Ezekiel 8 (BOGWICC)

1 Tsiku lachisanu la mwezi wachisanu ndi chimodzi, mʼchaka chachisanu ndi chimodzi, ndinakhala mʼnyumba mwanga pamodzi ndi akuluakulu a ku Yuda. Tsono mphamvu za Ambuye Yehova zinandifikira. 2 Nditayangʼana ndinangoona chinthu chooneka ngati munthu. Kuchokera pamene pamaoneka ngati chiwuno chake kumatsika mʼmunsi anali ngati moto, ndipo kuchokera mʼchiwuno kukwera mmwamba amaoneka mowala ngati mkuwa wonyezimira. 3 Iye anatambasula chinthu chooneka ngati dzanja ndipo anagwira tsitsi la pamutu panga. Nthawi yomweyo Mzimu unandikweza mlengalenga. Tsono ndikumachita ngati ndikuona Mulungu kutulo, Mzimu uja unapita nane ku Yerusalemu nundiyika pa khomo la chipata chamʼkati choyangʼana kumpoto. Kumeneko kunali fano limene limaputa mkwiyo wa Mulungu. 4 Kumeneko ndinaona ulemerero wa Mulungu wa Israeli ngati momwe ndinaonera mʼmasomphenya mʼchigwa muja. 5 Tsono Yehova anandiwuza kuti, “Iwe mwana wa munthu, tayangʼana kumpoto.” Choncho ndinayangʼana kumpoto ndipo ndinaona pa khomo la chipata pafupi ndi guwa lansembe ndinaona fano loputa mkwiyo wa Mulungu lija. 6 Ndipo Yehova anandifunsa kuti, “Iwe mwana wa munthu, kodi ukuona zimene akuchitazi, zonyansa zazikulu zimene Aisraeli akuchita kuno, zinthu zondichotsa Ine kumalo anga opatulika? Koma iwe udzaona zinthu zimene zili zonyansa kwambiri.” 7 Kenaka Iye anandipititsa ku khomo lolowera ku bwalo la Nyumba ya Mulungu. Nditayangʼanitsitsa ndinangoona dzenje pa khomapo. 8 Yehova anandiwuza kuti, “Iwe mwana wa munthu, tsopano bowola pa khomapo.” Ndinabowoladi pa khomapo ndipo ndinapezapo khomo. 9 Ndipo Yehova anandiwuza kuti, “Lowa, ndipo ona zinthu zonyansa zimene akuchita pamenepa.” 10 Motero Ine ndinalowa ndi kuyangʼana, ndipo ndinaona pa makoma onse zithunzi za zinthu zosiyanasiyana zokwawa pansi, za nyama zonyansa ndiponso za mafano onse amene Aisraeli ankapembedza. 11 Patsogolo pa zimenezi panayima akuluakulu makumi asanu ndi awiri a Aisraeli, ndipo Yaazaniya mwana wa Safani anali atayima pakati pawo. Aliyense wa iwo anali ndi chofukizira lubani mʼdzanja lake ndipo utsi wa fungo lokoma la lubani unkafuka. 12 Tsono Yehova anandifunsa kuti, “Iwe mwana wa munthu, kodi waona zimene akuluakulu a Aisraeli akuchita mu mdima, aliyense akupembedza fano lakelake mʼnyumbamo? Iwo akuti, ‘Yehova sakutiona; Yehova walisiya dziko!’ 13 Iye anandiwuzanso kuti, ‘Iwe udzawaonanso akuchita zinthu zonyansa kwambiri.’ ” 14 Kenaka anapita nane pa khomo la ku khomo la chipata cha Nyumba ya Mulungu choyangʼana kumpoto, ndipo kumeneko ndinaona akazi ena atakhala pansi, akulira mulungu wawo wotchedwa Tamuzi. 15 Yehova anandifunsa kuti, “Iwe mwana wa munthu, kodi ukuziona zimenezi? Iwe udzaona zinthu zimene zili zonyansa kwambiri kuposa izi.” 16 Kenaka Iye anapita nane mʼkati mwa bwalo la Nyumba ya Yehova. Kumeneko ku khomo lolowera ku Nyumba ya Yehova pakati pa khonde ndi guwa lansembe, panali amuna 25. Anafulatira Nyumba ya Mulungu wa Yehova ndipo nkhope zawo zinaloza kummawa, ndipo ankapembedza dzuwa choyangʼana kummawa. 17 Yehova anandifunsa kuti, “Iwe mwana wa munthu, kodi waziona zimenezi? Kodi nʼchinthu chopepuka kuti anthu a ku Yuda azichita zonyansa zimene akuchitazi pano? Kodi afike mpaka pomafalitsa za ndewu mʼdziko lonse? Iwotu akuwutsa ukali wanga. Akundipsetsa mtima ndi zochita zawo! 18 Choncho Ine ndidzawalanga ndili wokwiya. Sindidzawamvera chisoni kapena kuwaleka. Ngakhale atandifuwulira mʼmakutu mwanga sindidzawamvera.”

