Jeremiah 18 (BOGWICC)

1 Yehova anawuza Yeremiya kuti, 2 “Pita ku nyumba ya munthu wowumba mbiya, ndipo kumeneko ndikakuwuza mawu anga.” 3 Choncho ndinatsikira ku nyumba ya wowumba mbiya, ndipo ndinamuona akuwumba mbiya pa mkombero. 4 Tsono amati ngati mbiya imene waumba ikhala yosawumbika bwino ankayiphwanya nʼkuwumbanso ina monga mmene afunira ndi dothi lake lomwe lija. 5 Kenaka Yehova anandiwuza kuti, 6 “Inu Aisraeli, kodi Ine sindingathe kuchita nanu monga amachitira wowumba mbiya?” akutero Yehova. “Inu muli mʼmanja mwanga ngati mtapo mʼmanja mwa wowumba mbiya. 7 Ngati nditalengeza kuti mtundu wina wa anthu kapena ufumu wina ndiwuzula, kuwugwetsa ndi kuwuwononga, 8 ndipo ngati mtundu wa anthu umene ndawuchenjezawo ulapa zoyipa zawo, ndiye kuti Ine ndidzaleka ndipo sindidzabweretsa pa anthuwo mavuto amene ndinakonzekera kuwachitira. 9 Ndipo ngati ndilengeza kuti ndikufuna kumanga ndi kukhazikitsa mtundu wa anthu kapena ufumu. 10 Koma mtunduwo ukachita choyipa pamaso panga nʼkusandimvera, ndiye kuti sindidzawuchitiranso zabwino zimene ndimafuna ndiwuchitire. 11 “Ndipo tsopano kawawuze anthu a ku Yuda ndi amene akukhala mu Yerusalemu kuti, ‘Yehova akuti, Taonani! Ndikukukonzerani mavuto, ndi kuganizira zoti ndikulangeni. Kotero siyani makhalidwe anu oyipa aliyense wa inu, ndipo mukonzenso makhalidwe anu ndi zochita zanu.’ 12 Koma iwo adzayankha kuti, ‘Zimenezo nʼzosathandiza. Ife tidzapitiriza kuchita zomwe takonzekera; aliyense wa ife adzatsatira zoyipa za mtima wake wokanika.’ ” 13 Yehova akuti,“Uwafunse anthu a mitundu ina kuti:Kodi ndani anamvapo zinthu zofanana ndi zimenezi?Israeli amene anali ngati namwali wanga wachitachinthu choopsa kwambiri. 14 Kodi chisanu chimatha pa matanthweotsetsereka a phiri la Lebanoni?Kodi madzi ozizira amitsinje ochokeraku phiri la Lebanoni adzamphwa? 15 Komatu anthu anga andiyiwala;akufukiza lubani kwa mafano achabechabe.Amapunthwa mʼnjirazawo zakale.Amayenda mʼnjira zachidulendi kusiya njira zabwino. 16 Dziko lawo amalisandutsa chipululu,chinthu chochititsa manyazi nthawi zonse;onse odutsapo adzadabwa kwambirindipo adzapukusa mitu yawo. 17 Ngati mphepo yochokera kummawa,ndidzawabalalitsa pamaso pa adani awo;ndidzawafulatira osawathandizapa tsiku la mavuto awo.” 18 Anthuwo anati, “Tiyeni, tipangane zoti timuchitire Yeremiya; pakuti ansembe otiphunzitsa malamulo tidzakhala nawobe. Anthu anzeru otilangiza tidzakhala nawo, ndiponso aneneri otilalikira mawu. Choncho tiyeni timupezere chifukwa ndipo tisamvere chilichonse chimene akunena.” 19 Ndipo ndinapemphera kwa Yehova kuti, “Inu Yehova, ndimvereni;imvani zimene adani anga akunena za ine! 20 Kodi chinthu choyipa nʼkukhala dipo la chinthu chabwino?Komabe iwo andikumbira dzenje.Kumbukirani kuti ndinadzayima pamaso panukudzawapemphererakuti muwachotsere mkwiyo wanu. 21 Choncho langani ana awo ndi njala;aperekeni kuti aphedwe ndi lupanga.Akazi awo asanduke opanda ana ndi amasiye;amuna awo aphedwe ndi mliri,anyamata awo aphedwe ndi lupanga ku nkhondo. 22 Kulira kumveke kuchokera mʼnyumba zawomutawatumizira gulu lankhondo mwadzidzidzi kuti liwakanthe.Iwo andikumbira dzenje kuti ndigweremondipo atchera msampha mapazi anga. 23 Koma Inu Yehova, mukudziwaziwembu zawo zonse zofuna kundipha.Musawakhululukire zolakwa zawokapena kufafaniza machimo awo pamaso panu.Agonjetsedwe pamaso panu;muwalange muli wokwiya.”

