Psalms 35 (BOGWICC)

undefined Salimo la Davide. 1 Inu Yehova, mulimbane nawo amene akulimbana nane;mumenyane nawo amene akumenyana nane. 2 Tengani chishango ndi lihawo;dzukani ndipo bwerani mundithandize. 3 Tengani mkondo ndi nthungo,kulimbana ndi iwo amene akundithamangitsa.Uzani moyo wanga kuti,“Ine ndine chipulumutso chako.” 4 Iwo amene akufunafuna moyo wangaanyozedwe ndi kuchita manyazi;iwo amene akukonza kuti moyo wanga uwonongekeabwerere mʼmbuyo mochititsa mantha. 5 Akhale ngati mankhusu owuluka ndi mphepopamene mngelo wa Yehova akuwapirikitsa. 6 Njira yawo ikhale ya mdima ndi yotererapamene mngelo wa Yehova akuwathamangitsa. 7 Popeza ananditchera ukonde popanda chifukwandipo popanda chifukwa andikumbira dzenje, 8 chiwonongeko chiwapeza modzidzimutsaukonde umene iwo abisa uwakole,agwere mʼdzenje kuti awonongedwe. 9 Pamenepo moyo wanga udzakondwera mwa Yehovandi kusangalala ndi chipulumutso chake. 10 Thupi langa lidzafuwula mokondwera,“Ndani angafanane nanu Yehova?Mumalanditsa osauka kwa amene ali ndi mphamvu zambiri,osauka ndi osowa kwa iwo amene amawalanda.” 11 Mboni zopanda chisoni zinayimirira,zinandifunsa zinthu zimene sindikuzidziwa. 12 Iwo anandibwezera zoyipa pa zabwinondipo anasiya moyo wanga pa chisoni. 13 Koma pamene iwo ankadwala, ine ndinavala chigudulindi kudzichepetsa ndekha posala zakudya.Pamene mapemphero anga anabwerera kwa ine osayankhidwa, 14 ndinayendayenda ndi kulira maliro,kumulira ngati bwenzi langa kapena mʼbale wanga.Ndinaweramitsa mutu wanga mosweka mtimakukhala ngati ndikulira amayi anga. 15 Koma pamene ndinaphunthwa, iwo anasonkhana mosangalala;ondithira nkhondo anasonkhana kutsutsana nane, ineyo osadziwa.Iwo sanasiye kundiyankhulira mawu onyoza. 16 Monga anthu osapembedza, iwo anandinyoza mwachipongwe;anandikukutira mano awo. 17 Ambuye, mpaka liti mudzakhala mukungoyangʼana?Landitsani moyo wanga ku chiwonongeko chawo,moyo wanga wopambana ku mikango. 18 Ndidzakuyamikani mu msonkhano waukulu;pakati pa gulu lalikulu la anthu ndidzakutamandani. 19 Musalole adani anga onyengaakondwere chifukwa cha masautso anga;musalole kuti amene amadana nane popanda chifukwaandiyangʼane chamʼmbali mondinyoza. 20 Iwowo sayankhula mwamtendere,koma amaganizira zonamiziraiwo amene amakhala mwabata mʼdziko. 21 Iwo amandiseka mofuwula ndipo amati, “Haa! Haa!Ndipo ndi maso athuwa ife taziona.” 22 Yehova mwaona zimenezi; musakhale chete.Ambuye musakhale kutali ndi ine. 23 Dzukani, ndipo nyamukani kunditeteza!Mulimbane nawo chifukwa cha ine, Mulungu wanga ndi Ambuye anga. 24 Onetsani kusalakwa kwanga mwa chilungamo chanu, Inu Yehova Mulungu wanga.Musalole kuti akondwere chifukwa cha mavuto anga. 25 Musalole kuti aganize kuti, “Amati atani, zachitika monga momwe timafunira!”Kapena kunena kuti, “Tamutha ameneyu basi.” 26 Onse amene amakondwera ndi masautso angaachite manyazi ndi kusokonezeka.Onse amene amadzikweza kufuna kundipambana,avekedwe manyazi ndi mnyozo ngati zovala. 27 Koma amene amakondwera chifukwa chakuti ndine wosalakwa,afuwule mwachimwemwe ndi chisangalalo.Nthawi zonse azinena kuti, “Yehova akwezeke,Iye amene amakondwera ndi kupeza bwino kwa mtumiki wake.” 28 Pakamwa panga padzayankhula za chilungamo chanundi za matamando anu tsiku lonse.

