Ephesians 6 (BOGWICC)

1 Inu ana, mverani makolo anu mwa Ambuye, pakuti zimenezi ndi zoyenera. 2 “Lemekeza abambo ndi amayi ako.” Limeneli ndi lamulo loyamba lokhala ndi lonjezo. 3 Ngati ulemekeza abambo ako ndi amayi ako, “zinthu zidzakuyendera bwino ndipo udzasangalala ndi moyo wautali pa dziko lapansi.” 4 Abambo musakwiyitse ana anu; mʼmalo mwake, muwalere mʼchiphunzitso ndi mʼchilangizo cha Ambuye. 5 Inu antchito, mverani mabwana anu mwaulemu ndi mwamantha ndi moona mtima, monga momwe mungamvere Khristu. 6 Musawamvere pamene akukuonani kuti akukomereni mtima, koma ngati akapolo a Khristu ochita chifuniro cha Mulungu kuchokera mu mtima mwanu. 7 Tumikirani ndi mtima wonse, ngati kuti mukutumikira Ambuye, osati anthu. 8 Inu mukudziwa kuti Ambuye adzamupatsa munthu aliyense mphotho chifukwa cha ntchito yake yabwino imene anagwira, kaya munthuyo ndi kapolo kapena mfulu. 9 Ndipo inu mabwana, muziwachitiranso chimodzimodzi antchito anu. Musamawaopseze, popeza mukudziwa kuti Mbuye wawo ndi wanunso, nonse Mbuye wanu ali kumwamba, ndipo Iyeyo alibe tsankho. 10 Potsiriza ndikuti, dzilimbitseni mwa Ambuye ndi mwa mphamvu zake zazikulu. 11 Valani zida zonse za Mulungu kuti muthe kuyima ndi kukana machenjerero a Satana. 12 Pakuti sitikulimbana ndi thupi ndi magazi, koma tikulimbana ndi maufumu, maulamuliro, mphamvu za dziko la mdima, ndi mphamvu zoyipa kwambiri zauzimu zamlengalenga. 13 Choncho valani zida zonse za Mulungu, kuti pamene tsiku loyipa kwambiri lifika, mudzathe kuyima chilili, ndipo mutatha kuchita zonse, mudzayimabe mwamphamvu. 14 Tsono imani mwamphamvu, mutamangira choonadi ngati lamba mʼchiwuno mwanu, mutavala chilungamo ngati chitsulo chotchinjiriza pa chifuwa. 15 Valani Uthenga Wabwino wamtendere ku mapazi anu ngati nsapato. 16 Kuwonjezera pa zonsezi, nyamulani chishango cha chikhulupiriro, ndipo ndi chimenechi mudzatha kuzimitsa mivi yonse yoyaka moto ya oyipayo. 17 Valani chipewa cha chipulumutso ndi kutenga lupanga la mzimu, limene ndi Mawu a Mulungu. 18 Ndipo mupemphere mwa Mzimu nthawi zonse, mʼmitundu yonse ya mapemphero ndi zopempha. Ndipo pozindikira izi, khalani achangu kupempherera oyera mtima nthawi zonse. 19 Mundipempherere inenso, kuti nthawi iliyonse pamene nditsekula pakamwa panga, andipatse mawu kuti ndiwulule zinsinsi za Uthenga Wabwino mopanda mantha. 20 Ndine kazembe wa Uthenga Wabwinowu ngakhale ndili womangidwa mʼndende. Pempherani kuti ndilalikire mopanda mantha, monga ndiyenera. 21 Tukiko, mʼbale wanga wokondedwa ndi mtumiki wokhulupirika mwa Ambuye, adzakuwuzani zonse kuti inunso mudziwe mmene ndilili ndi zimene ndikuchita. 22 Ine ndikumutumiza kwa inu, kuti mudziwe za moyo wathu, ndi kuti akulimbikitseni. 23 Mtendere, chikondi pamodzi ndi chikhulupiriro kuchokera kwa Mulungu Atate ndi Ambuye Yesu Khristu zikhale ndi abale onse. 24 Chisomo kwa onse amene amakonda Ambuye athu Yesu Khristu ndi chikondi chosatha.

