Genesis 9 (BOGWICC)

1 Ndipo Mulungu anadalitsa Nowa ndi ana ake aamuna nati kwa iwo, “Berekanani ndipo muchulukane ndi kudzaza dziko lapansi. 2 Nyama zonse za dziko lapansi, ndi mbalame zonse za mlengalenga, ndi chamoyo chilichonse chokwawa, ndiponso nsomba zonse za ku nyanja; zidzakuopani ndipo ndazipereka kuti muzilamulire. 3 Tsopano chamoyo chilichonse chidzakhala chakudya chanu. Monga momwe ndinakupatsirani ndiwo zamasamba, tsopano ndikupatsaninso nyama iliyonse. 4 “Koma musamadye nyama imene ikanali ndi magazi oyenda. 5 Aliyense wopha munthu adzaphedwa, nyama iliyonse yopha munthu idzaphedwa, munthu aliyense wopha munthu mnzake, adzaphedwa. 6 “Aliyense wopha munthu,adzaphedwanso ndi munthu;pakuti Mulungu analenga munthumʼchifanizo chake. 7 Inu muberekane ndi kuchulukana kuti mudzaze dziko lonse lapansi ndi kuligonjetsa.” 8 Mulungu anawuza Nowa ndi ana ake kuti, 9 “Tsopano Ine ndapangana ndi iwe ndi zidzukulu zako zamʼtsogolomo, 10 pamodzi ndi zamoyo zonse, mbalame, ziweto ndi nyama zonse za kuthengo, ndi zonse zimene zinatuluka mʼchombo pamodzi ndi iwe. 11 Pangano langa ndi ili: Ine ndilonjeza kuti sindidzawononganso zamoyo ndi madzi a chigumula. Chigumula sichidzawononganso dziko lapansi.” 12 Ndipo Mulungu anati, “Ine ndikupereka chizindikiro ichi cha pangano langa la pakati pa Ine ndi iwe, ana ako, zamoyo zonse, pamodzi ndi mibado ya mʼtsogolo. 13 Ndayika utawaleza wanga mʼmitambo, ndipo chidzakhala chizindikiro cha pangano langa ndi dziko lapansi. 14 Nthawi zonse pakakhala mitambo mu mlengalenga ndipo utawaleza uwoneka, 15 ndizikumbukira pangano langa pakati pa Ine ndi inu ndi zolengedwa zonse. Madzi sadzakhalanso chigumula chowononga dziko lapansi. 16 Utawaleza ukamadzaoneka mʼmitambo, ndidzawuona ndi kukumbukira pangano losatha pakati pa Mulungu ndi zamoyo zonse pa dziko lapansi.” 17 Choncho Mulungu anati kwa Nowa, “Ichi ndiye chizindikiro cha pangano limene ndalichita pakati pa Ine ndi zamoyo zonse pa dziko lapansi.” 18 Ana aamuna a Nowa amene anatuluka mʼchombo muja anali Semu, Hamu ndi Yafeti. Hamu anali abambo ake a Kanaani. 19 Ana aamuna a Nowa amenewa ndiwo anali makolo a anthu onse pa dziko lapansi. 20 Nowa anali munthu woyamba kulima munda wamphesa. 21 Tsiku lina pamene Nowa anamwako vinyo wa zipatso za mʼmundawo analedzera ndipo anavula zovala zake zonse ndi kugona mu tenti yake ali maliseche. 22 Hamu, abambo ake a Kanaani ataona kuti abambo ake ali maliseche anakawuza abale ake awiri aja omwe anali panja. 23 Koma Semu ndi Yafeti anatenga chofunda nachiyika pa mapewa awo; ndipo anayenda chamʼmbuyo naphimba umaliseche wa abambo awo. Anafulatira kuti asaone umaliseche wa abambo awo. 24 Nowa atadzuka, kuledzera kutatha, ndikudziwa zimene mwana wake wamngʼono wamwamuna uja anamuchitira, 25 anati,“Atembereredwe Kanaani!Adzakhala kapolowa pansi kwenikweni kwa abale ake.” 26 Anatinso,“Atamandike Yehova, Mulungu wa Semu!Kanaani akhale kapolo wa Semu. 27 Mulungu akulitse dziko la Yafeti;Yafeti alandire madalitso pamodzi ndi Semu,ndipo Kanaani akhale kapolo wawo.” 28 Chitatha chigumula, Nowa anakhala ndi moyo zaka 350. 29 Anamwalira ali ndi zaka 950.