In Other Versions

Psalms 35 in the ANGEFD

Psalms 35 in the ANTPNG2D

Psalms 35 in the AS21

Psalms 35 in the BAGH

Psalms 35 in the BBPNG

Psalms 35 in the BBT1E

Psalms 35 in the BDS

Psalms 35 in the BEV

Psalms 35 in the BHAD

Psalms 35 in the BIB

Psalms 35 in the BLPT

Psalms 35 in the BNT

Psalms 35 in the BNTABOOT

Psalms 35 in the BNTLV

Psalms 35 in the BOATCB

Psalms 35 in the BOATCB2

Psalms 35 in the BOBCV

Psalms 35 in the BOCNT

Psalms 35 in the BOECS

Psalms 35 in the BOHCB

Psalms 35 in the BOHCV

Psalms 35 in the BOHLNT

Psalms 35 in the BOHNTLTAL

Psalms 35 in the BOICB

Psalms 35 in the BOILNTAP

Psalms 35 in the BOITCV

Psalms 35 in the BOKCV

Psalms 35 in the BOKCV2

Psalms 35 in the BOKHWOG

Psalms 35 in the BOKSSV

Psalms 35 in the BOLCB

Psalms 35 in the BOLCB2

Psalms 35 in the BOMCV

Psalms 35 in the BONAV

Psalms 35 in the BONCB

Psalms 35 in the BONLT

Psalms 35 in the BONUT2

Psalms 35 in the BOPLNT

Psalms 35 in the BOSCB

Psalms 35 in the BOSNC

Psalms 35 in the BOTLNT

Psalms 35 in the BOVCB

Psalms 35 in the BOYCB

Psalms 35 in the BPBB

Psalms 35 in the BPH

Psalms 35 in the BSB

Psalms 35 in the CCB

Psalms 35 in the CUV

Psalms 35 in the CUVS

Psalms 35 in the DBT

Psalms 35 in the DGDNT

Psalms 35 in the DHNT

Psalms 35 in the DNT

Psalms 35 in the ELBE

Psalms 35 in the EMTV

Psalms 35 in the ESV

Psalms 35 in the FBV

Psalms 35 in the FEB

Psalms 35 in the GGMNT

Psalms 35 in the GNT

Psalms 35 in the HARY

Psalms 35 in the HNT

Psalms 35 in the IRVA

Psalms 35 in the IRVB

Psalms 35 in the IRVG

Psalms 35 in the IRVH

Psalms 35 in the IRVK

Psalms 35 in the IRVM

Psalms 35 in the IRVM2

Psalms 35 in the IRVO

Psalms 35 in the IRVP

Psalms 35 in the IRVT

Psalms 35 in the IRVT2

Psalms 35 in the IRVU

Psalms 35 in the ISVN

Psalms 35 in the JSNT

Psalms 35 in the KAPI

Psalms 35 in the KBT1ETNIK

Psalms 35 in the KBV

Psalms 35 in the KJV

Psalms 35 in the KNFD

Psalms 35 in the LBA

Psalms 35 in the LBLA

Psalms 35 in the LNT

Psalms 35 in the LSV

Psalms 35 in the MAAL

Psalms 35 in the MBV

Psalms 35 in the MBV2

Psalms 35 in the MHNT

Psalms 35 in the MKNFD

Psalms 35 in the MNG

Psalms 35 in the MNT

Psalms 35 in the MNT2

Psalms 35 in the MRS1T

Psalms 35 in the NAA

Psalms 35 in the NASB

Psalms 35 in the NBLA

Psalms 35 in the NBS

Psalms 35 in the NBVTP

Psalms 35 in the NET2

Psalms 35 in the NIV11

Psalms 35 in the NNT

Psalms 35 in the NNT2

Psalms 35 in the NNT3

Psalms 35 in the PDDPT

Psalms 35 in the PFNT

Psalms 35 in the RMNT

Psalms 35 in the SBIAS

Psalms 35 in the SBIBS

Psalms 35 in the SBIBS2

Psalms 35 in the SBICS

Psalms 35 in the SBIDS

Psalms 35 in the SBIGS

Psalms 35 in the SBIHS

Psalms 35 in the SBIIS

Psalms 35 in the SBIIS2

Psalms 35 in the SBIIS3

Psalms 35 in the SBIKS

Psalms 35 in the SBIKS2

Psalms 35 in the SBIMS

Psalms 35 in the SBIOS

Psalms 35 in the SBIPS

Psalms 35 in the SBISS

Psalms 35 in the SBITS

Psalms 35 in the SBITS2

Psalms 35 in the SBITS3

Psalms 35 in the SBITS4

Psalms 35 in the SBIUS

Psalms 35 in the SBIVS

Psalms 35 in the SBT

Psalms 35 in the SBT1E

Psalms 35 in the SCHL

Psalms 35 in the SNT

Psalms 35 in the SUSU

Psalms 35 in the SUSU2

Psalms 35 in the SYNO

Psalms 35 in the TBIAOTANT

Psalms 35 in the TBT1E

Psalms 35 in the TBT1E2

Psalms 35 in the TFTIP

Psalms 35 in the TFTU

Psalms 35 in the TGNTATF3T

Psalms 35 in the THAI

Psalms 35 in the TNFD

Psalms 35 in the TNT

Psalms 35 in the TNTIK

Psalms 35 in the TNTIL

Psalms 35 in the TNTIN

Psalms 35 in the TNTIP

Psalms 35 in the TNTIZ

Psalms 35 in the TOMA

Psalms 35 in the TTENT

Psalms 35 in the UBG

Psalms 35 in the UGV

Psalms 35 in the UGV2

Psalms 35 in the UGV3

Psalms 35 in the VBL

Psalms 35 in the VDCC

Psalms 35 in the YALU

Psalms 35 in the YAPE

Psalms 35 in the YBVTP

Psalms 35 in the ZBP