In Other Versions

Ezekiel 8 in the ANGEFD

Ezekiel 8 in the ANTPNG2D

Ezekiel 8 in the AS21

Ezekiel 8 in the BAGH

Ezekiel 8 in the BBPNG

Ezekiel 8 in the BBT1E

Ezekiel 8 in the BDS

Ezekiel 8 in the BEV

Ezekiel 8 in the BHAD

Ezekiel 8 in the BIB

Ezekiel 8 in the BLPT

Ezekiel 8 in the BNT

Ezekiel 8 in the BNTABOOT

Ezekiel 8 in the BNTLV

Ezekiel 8 in the BOATCB

Ezekiel 8 in the BOATCB2

Ezekiel 8 in the BOBCV

Ezekiel 8 in the BOCNT

Ezekiel 8 in the BOECS

Ezekiel 8 in the BOHCB

Ezekiel 8 in the BOHCV

Ezekiel 8 in the BOHLNT

Ezekiel 8 in the BOHNTLTAL

Ezekiel 8 in the BOICB

Ezekiel 8 in the BOILNTAP

Ezekiel 8 in the BOITCV

Ezekiel 8 in the BOKCV

Ezekiel 8 in the BOKCV2

Ezekiel 8 in the BOKHWOG

Ezekiel 8 in the BOKSSV

Ezekiel 8 in the BOLCB

Ezekiel 8 in the BOLCB2

Ezekiel 8 in the BOMCV

Ezekiel 8 in the BONAV

Ezekiel 8 in the BONCB

Ezekiel 8 in the BONLT

Ezekiel 8 in the BONUT2

Ezekiel 8 in the BOPLNT

Ezekiel 8 in the BOSCB

Ezekiel 8 in the BOSNC

Ezekiel 8 in the BOTLNT

Ezekiel 8 in the BOVCB

Ezekiel 8 in the BOYCB

Ezekiel 8 in the BPBB

Ezekiel 8 in the BPH

Ezekiel 8 in the BSB

Ezekiel 8 in the CCB

Ezekiel 8 in the CUV

Ezekiel 8 in the CUVS

Ezekiel 8 in the DBT

Ezekiel 8 in the DGDNT

Ezekiel 8 in the DHNT

Ezekiel 8 in the DNT

Ezekiel 8 in the ELBE

Ezekiel 8 in the EMTV

Ezekiel 8 in the ESV

Ezekiel 8 in the FBV

Ezekiel 8 in the FEB

Ezekiel 8 in the GGMNT

Ezekiel 8 in the GNT

Ezekiel 8 in the HARY

Ezekiel 8 in the HNT

Ezekiel 8 in the IRVA

Ezekiel 8 in the IRVB

Ezekiel 8 in the IRVG

Ezekiel 8 in the IRVH

Ezekiel 8 in the IRVK

Ezekiel 8 in the IRVM

Ezekiel 8 in the IRVM2

Ezekiel 8 in the IRVO

Ezekiel 8 in the IRVP

Ezekiel 8 in the IRVT

Ezekiel 8 in the IRVT2

Ezekiel 8 in the IRVU

Ezekiel 8 in the ISVN

Ezekiel 8 in the JSNT

Ezekiel 8 in the KAPI

Ezekiel 8 in the KBT1ETNIK

Ezekiel 8 in the KBV

Ezekiel 8 in the KJV

