthawi yotaya. 7 Nthawi yongʼamba ndi nthawi yosoka,nthawi yokhala chete ndi nthawi yoyankhula. 8 Nthawi yokondana ndi nthawi yodana,nthawi ya nkhondo ndi nthawi ya mtendere. 9 Kodi wantchito amapeza phindu lanji pa ntchito yake yolemetsa? 10 Ine ndinaona chipsinjo chimene Mulungu anayika pa anthu. 11 Iye anapanga chinthu chilichonse kuti chikhale chabwino pa nthawi yake. Anayika nzeru zamuyaya mʼmitima ya anthu; komabe anthuwo sangathe kuzindikira zomwe Mulungu wachita kuyambira pa chiyambi mpaka chimaliziro. 12 Ine ndikudziwa kuti palibenso kanthu kabwino kwa anthu kopambana kusangalala ndi kuchita zabwino pamene ali ndi moyo. 13 Ndi mphatso ya Mulungu kwa munthu kuti azidya, azimwa ndi kumakondwera ndi ntchito zake zolemetsa. 14 Ndikudziwa kuti chilichonse chimene Mulungu amachita chidzakhala mpaka muyaya; palibe zimene zingawonjezedwe kapena kuchotsedwa. Mulungu amazichita kuti anthu azimuopa. 15 Chilichonse chimene chilipo chinalipo kale,ndipo chimene chidzakhalapo chinalipo poyamba;Mulungu amabwezanso zakale zimene zinapita kuti zichitikenso. 16 Ndipo ndinaona chinthu chinanso pansi pano:ku malo achiweruzo, kuyipa mtima kuli komweko,ku malo achilungamo, kuyipa mtima kuli komweko. 17 Ndinalingalira mu mtima mwanga kuti;“Mulungu adzaweruzaolungama pamodzi ndi oyipa omwe,pakuti anayika nthawi yochitikira chinthu chilichonse,nthawi ya ntchito iliyonse.” 18 Ndinalingaliranso kuti, “Kunena za anthu, Mulungu amawayesa ndi cholinga choti awaonetse kuti iwo ali ngati nyama. 19 Zimene zimachitikira munthu, zomwezonso zimachitikira nyama; chinthu chimodzi chomwecho chimachitikira onse: Monga munthu amafa momwemonso nyama imafa. Zonsezi zimapuma mpweya umodzimodzi omwewo; munthu saposa nyama. Zonsezi ndi zopandapake. 20 Zonse zimapita kumodzimodzi; zonsezi zimachokera ku fumbi, ndipo zimabwereranso ku fumbi komweko. 21 Kodi ndani amene amadziwa ngati mzimu wa munthu umakwera kumwamba, ndipo mzimu wa nyama umatsikira kunsi kwa dziko?” 22 Kotero ndinaona kuti palibe chinthu chabwino kwa munthu kuposa kuti munthu azisangalala ndi ntchito yake, pakuti ichi ndiye chake chenicheni. Pakuti ndani amene angamubweretse kuti adzaone zimene zidzamuchitikira iye akadzamwalira?

