Joshua 4 (BOGWICC)

1 Anthu onse atatha kuwoloka Yorodani, Yehova anati kwa Yoswa, 2 “Sankha amuna khumi ndi awiri, mmodzi pa fuko lililonse. 3 Tsono uwalamule kuti, ‘Tengani miyala khumi ndi iwiri pakati penipeni pa mtsinje wa Yorodani, pamalo pamene ansembe anayimirirapo. Miyalayo muwoloke nayo ndi kudzayitula pamalo pamene mukagone usiku uno.’ ” 4 Choncho Yoswa anayitana amuna khumi ndi awiri amene anawasankha aja kuchokera pakati pa Aisraeli, mmodzi pa fuko lililonse, 5 ndipo anawawuza kuti, “Lowani pakati pa mtsinje wa Yorodani, patsogolo pa Bokosi la Yehova Mulungu wanu. Ndipo aliyense wa inu atenge mwala pa phewa lake, monga mwa chiwerengero cha mafuko a Aisraeli, 6 kuti ikhale chizindikiro kwa inu. Mʼtsogolo muno ana anu akamadzakufunsani kuti, ‘Kodi miyala iyi ikutanthauza chiyani?’ 7 Muzidzawawuza kuti, ‘Madzi a Yorodani analeka kuyenda pamene Bokosi la Chipangano la Yehova linkawoloka mtsinjewo. Miyala iyi idzakhala chikumbutso kwa anthu a Israeli kwa muyaya.’ ” 8 Aisraeli anachitadi monga Yoswa anawalamulira. Iwo ananyamula miyala khumi ndi iwiri kuchokera pakati pa Yorodani, fuko lililonse la Israeli mwala wake, monga Yehova analamulira Yoswa. Miyalayo anapita nayo ku misasa yawo nakayikhazika kumeneko. 9 Yoswa anayimika miyala khumi ndi iwiri imene inali pakati pa Yorodani pamalo pamene ansembe onyamula Bokosi la Chipangano anayimapo. Ndipo miyalayo ili pamalo pomwepo mpaka lero lino. 10 Ansembe onyamula Bokosi lija anayimirirabe pakati pa Yorodani mpaka zonse zimene Yehova analamulira Yoswa kuti awuze anthu zinatha. Zimenezi zinali monga momwe Mose anamufotokozera Yoswa. Tsono anthu anawoloka mtsinjewo mofulumira. 11 Anthu atatha kuwoloka, ansembe anatsogolera anthuwo atanyamula Bokosi la Yehova. 12 Anthu a fuko la Rubeni, Gadi ndi theka la fuko la Manase anawoloka patsogolo pa Aisraeli ali ndi zida, monga momwe Mose anawalamulira. 13 Asilikali pafupifupi 40,000 anawoloka napita kukayima mʼchigwa cha Yeriko kukonzekera nkhondo. 14 Zimene Yehova anachita tsiku limeneli zinapatsa anthu mtima wolemekeza Yoswa. Ndipo anamulemekeza masiku onse a moyo wake, monga momwe analemekezera Mose. 15 Kenaka Yehova anati kwa Yoswa, 16 “Lamula ansembe onyamula Bokosi la Chipanganowo kuti atuluke mu Yorodani.” 17 Choncho Yoswa anawalamuladi ansembe aja kuti atuluke mu Yorodani muja. 18 Ansembe onyamula Bokosi la Chipangano la Yehova aja atangotuluka mu mtsinje muja nʼkuponda powuma, madzi a mu Yorodani anayambanso kuyenda ngati poyamba mpaka kumasefukira. 19 Aisraeli anawoloka Yorodani tsiku lakhumi la mwezi woyamba ndipo anakamanga misasa yawo ku Giligala mbali ya kummawa kwa Yeriko. 20 Ku Giligala, Yoswa anayimikako miyala khumi ndi iwiri imene anayitenga mu Yorodani ija. 21 Ndipo iye anati kwa Aisraeli, “Mʼtsogolo muno pamene adzukulu anu adzafunsa makolo awo kuti, ‘Kodi miyala iyi ikutanthauza chiyani?’ 22 Muzidzawawuza kuti, ‘Aisraeli anawoloka Yorodani pansi pali powuma.’ 23 Pakuti Yehova Mulungu wanu ndiye anawumitsa Yorodani pamaso panu mpaka inu mutawoloka. Yehova Mulungu wanu anaphwetsa madzi a Yorodani monga mmene anachitira ndi Nyanja Yofiira mpaka ife tinawoloka powuma. 24 Iye anachita zimenezi kuti anthu onse pa dziko lapansi adziwe kuti dzanja la Yehova ndi lamphamvu, ndi kuti inu muziopa Yehova Mulungu wanu masiku onse.”

