Isaiah 8 (BOGWICC)

1 Yehova anati kwa ine, “Tenga cholembapo chachikulu ndipo ulembepo malemba odziwika bwino: KUSAKAZA-KWAMSANGA KUFUNKHA-KOFULUMIRA. 2 Ndipo ndidzayitana wansembe Uriya ndi Zekariya mwana wa Yeberekiya kuti akhale mboni zanga zodalirika.” 3 Ndipo ine ndinapita kwa mneneri wamkazi, ndipo anakhala woyembekezera nabala mwana wamwamuna. Ndipo Yehova anati kwa ine, “Umutche dzina lakuti, ‘Kusakaza-Kwamsanga Kufunkha-Kofulumira.’ 4 Mwanayo asanayambe kudziwa kuyitana kuti, ‘Ababa’ kapena ‘Amama’ chuma cha Damasiko ndi zofunkha za Samariya zidzatengedwa ndi mfumu ya ku Asiriya.” 5 Yehova anayankhulanso ndi Ine; 6 “Popeza anthu a dziko ili akanamadzi anga oyenda mwachifatse a ku Siloamu,ndipo akukondwerera Rezinindi mwana wa Remaliya, 7 nʼchifukwa chake Ambuye ali pafupi kubweretsamadzi amkokomo a mtsinje wa Yufurate kudzalimbana nawo;mfumu ya ku Asiriya ndi gulu lake lonse lankhondo.Madziwo adzasefukira mʼngalande zake zonsendi mʼmagombe ake onse. 8 Ndipo adzalowa mwamphamvu mʼdziko la Yuda, adzasefukira,adzapitirira mpaka kumuyesa mʼkhosi.Mapiko ake otambasuka adzaphimba dziko lako lonse,iwe Imanueli!” 9 Chitani phokoso lankhondo, inu mitundu ya anthu, ndipo munjenjemere!Tamverani, inu mayiko onse akutali.Konzekerani nkhondo ndipo munjenjemere!Konzekerani nkhondo ndipo munjenjemere! 10 Konzani kachitidwe kanu kankhondo, koma simudzaphula kanthu,kambiranani zochita, koma zidzalephereka,pakuti Mulungu ali nafe. 11 Yehova anandiyankhula ine mwamphamvu, ndipo anandichenjeza kuti ndisamayende mʼnjira za anthuwa. Iye anati: 12 “Usamanene kuti ndi chiwembu,chilichonse chimene anthuwa amati ndi chiwembuusamaope zimene anthuwa amaziopa,ndipo usamachite nazo mantha. 13 Yehova Wamphamvuzonse ndiye amene uyenera kumuona kuti ndi woyera,ndiye amene uyenera kumuopa,ndiye amene uyenera kuchita naye mantha, 14 ndipo ndiye amene adzakhala malo opatulika;koma kwa anthu a ku Yuda ndi kwa anthu a ku Israeli adzakhalamwala wopunthwitsa,mwala umene umapunthwitsa anthu,thanthwe limene limagwetsa anthu.Ndipo kwa anthu a mu Yerusalemu adzakhala ngati msampha ndi khwekhwe. 15 Anthu ambiri adzapunthwapoadzagwa ndi kuthyokathyoka,adzakodwa ndi kugwidwa.” 16 Manga umboniwundipo umate malamulowa pamaso pa ophunzira anga. 17 Ndidzayembekezera Yehova,amene akubisira nkhope yake nyumba ya Yakobo.Ine ndidzakhulupirira Iyeyo. 18 Onani, ine ndili pano pamodzi ndi ana amene Yehova wandipatsa, ndife zizindikiro ndi zodabwitsa kwa Aisraeli zochokera kwa Yehova Wamphamvuzonse, amene amakhala pa Phiri la Ziyoni. 19 Anthu akakuwuza kuti kafunsire kwa oyankhula ndi mizimu, amene amayankhula monongʼona ndi mongʼungʼudza, kodi anthu sayenera kukafunsira kwa Mulungu wawo? Chifukwa chiyani amafunsira kwa anthu akufa mʼmalo mwa kwa anthu amoyo, 20 kuti akalandireko mawu enieni ndi malangizo? Ngati anthuwo sayankhula monga mwa mawu awa, mwa iwo mulibe kuwala. 21 Anthu adzayendayenda mʼdziko movutika kwambiri ali ndi njala; pamene afowokeratu ndi njala, iwo adzakwiya kwambiri ndipo adzayangʼana kumwamba ndi kutemberera mfumu yawo ndi Mulungu wawo. 22 Ndipo akadzayangʼana pa dziko lapansi adzangoona mavuto okhaokha ndi mdima woopsa ndi wodetsa nkhawa, ndipo adzaponyedwa mu mdima wandiweyani.