In Other Versions

Ecclesiastes 3 in the ANGEFD

Ecclesiastes 3 in the ANTPNG2D

Ecclesiastes 3 in the AS21

Ecclesiastes 3 in the BAGH

Ecclesiastes 3 in the BBPNG

Ecclesiastes 3 in the BBT1E

Ecclesiastes 3 in the BDS

Ecclesiastes 3 in the BEV

Ecclesiastes 3 in the BHAD

Ecclesiastes 3 in the BIB

Ecclesiastes 3 in the BLPT

Ecclesiastes 3 in the BNT

Ecclesiastes 3 in the BNTABOOT

Ecclesiastes 3 in the BNTLV

Ecclesiastes 3 in the BOATCB

Ecclesiastes 3 in the BOATCB2

Ecclesiastes 3 in the BOBCV

Ecclesiastes 3 in the BOCNT

Ecclesiastes 3 in the BOECS

Ecclesiastes 3 in the BOHCB

Ecclesiastes 3 in the BOHCV

Ecclesiastes 3 in the BOHLNT

Ecclesiastes 3 in the BOHNTLTAL

Ecclesiastes 3 in the BOICB

Ecclesiastes 3 in the BOILNTAP

Ecclesiastes 3 in the BOITCV

Ecclesiastes 3 in the BOKCV

Ecclesiastes 3 in the BOKCV2

Ecclesiastes 3 in the BOKHWOG

Ecclesiastes 3 in the BOKSSV

Ecclesiastes 3 in the BOLCB

Ecclesiastes 3 in the BOLCB2

Ecclesiastes 3 in the BOMCV

Ecclesiastes 3 in the BONAV

Ecclesiastes 3 in the BONCB

Ecclesiastes 3 in the BONLT

Ecclesiastes 3 in the BONUT2

Ecclesiastes 3 in the BOPLNT

Ecclesiastes 3 in the BOSCB

Ecclesiastes 3 in the BOSNC

Ecclesiastes 3 in the BOTLNT

Ecclesiastes 3 in the BOVCB

Ecclesiastes 3 in the BOYCB

Ecclesiastes 3 in the BPBB

Ecclesiastes 3 in the BPH

Ecclesiastes 3 in the BSB

Ecclesiastes 3 in the CCB

Ecclesiastes 3 in the CUV

Ecclesiastes 3 in the CUVS

Ecclesiastes 3 in the DBT

Ecclesiastes 3 in the DGDNT

Ecclesiastes 3 in the DHNT

Ecclesiastes 3 in the DNT

Ecclesiastes 3 in the ELBE

Ecclesiastes 3 in the EMTV

Ecclesiastes 3 in the ESV

Ecclesiastes 3 in the FBV

Ecclesiastes 3 in the FEB

Ecclesiastes 3 in the GGMNT

Ecclesiastes 3 in the GNT

Ecclesiastes 3 in the HARY

Ecclesiastes 3 in the HNT

Ecclesiastes 3 in the IRVA

Ecclesiastes 3 in the IRVB

Ecclesiastes 3 in the IRVG

Ecclesiastes 3 in the IRVH

Ecclesiastes 3 in the IRVK

Ecclesiastes 3 in the IRVM

Ecclesiastes 3 in the IRVM2

Ecclesiastes 3 in the IRVO

Ecclesiastes 3 in the IRVP

Ecclesiastes 3 in the IRVT

Ecclesiastes 3 in the IRVT2

Ecclesiastes 3 in the IRVU

Ecclesiastes 3 in the ISVN

Ecclesiastes 3 in the JSNT

Ecclesiastes 3 in the KAPI

Ecclesiastes 3 in the KBT1ETNIK

Ecclesiastes 3 in the KBV

Ecclesiastes 3 in the KJV

Ecclesiastes 3 in the KNFD

Ecclesiastes 3 in the LBA

Ecclesiastes 3 in the LBLA

Ecclesiastes 3 in the LNT

Ecclesiastes 3 in the LSV

Ecclesiastes 3 in the MAAL

Ecclesiastes 3 in the MBV

Ecclesiastes 3 in the MBV2

Ecclesiastes 3 in the MHNT

Ecclesiastes 3 in the MKNFD

Ecclesiastes 3 in the MNG

Ecclesiastes 3 in the MNT

Ecclesiastes 3 in the MNT2

Ecclesiastes 3 in the MRS1T

Ecclesiastes 3 in the NAA

Ecclesiastes 3 in the NASB

Ecclesiastes 3 in the NBLA

Ecclesiastes 3 in the NBS

Ecclesiastes 3 in the NBVTP

Ecclesiastes 3 in the NET2

Ecclesiastes 3 in the NIV11

Ecclesiastes 3 in the NNT

Ecclesiastes 3 in the NNT2

Ecclesiastes 3 in the NNT3

Ecclesiastes 3 in the PDDPT

Ecclesiastes 3 in the PFNT

Ecclesiastes 3 in the RMNT

Ecclesiastes 3 in the SBIAS

Ecclesiastes 3 in the SBIBS

Ecclesiastes 3 in the SBIBS2

Ecclesiastes 3 in the SBICS

Ecclesiastes 3 in the SBIDS

Ecclesiastes 3 in the SBIGS

Ecclesiastes 3 in the SBIHS

Ecclesiastes 3 in the SBIIS

Ecclesiastes 3 in the SBIIS2

Ecclesiastes 3 in the SBIIS3

Ecclesiastes 3 in the SBIKS

Ecclesiastes 3 in the SBIKS2

Ecclesiastes 3 in the SBIMS

Ecclesiastes 3 in the SBIOS

Ecclesiastes 3 in the SBIPS

Ecclesiastes 3 in the SBISS

Ecclesiastes 3 in the SBITS

Ecclesiastes 3 in the SBITS2

Ecclesiastes 3 in the SBITS3

Ecclesiastes 3 in the SBITS4

Ecclesiastes 3 in the SBIUS

Ecclesiastes 3 in the SBIVS

Ecclesiastes 3 in the SBT

Ecclesiastes 3 in the SBT1E

Ecclesiastes 3 in the SCHL

Ecclesiastes 3 in the SNT

Ecclesiastes 3 in the SUSU

Ecclesiastes 3 in the SUSU2

Ecclesiastes 3 in the SYNO

Ecclesiastes 3 in the TBIAOTANT

Ecclesiastes 3 in the TBT1E

Ecclesiastes 3 in the TBT1E2

Ecclesiastes 3 in the TFTIP

Ecclesiastes 3 in the TFTU

Ecclesiastes 3 in the TGNTATF3T

Ecclesiastes 3 in the THAI

Ecclesiastes 3 in the TNFD

Ecclesiastes 3 in the TNT

Ecclesiastes 3 in the TNTIK

Ecclesiastes 3 in the TNTIL

Ecclesiastes 3 in the TNTIN

Ecclesiastes 3 in the TNTIP

Ecclesiastes 3 in the TNTIZ

Ecclesiastes 3 in the TOMA

Ecclesiastes 3 in the TTENT

Ecclesiastes 3 in the UBG

Ecclesiastes 3 in the UGV

Ecclesiastes 3 in the UGV2

Ecclesiastes 3 in the UGV3

Ecclesiastes 3 in the VBL

Ecclesiastes 3 in the VDCC

Ecclesiastes 3 in the YALU

Ecclesiastes 3 in the YAPE

Ecclesiastes 3 in the YBVTP

Ecclesiastes 3 in the ZBP