In Other Versions

Genesis 9 in the ANGEFD

Genesis 9 in the ANTPNG2D

Genesis 9 in the AS21

Genesis 9 in the BAGH

Genesis 9 in the BBPNG

Genesis 9 in the BBT1E

Genesis 9 in the BDS

Genesis 9 in the BEV

Genesis 9 in the BHAD

Genesis 9 in the BIB

Genesis 9 in the BLPT

Genesis 9 in the BNT

Genesis 9 in the BNTABOOT

Genesis 9 in the BNTLV

Genesis 9 in the BOATCB

Genesis 9 in the BOATCB2

Genesis 9 in the BOBCV

Genesis 9 in the BOCNT

Genesis 9 in the BOECS

Genesis 9 in the BOHCB

Genesis 9 in the BOHCV

Genesis 9 in the BOHLNT

Genesis 9 in the BOHNTLTAL

Genesis 9 in the BOICB

Genesis 9 in the BOILNTAP

Genesis 9 in the BOITCV

Genesis 9 in the BOKCV

Genesis 9 in the BOKCV2

Genesis 9 in the BOKHWOG

Genesis 9 in the BOKSSV

Genesis 9 in the BOLCB

Genesis 9 in the BOLCB2

Genesis 9 in the BOMCV

Genesis 9 in the BONAV

Genesis 9 in the BONCB

Genesis 9 in the BONLT

Genesis 9 in the BONUT2

Genesis 9 in the BOPLNT

Genesis 9 in the BOSCB

Genesis 9 in the BOSNC

Genesis 9 in the BOTLNT

Genesis 9 in the BOVCB

Genesis 9 in the BOYCB

Genesis 9 in the BPBB

Genesis 9 in the BPH

Genesis 9 in the BSB

Genesis 9 in the CCB

Genesis 9 in the CUV

Genesis 9 in the CUVS

Genesis 9 in the DBT

Genesis 9 in the DGDNT

Genesis 9 in the DHNT

Genesis 9 in the DNT

Genesis 9 in the ELBE

Genesis 9 in the EMTV

Genesis 9 in the ESV

Genesis 9 in the FBV

Genesis 9 in the FEB

Genesis 9 in the GGMNT

Genesis 9 in the GNT

Genesis 9 in the HARY

Genesis 9 in the HNT

Genesis 9 in the IRVA

Genesis 9 in the IRVB

Genesis 9 in the IRVG

Genesis 9 in the IRVH

Genesis 9 in the IRVK

Genesis 9 in the IRVM

Genesis 9 in the IRVM2

Genesis 9 in the IRVO

Genesis 9 in the IRVP

Genesis 9 in the IRVT

Genesis 9 in the IRVT2

Genesis 9 in the IRVU

Genesis 9 in the ISVN

Genesis 9 in the JSNT

Genesis 9 in the KAPI

Genesis 9 in the KBT1ETNIK

Genesis 9 in the KBV

Genesis 9 in the KJV

Genesis 9 in the KNFD

Genesis 9 in the LBA

Genesis 9 in the LBLA

Genesis 9 in the LNT

Genesis 9 in the LSV

Genesis 9 in the MAAL

Genesis 9 in the MBV

Genesis 9 in the MBV2

Genesis 9 in the MHNT

Genesis 9 in the MKNFD

Genesis 9 in the MNG

Genesis 9 in the MNT

Genesis 9 in the MNT2

Genesis 9 in the MRS1T

Genesis 9 in the NAA

Genesis 9 in the NASB

Genesis 9 in the NBLA

Genesis 9 in the NBS

Genesis 9 in the NBVTP

Genesis 9 in the NET2

Genesis 9 in the NIV11

Genesis 9 in the NNT

Genesis 9 in the NNT2

Genesis 9 in the NNT3

Genesis 9 in the PDDPT

Genesis 9 in the PFNT

Genesis 9 in the RMNT

Genesis 9 in the SBIAS

Genesis 9 in the SBIBS

Genesis 9 in the SBIBS2

Genesis 9 in the SBICS

Genesis 9 in the SBIDS

Genesis 9 in the SBIGS

Genesis 9 in the SBIHS

Genesis 9 in the SBIIS

Genesis 9 in the SBIIS2

Genesis 9 in the SBIIS3

Genesis 9 in the SBIKS

Genesis 9 in the SBIKS2

Genesis 9 in the SBIMS

Genesis 9 in the SBIOS

Genesis 9 in the SBIPS

Genesis 9 in the SBISS

Genesis 9 in the SBITS

Genesis 9 in the SBITS2

Genesis 9 in the SBITS3

Genesis 9 in the SBITS4

Genesis 9 in the SBIUS

Genesis 9 in the SBIVS

Genesis 9 in the SBT

Genesis 9 in the SBT1E

Genesis 9 in the SCHL

Genesis 9 in the SNT

Genesis 9 in the SUSU

Genesis 9 in the SUSU2

Genesis 9 in the SYNO

Genesis 9 in the TBIAOTANT

Genesis 9 in the TBT1E

Genesis 9 in the TBT1E2

Genesis 9 in the TFTIP

Genesis 9 in the TFTU

Genesis 9 in the TGNTATF3T

Genesis 9 in the THAI

Genesis 9 in the TNFD

Genesis 9 in the TNT

Genesis 9 in the TNTIK

Genesis 9 in the TNTIL

Genesis 9 in the TNTIN

Genesis 9 in the TNTIP

Genesis 9 in the TNTIZ

Genesis 9 in the TOMA

Genesis 9 in the TTENT

Genesis 9 in the UBG

Genesis 9 in the UGV

Genesis 9 in the UGV2

Genesis 9 in the UGV3

Genesis 9 in the VBL

Genesis 9 in the VDCC

Genesis 9 in the YALU

Genesis 9 in the YAPE

Genesis 9 in the YBVTP

Genesis 9 in the ZBP