In Other Versions

Isaiah 8 in the ANGEFD

Isaiah 8 in the ANTPNG2D

Isaiah 8 in the AS21

Isaiah 8 in the BAGH

Isaiah 8 in the BBPNG

Isaiah 8 in the BBT1E

Isaiah 8 in the BDS

Isaiah 8 in the BEV

Isaiah 8 in the BHAD

Isaiah 8 in the BIB

Isaiah 8 in the BLPT

Isaiah 8 in the BNT

Isaiah 8 in the BNTABOOT

Isaiah 8 in the BNTLV

Isaiah 8 in the BOATCB

Isaiah 8 in the BOATCB2

Isaiah 8 in the BOBCV

Isaiah 8 in the BOCNT

Isaiah 8 in the BOECS

Isaiah 8 in the BOHCB

Isaiah 8 in the BOHCV

Isaiah 8 in the BOHLNT

Isaiah 8 in the BOHNTLTAL

Isaiah 8 in the BOICB

Isaiah 8 in the BOILNTAP

Isaiah 8 in the BOITCV

Isaiah 8 in the BOKCV

Isaiah 8 in the BOKCV2

Isaiah 8 in the BOKHWOG

Isaiah 8 in the BOKSSV

Isaiah 8 in the BOLCB

Isaiah 8 in the BOLCB2

Isaiah 8 in the BOMCV

Isaiah 8 in the BONAV

Isaiah 8 in the BONCB

Isaiah 8 in the BONLT

Isaiah 8 in the BONUT2

Isaiah 8 in the BOPLNT

Isaiah 8 in the BOSCB

Isaiah 8 in the BOSNC

Isaiah 8 in the BOTLNT

Isaiah 8 in the BOVCB

Isaiah 8 in the BOYCB

Isaiah 8 in the BPBB

Isaiah 8 in the BPH

Isaiah 8 in the BSB

Isaiah 8 in the CCB

Isaiah 8 in the CUV

Isaiah 8 in the CUVS

Isaiah 8 in the DBT

Isaiah 8 in the DGDNT

Isaiah 8 in the DHNT

Isaiah 8 in the DNT

Isaiah 8 in the ELBE

Isaiah 8 in the EMTV

Isaiah 8 in the ESV

Isaiah 8 in the FBV

Isaiah 8 in the FEB

Isaiah 8 in the GGMNT

Isaiah 8 in the GNT

Isaiah 8 in the HARY

Isaiah 8 in the HNT

Isaiah 8 in the IRVA

Isaiah 8 in the IRVB

Isaiah 8 in the IRVG

Isaiah 8 in the IRVH

Isaiah 8 in the IRVK

Isaiah 8 in the IRVM

Isaiah 8 in the IRVM2

Isaiah 8 in the IRVO

Isaiah 8 in the IRVP

Isaiah 8 in the IRVT

Isaiah 8 in the IRVT2

Isaiah 8 in the IRVU

Isaiah 8 in the ISVN

Isaiah 8 in the JSNT

Isaiah 8 in the KAPI

Isaiah 8 in the KBT1ETNIK

Isaiah 8 in the KBV

Isaiah 8 in the KJV

Isaiah 8 in the KNFD

Isaiah 8 in the LBA

Isaiah 8 in the LBLA

Isaiah 8 in the LNT

Isaiah 8 in the LSV

Isaiah 8 in the MAAL

Isaiah 8 in the MBV

Isaiah 8 in the MBV2

Isaiah 8 in the MHNT

Isaiah 8 in the MKNFD

Isaiah 8 in the MNG

Isaiah 8 in the MNT

Isaiah 8 in the MNT2

Isaiah 8 in the MRS1T

Isaiah 8 in the NAA

Isaiah 8 in the NASB

Isaiah 8 in the NBLA

Isaiah 8 in the NBS

Isaiah 8 in the NBVTP

Isaiah 8 in the NET2

Isaiah 8 in the NIV11

Isaiah 8 in the NNT

Isaiah 8 in the NNT2

Isaiah 8 in the NNT3

Isaiah 8 in the PDDPT

Isaiah 8 in the PFNT

Isaiah 8 in the RMNT

Isaiah 8 in the SBIAS

Isaiah 8 in the SBIBS

Isaiah 8 in the SBIBS2

Isaiah 8 in the SBICS

Isaiah 8 in the SBIDS

Isaiah 8 in the SBIGS

Isaiah 8 in the SBIHS

Isaiah 8 in the SBIIS

Isaiah 8 in the SBIIS2

Isaiah 8 in the SBIIS3

Isaiah 8 in the SBIKS

Isaiah 8 in the SBIKS2

Isaiah 8 in the SBIMS

Isaiah 8 in the SBIOS

Isaiah 8 in the SBIPS

Isaiah 8 in the SBISS

Isaiah 8 in the SBITS

Isaiah 8 in the SBITS2

Isaiah 8 in the SBITS3

Isaiah 8 in the SBITS4

Isaiah 8 in the SBIUS

Isaiah 8 in the SBIVS

Isaiah 8 in the SBT

Isaiah 8 in the SBT1E

Isaiah 8 in the SCHL

Isaiah 8 in the SNT

Isaiah 8 in the SUSU

Isaiah 8 in the SUSU2

Isaiah 8 in the SYNO

Isaiah 8 in the TBIAOTANT

Isaiah 8 in the TBT1E

Isaiah 8 in the TBT1E2

Isaiah 8 in the TFTIP

Isaiah 8 in the TFTU

Isaiah 8 in the TGNTATF3T

Isaiah 8 in the THAI

Isaiah 8 in the TNFD

Isaiah 8 in the TNT

Isaiah 8 in the TNTIK

Isaiah 8 in the TNTIL

Isaiah 8 in the TNTIN

Isaiah 8 in the TNTIP

Isaiah 8 in the TNTIZ

Isaiah 8 in the TOMA

Isaiah 8 in the TTENT

Isaiah 8 in the UBG

Isaiah 8 in the UGV

Isaiah 8 in the UGV2

Isaiah 8 in the UGV3

Isaiah 8 in the VBL

Isaiah 8 in the VDCC

Isaiah 8 in the YALU

Isaiah 8 in the YAPE

Isaiah 8 in the YBVTP

Isaiah 8 in the ZBP