Ezekiel 8 in the KNFD

Ezekiel 8 in the LBA

Ezekiel 8 in the LBLA

Ezekiel 8 in the LNT

Ezekiel 8 in the LSV

Ezekiel 8 in the MAAL

Ezekiel 8 in the MBV

Ezekiel 8 in the MBV2

Ezekiel 8 in the MHNT

Ezekiel 8 in the MKNFD

Ezekiel 8 in the MNG

Ezekiel 8 in the MNT

Ezekiel 8 in the MNT2

Ezekiel 8 in the MRS1T

Ezekiel 8 in the NAA

Ezekiel 8 in the NASB

Ezekiel 8 in the NBLA

Ezekiel 8 in the NBS

Ezekiel 8 in the NBVTP

Ezekiel 8 in the NET2

Ezekiel 8 in the NIV11

Ezekiel 8 in the NNT

Ezekiel 8 in the NNT2

Ezekiel 8 in the NNT3

Ezekiel 8 in the PDDPT

Ezekiel 8 in the PFNT

Ezekiel 8 in the RMNT

Ezekiel 8 in the SBIAS

Ezekiel 8 in the SBIBS

Ezekiel 8 in the SBIBS2

Ezekiel 8 in the SBICS

Ezekiel 8 in the SBIDS

Ezekiel 8 in the SBIGS

Ezekiel 8 in the SBIHS

Ezekiel 8 in the SBIIS

Ezekiel 8 in the SBIIS2

Ezekiel 8 in the SBIIS3

Ezekiel 8 in the SBIKS

Ezekiel 8 in the SBIKS2

Ezekiel 8 in the SBIMS

Ezekiel 8 in the SBIOS

Ezekiel 8 in the SBIPS

Ezekiel 8 in the SBISS

Ezekiel 8 in the SBITS

Ezekiel 8 in the SBITS2

Ezekiel 8 in the SBITS3

Ezekiel 8 in the SBITS4

Ezekiel 8 in the SBIUS

Ezekiel 8 in the SBIVS

Ezekiel 8 in the SBT

Ezekiel 8 in the SBT1E

Ezekiel 8 in the SCHL

Ezekiel 8 in the SNT

Ezekiel 8 in the SUSU

Ezekiel 8 in the SUSU2

Ezekiel 8 in the SYNO

Ezekiel 8 in the TBIAOTANT

Ezekiel 8 in the TBT1E

Ezekiel 8 in the TBT1E2

Ezekiel 8 in the TFTIP

Ezekiel 8 in the TFTU

Ezekiel 8 in the TGNTATF3T

Ezekiel 8 in the THAI

Ezekiel 8 in the TNFD

Ezekiel 8 in the TNT

Ezekiel 8 in the TNTIK

Ezekiel 8 in the TNTIL

Ezekiel 8 in the TNTIN

Ezekiel 8 in the TNTIP

Ezekiel 8 in the TNTIZ

Ezekiel 8 in the TOMA

Ezekiel 8 in the TTENT

Ezekiel 8 in the UBG

Ezekiel 8 in the UGV

Ezekiel 8 in the UGV2

Ezekiel 8 in the UGV3

Ezekiel 8 in the VBL

Ezekiel 8 in the VDCC

Ezekiel 8 in the YALU

Ezekiel 8 in the YAPE

Ezekiel 8 in the YBVTP

Ezekiel 8 in the ZBP