In Other Versions

Joshua 4 in the ANGEFD

Joshua 4 in the ANTPNG2D

Joshua 4 in the AS21

Joshua 4 in the BAGH

Joshua 4 in the BBPNG

Joshua 4 in the BBT1E

Joshua 4 in the BDS

Joshua 4 in the BEV

Joshua 4 in the BHAD

Joshua 4 in the BIB

Joshua 4 in the BLPT

Joshua 4 in the BNT

Joshua 4 in the BNTABOOT

Joshua 4 in the BNTLV

Joshua 4 in the BOATCB

Joshua 4 in the BOATCB2

Joshua 4 in the BOBCV

Joshua 4 in the BOCNT

Joshua 4 in the BOECS

Joshua 4 in the BOHCB

Joshua 4 in the BOHCV

Joshua 4 in the BOHLNT

Joshua 4 in the BOHNTLTAL

Joshua 4 in the BOICB

Joshua 4 in the BOILNTAP

Joshua 4 in the BOITCV

Joshua 4 in the BOKCV

Joshua 4 in the BOKCV2

Joshua 4 in the BOKHWOG

Joshua 4 in the BOKSSV

Joshua 4 in the BOLCB

Joshua 4 in the BOLCB2

Joshua 4 in the BOMCV

Joshua 4 in the BONAV

Joshua 4 in the BONCB

Joshua 4 in the BONLT

Joshua 4 in the BONUT2

Joshua 4 in the BOPLNT

Joshua 4 in the BOSCB

Joshua 4 in the BOSNC

Joshua 4 in the BOTLNT

Joshua 4 in the BOVCB

Joshua 4 in the BOYCB

Joshua 4 in the BPBB

Joshua 4 in the BPH

Joshua 4 in the BSB

Joshua 4 in the CCB

Joshua 4 in the CUV

Joshua 4 in the CUVS

Joshua 4 in the DBT

Joshua 4 in the DGDNT

Joshua 4 in the DHNT

Joshua 4 in the DNT

Joshua 4 in the ELBE

Joshua 4 in the EMTV

Joshua 4 in the ESV

Joshua 4 in the FBV

Joshua 4 in the FEB

Joshua 4 in the GGMNT

Joshua 4 in the GNT

Joshua 4 in the HARY

Joshua 4 in the HNT

Joshua 4 in the IRVA

Joshua 4 in the IRVB

Joshua 4 in the IRVG

Joshua 4 in the IRVH

Joshua 4 in the IRVK

Joshua 4 in the IRVM

Joshua 4 in the IRVM2

Joshua 4 in the IRVO

Joshua 4 in the IRVP

Joshua 4 in the IRVT

Joshua 4 in the IRVT2

Joshua 4 in the IRVU

Joshua 4 in the ISVN

Joshua 4 in the JSNT

Joshua 4 in the KAPI

Joshua 4 in the KBT1ETNIK

Joshua 4 in the KBV

Joshua 4 in the KJV

Joshua 4 in the KNFD

Joshua 4 in the LBA

Joshua 4 in the LBLA

Joshua 4 in the LNT

Joshua 4 in the LSV

Joshua 4 in the MAAL

Joshua 4 in the MBV

Joshua 4 in the MBV2

Joshua 4 in the MHNT

Joshua 4 in the MKNFD

Joshua 4 in the MNG

Joshua 4 in the MNT

Joshua 4 in the MNT2

Joshua 4 in the MRS1T

Joshua 4 in the NAA

Joshua 4 in the NASB

Joshua 4 in the NBLA

Joshua 4 in the NBS

Joshua 4 in the NBVTP

Joshua 4 in the NET2

Joshua 4 in the NIV11

Joshua 4 in the NNT

Joshua 4 in the NNT2

Joshua 4 in the NNT3

Joshua 4 in the PDDPT

Joshua 4 in the PFNT

Joshua 4 in the RMNT

Joshua 4 in the SBIAS

Joshua 4 in the SBIBS

Joshua 4 in the SBIBS2

Joshua 4 in the SBICS

Joshua 4 in the SBIDS

Joshua 4 in the SBIGS

Joshua 4 in the SBIHS

Joshua 4 in the SBIIS

Joshua 4 in the SBIIS2

Joshua 4 in the SBIIS3

Joshua 4 in the SBIKS

Joshua 4 in the SBIKS2

Joshua 4 in the SBIMS

Joshua 4 in the SBIOS

Joshua 4 in the SBIPS

Joshua 4 in the SBISS

Joshua 4 in the SBITS

Joshua 4 in the SBITS2

Joshua 4 in the SBITS3

Joshua 4 in the SBITS4

Joshua 4 in the SBIUS

Joshua 4 in the SBIVS

Joshua 4 in the SBT

Joshua 4 in the SBT1E

Joshua 4 in the SCHL

Joshua 4 in the SNT

Joshua 4 in the SUSU

Joshua 4 in the SUSU2

Joshua 4 in the SYNO

Joshua 4 in the TBIAOTANT

Joshua 4 in the TBT1E

Joshua 4 in the TBT1E2

Joshua 4 in the TFTIP

Joshua 4 in the TFTU

Joshua 4 in the TGNTATF3T

Joshua 4 in the THAI

Joshua 4 in the TNFD

Joshua 4 in the TNT

Joshua 4 in the TNTIK

Joshua 4 in the TNTIL

Joshua 4 in the TNTIN

Joshua 4 in the TNTIP

Joshua 4 in the TNTIZ

Joshua 4 in the TOMA

Joshua 4 in the TTENT

Joshua 4 in the UBG

Joshua 4 in the UGV

Joshua 4 in the UGV2

Joshua 4 in the UGV3

Joshua 4 in the VBL

Joshua 4 in the VDCC

Joshua 4 in the YALU

Joshua 4 in the YAPE

Joshua 4 in the YBVTP

Joshua 4 in the ZBP