In Other Versions

Jeremiah 18 in the ANGEFD

Jeremiah 18 in the ANTPNG2D

Jeremiah 18 in the AS21

Jeremiah 18 in the BAGH

Jeremiah 18 in the BBPNG

Jeremiah 18 in the BBT1E

Jeremiah 18 in the BDS

Jeremiah 18 in the BEV

Jeremiah 18 in the BHAD

Jeremiah 18 in the BIB

Jeremiah 18 in the BLPT

Jeremiah 18 in the BNT

Jeremiah 18 in the BNTABOOT

Jeremiah 18 in the BNTLV

Jeremiah 18 in the BOATCB

Jeremiah 18 in the BOATCB2

Jeremiah 18 in the BOBCV

Jeremiah 18 in the BOCNT

Jeremiah 18 in the BOECS

Jeremiah 18 in the BOHCB

Jeremiah 18 in the BOHCV

Jeremiah 18 in the BOHLNT

Jeremiah 18 in the BOHNTLTAL

Jeremiah 18 in the BOICB

Jeremiah 18 in the BOILNTAP

Jeremiah 18 in the BOITCV

Jeremiah 18 in the BOKCV

Jeremiah 18 in the BOKCV2

Jeremiah 18 in the BOKHWOG

Jeremiah 18 in the BOKSSV

Jeremiah 18 in the BOLCB

Jeremiah 18 in the BOLCB2

Jeremiah 18 in the BOMCV

Jeremiah 18 in the BONAV

Jeremiah 18 in the BONCB

Jeremiah 18 in the BONLT

Jeremiah 18 in the BONUT2

Jeremiah 18 in the BOPLNT

Jeremiah 18 in the BOSCB

Jeremiah 18 in the BOSNC

Jeremiah 18 in the BOTLNT

Jeremiah 18 in the BOVCB

Jeremiah 18 in the BOYCB

Jeremiah 18 in the BPBB

Jeremiah 18 in the BPH

Jeremiah 18 in the BSB

Jeremiah 18 in the CCB

Jeremiah 18 in the CUV

Jeremiah 18 in the CUVS

Jeremiah 18 in the DBT

Jeremiah 18 in the DGDNT

Jeremiah 18 in the DHNT

Jeremiah 18 in the DNT

Jeremiah 18 in the ELBE

Jeremiah 18 in the EMTV

Jeremiah 18 in the ESV

Jeremiah 18 in the FBV

Jeremiah 18 in the FEB

Jeremiah 18 in the GGMNT

Jeremiah 18 in the GNT

Jeremiah 18 in the HARY

Jeremiah 18 in the HNT

Jeremiah 18 in the IRVA

Jeremiah 18 in the IRVB

Jeremiah 18 in the IRVG

Jeremiah 18 in the IRVH

Jeremiah 18 in the IRVK

Jeremiah 18 in the IRVM

Jeremiah 18 in the IRVM2

Jeremiah 18 in the IRVO

Jeremiah 18 in the IRVP

Jeremiah 18 in the IRVT

Jeremiah 18 in the IRVT2

Jeremiah 18 in the IRVU

Jeremiah 18 in the ISVN

Jeremiah 18 in the JSNT

Jeremiah 18 in the KAPI

Jeremiah 18 in the KBT1ETNIK

Jeremiah 18 in the KBV

Jeremiah 18 in the KJV

Jeremiah 18 in the KNFD

Jeremiah 18 in the LBA

Jeremiah 18 in the LBLA

Jeremiah 18 in the LNT

Jeremiah 18 in the LSV

Jeremiah 18 in the MAAL

Jeremiah 18 in the MBV

Jeremiah 18 in the MBV2

Jeremiah 18 in the MHNT

Jeremiah 18 in the MKNFD

Jeremiah 18 in the MNG

Jeremiah 18 in the MNT

Jeremiah 18 in the MNT2

Jeremiah 18 in the MRS1T

Jeremiah 18 in the NAA

Jeremiah 18 in the NASB

Jeremiah 18 in the NBLA

Jeremiah 18 in the NBS

Jeremiah 18 in the NBVTP

Jeremiah 18 in the NET2

Jeremiah 18 in the NIV11

Jeremiah 18 in the NNT

Jeremiah 18 in the NNT2

Jeremiah 18 in the NNT3

Jeremiah 18 in the PDDPT

Jeremiah 18 in the PFNT

Jeremiah 18 in the RMNT

Jeremiah 18 in the SBIAS

Jeremiah 18 in the SBIBS

Jeremiah 18 in the SBIBS2

Jeremiah 18 in the SBICS

Jeremiah 18 in the SBIDS

Jeremiah 18 in the SBIGS

Jeremiah 18 in the SBIHS

Jeremiah 18 in the SBIIS

Jeremiah 18 in the SBIIS2

Jeremiah 18 in the SBIIS3

Jeremiah 18 in the SBIKS

Jeremiah 18 in the SBIKS2

Jeremiah 18 in the SBIMS

Jeremiah 18 in the SBIOS

Jeremiah 18 in the SBIPS

Jeremiah 18 in the SBISS

Jeremiah 18 in the SBITS

Jeremiah 18 in the SBITS2

Jeremiah 18 in the SBITS3

Jeremiah 18 in the SBITS4

Jeremiah 18 in the SBIUS

Jeremiah 18 in the SBIVS

Jeremiah 18 in the SBT

Jeremiah 18 in the SBT1E

Jeremiah 18 in the SCHL

Jeremiah 18 in the SNT

Jeremiah 18 in the SUSU

Jeremiah 18 in the SUSU2

Jeremiah 18 in the SYNO

Jeremiah 18 in the TBIAOTANT

Jeremiah 18 in the TBT1E

Jeremiah 18 in the TBT1E2

Jeremiah 18 in the TFTIP

Jeremiah 18 in the TFTU

Jeremiah 18 in the TGNTATF3T

Jeremiah 18 in the THAI

Jeremiah 18 in the TNFD

Jeremiah 18 in the TNT

Jeremiah 18 in the TNTIK

Jeremiah 18 in the TNTIL

Jeremiah 18 in the TNTIN

Jeremiah 18 in the TNTIP

Jeremiah 18 in the TNTIZ

Jeremiah 18 in the TOMA

Jeremiah 18 in the TTENT

Jeremiah 18 in the UBG

Jeremiah 18 in the UGV

Jeremiah 18 in the UGV2

Jeremiah 18 in the UGV3

Jeremiah 18 in the VBL

Jeremiah 18 in the VDCC

Jeremiah 18 in the YALU

Jeremiah 18 in the YAPE

Jeremiah 18 in the YBVTP

Jeremiah 18 in the ZBP