In Other Versions

Ephesians 6 in the ANGEFD

Ephesians 6 in the ANTPNG2D

Ephesians 6 in the AS21

Ephesians 6 in the BAGH

Ephesians 6 in the BBPNG

Ephesians 6 in the BBT1E

Ephesians 6 in the BDS

Ephesians 6 in the BEV

Ephesians 6 in the BHAD

Ephesians 6 in the BIB

Ephesians 6 in the BLPT

Ephesians 6 in the BNT

Ephesians 6 in the BNTABOOT

Ephesians 6 in the BNTLV

Ephesians 6 in the BOATCB

Ephesians 6 in the BOATCB2

Ephesians 6 in the BOBCV

Ephesians 6 in the BOCNT

Ephesians 6 in the BOECS

Ephesians 6 in the BOHCB

Ephesians 6 in the BOHCV

Ephesians 6 in the BOHLNT

Ephesians 6 in the BOHNTLTAL

Ephesians 6 in the BOICB

Ephesians 6 in the BOILNTAP

Ephesians 6 in the BOITCV

Ephesians 6 in the BOKCV

Ephesians 6 in the BOKCV2

Ephesians 6 in the BOKHWOG

Ephesians 6 in the BOKSSV

Ephesians 6 in the BOLCB

Ephesians 6 in the BOLCB2

Ephesians 6 in the BOMCV

Ephesians 6 in the BONAV

Ephesians 6 in the BONCB

Ephesians 6 in the BONLT

Ephesians 6 in the BONUT2

Ephesians 6 in the BOPLNT

Ephesians 6 in the BOSCB

Ephesians 6 in the BOSNC

Ephesians 6 in the BOTLNT

Ephesians 6 in the BOVCB

Ephesians 6 in the BOYCB

Ephesians 6 in the BPBB

Ephesians 6 in the BPH

Ephesians 6 in the BSB

Ephesians 6 in the CCB

Ephesians 6 in the CUV

Ephesians 6 in the CUVS

Ephesians 6 in the DBT

Ephesians 6 in the DGDNT

Ephesians 6 in the DHNT

Ephesians 6 in the DNT

Ephesians 6 in the ELBE

Ephesians 6 in the EMTV

Ephesians 6 in the ESV

Ephesians 6 in the FBV

Ephesians 6 in the FEB

Ephesians 6 in the GGMNT

Ephesians 6 in the GNT

Ephesians 6 in the HARY

Ephesians 6 in the HNT

Ephesians 6 in the IRVA

Ephesians 6 in the IRVB

Ephesians 6 in the IRVG

Ephesians 6 in the IRVH

Ephesians 6 in the IRVK

Ephesians 6 in the IRVM

Ephesians 6 in the IRVM2

Ephesians 6 in the IRVO

Ephesians 6 in the IRVP

Ephesians 6 in the IRVT

Ephesians 6 in the IRVT2

Ephesians 6 in the IRVU

Ephesians 6 in the ISVN

Ephesians 6 in the JSNT

Ephesians 6 in the KAPI

Ephesians 6 in the KBT1ETNIK

Ephesians 6 in the KBV

Ephesians 6 in the KJV

Ephesians 6 in the KNFD

Ephesians 6 in the LBA

Ephesians 6 in the LBLA

Ephesians 6 in the LNT

Ephesians 6 in the LSV

Ephesians 6 in the MAAL

Ephesians 6 in the MBV

Ephesians 6 in the MBV2

Ephesians 6 in the MHNT

Ephesians 6 in the MKNFD

Ephesians 6 in the MNG

Ephesians 6 in the MNT

Ephesians 6 in the MNT2

Ephesians 6 in the MRS1T

Ephesians 6 in the NAA

Ephesians 6 in the NASB

Ephesians 6 in the NBLA

Ephesians 6 in the NBS

Ephesians 6 in the NBVTP

Ephesians 6 in the NET2

Ephesians 6 in the NIV11

Ephesians 6 in the NNT

Ephesians 6 in the NNT2

Ephesians 6 in the NNT3

Ephesians 6 in the PDDPT

Ephesians 6 in the PFNT

Ephesians 6 in the RMNT

Ephesians 6 in the SBIAS

Ephesians 6 in the SBIBS

Ephesians 6 in the SBIBS2

Ephesians 6 in the SBICS

Ephesians 6 in the SBIDS

Ephesians 6 in the SBIGS

Ephesians 6 in the SBIHS

Ephesians 6 in the SBIIS

Ephesians 6 in the SBIIS2

Ephesians 6 in the SBIIS3

Ephesians 6 in the SBIKS

Ephesians 6 in the SBIKS2

Ephesians 6 in the SBIMS

Ephesians 6 in the SBIOS

Ephesians 6 in the SBIPS

Ephesians 6 in the SBISS

Ephesians 6 in the SBITS

Ephesians 6 in the SBITS2

Ephesians 6 in the SBITS3

Ephesians 6 in the SBITS4

Ephesians 6 in the SBIUS

Ephesians 6 in the SBIVS

Ephesians 6 in the SBT

Ephesians 6 in the SBT1E

Ephesians 6 in the SCHL

Ephesians 6 in the SNT

Ephesians 6 in the SUSU

Ephesians 6 in the SUSU2

Ephesians 6 in the SYNO

Ephesians 6 in the TBIAOTANT

Ephesians 6 in the TBT1E

Ephesians 6 in the TBT1E2

Ephesians 6 in the TFTIP

Ephesians 6 in the TFTU

Ephesians 6 in the TGNTATF3T

Ephesians 6 in the THAI

Ephesians 6 in the TNFD

Ephesians 6 in the TNT

Ephesians 6 in the TNTIK

Ephesians 6 in the TNTIL

Ephesians 6 in the TNTIN

Ephesians 6 in the TNTIP

Ephesians 6 in the TNTIZ

Ephesians 6 in the TOMA

Ephesians 6 in the TTENT

Ephesians 6 in the UBG

Ephesians 6 in the UGV

Ephesians 6 in the UGV2

Ephesians 6 in the UGV3

Ephesians 6 in the VBL

Ephesians 6 in the VDCC

Ephesians 6 in the YALU

Ephesians 6 in the YAPE

Ephesians 6 in the YBVTP

Ephesians 6 in the ZBP