Proverbs 28 (BOGWICC)
1 Munthu woyipa amathawa ngakhale palibe wina womuthamangitsa,koma wolungama ndi wolimba mtima ngati mkango. 2 Pamene mʼdziko muli kuwukirana, dzikolo limakhala ndi olamulira ambiri,koma anthu omvetsa ndi odziwa zinthu bwino ndiwo angakhazikitse bata mʼdzikolo nthawi yayitali. 3 Munthu wosauka amene amapondereza osauka anzakeali ngati mvula yamkuntho imene imawononga mbewu mʼmunda. 4 Amene amakana malamulo amatamanda anthu oyipa,koma amene amasunga malamulo amatsutsana nawo. 5 Anthu oyipa samvetsa za chiweruzo cholungama,koma amene amafuna kuchita zimene Yehova afuna amachimvetsetsa bwino. 6 Munthu wosauka wa makhalidwe abwinoaposa munthu wolemera wa makhalidwe okhotakhota. 7 Amene amasunga malamulo ndi mwana wozindikira zinthu,koma amene amayenda ndi anthu adyera amachititsa manyazi abambo ake. 8 Amene amachulukitsa chuma chake polandira chiwongoladzanja chochulukaamakundikira chumacho anthu ena, amene adzachitira chifundo anthu osauka. 9 Wokana kumvera malamulongakhale pemphero lake lomwe limamunyansa Yehova. 10 Amene amatsogolera anthu olungama kuti ayende mʼnjira yoyipaadzagwera mu msampha wake womwe,koma anthu opanda cholakwa adzalandira cholowa chabwino. 11 Munthu wolemera amadziyesa kuti ndi wanzeru,koma munthu wosauka amene ali ndi nzeru zodziwa zinthu amamutulukira. 12 Pamene olungama apambana pamakhala chikondwerero chachikulu;koma pamene anthu oyipa apatsidwa ulamuliro, anthu amabisala. 13 Wobisa machimo ake sadzaona mwayi,koma aliyense amene awulula ndi kuleka machimowo, adzalandira chifundo. 14 Ndi wodala munthu amene amaopa Yehova nthawi zonse,koma amene aumitsa mtima wake adzagwa mʼmavuto. 15 Ngati mkango wobuma kapena chimbalangondo cholusandi mmenenso amakhalira munthu woyipa akamalamulira anthu osauka. 16 Wolamulira amene samvetsa zinthu ndiye amakhala wankhanzakoma amene amadana ndi phindu lopeza mwachinyengo adzakhala ndi moyo wautali. 17 Munthu amene wapalamula mlandu wopha munthuadzakhala wothawathawa mpaka imfa yake;wina aliyense asamuthandize. 18 Amene amayenda mokhulupirika adzapulumutsidwakoma amene njira zake ndi zokhotakhota adzagwa mʼdzenje. 19 Amene amalima mʼmunda mwake adzakhala ndi chakudya chochuluka,koma amene amangosewera adzakhala mʼmphawi. 20 Munthu wokhulupirika adzadalitsika kwambiri,koma wofuna kulemera mofulumira adzalangidwa. 21 Kukondera si kwabwino,ena amachita zolakwazo chifukwa cha kachidutswa ka buledi. 22 Munthu wowumira amafunitsitsa kulemerakoma sazindikira kuti umphawi udzamugwera. 23 Amene amadzudzula mnzake potsiriza pakemnzakeyo adzamukonda kwambiri, kupambana amene amanena mawu oshashalika. 24 Amene amabera abambo ake kapena amayi akenamanena kuti “kumeneko sikulakwa,”ndi mnzake wa munthu amene amasakaza. 25 Munthu wadyera amayambitsa mikangano,koma amene amadalira Yehova adzalemera. 26 Amene amadzidalira yekha ndi chitsiru,koma amene amatsata nzeru za ena adzapulumuka. 27 Amene amapereka kwa osauka sadzasowa kanthu,koma amene amatsinzina maso ake adzatembereredwa kwambiri. 28 Pamene anthu oyipa apatsidwa ulamuliro anthu amabisala,koma anthu oyipa akawonongeka olungama amapeza bwino.
In Other Versions
Proverbs 28 in the ANGEFD
Proverbs 28 in the ANTPNG2D
Proverbs 28 in the AS21
Proverbs 28 in the BAGH
Proverbs 28 in the BBPNG
Proverbs 28 in the BBT1E
Proverbs 28 in the BDS
Proverbs 28 in the BEV
Proverbs 28 in the BHAD
Proverbs 28 in the BIB
Proverbs 28 in the BLPT
Proverbs 28 in the BNT
Proverbs 28 in the BNTABOOT
Proverbs 28 in the BNTLV
Proverbs 28 in the BOATCB
Proverbs 28 in the BOATCB2
Proverbs 28 in the BOBCV
Proverbs 28 in the BOCNT
Proverbs 28 in the BOECS
Proverbs 28 in the BOHCB
Proverbs 28 in the BOHCV
Proverbs 28 in the BOHLNT
Proverbs 28 in the BOHNTLTAL
Proverbs 28 in the BOICB
Proverbs 28 in the BOILNTAP
Proverbs 28 in the BOITCV
Proverbs 28 in the BOKCV
Proverbs 28 in the BOKCV2
Proverbs 28 in the BOKHWOG
Proverbs 28 in the BOKSSV
Proverbs 28 in the BOLCB
Proverbs 28 in the BOLCB2
Proverbs 28 in the BOMCV
Proverbs 28 in the BONAV
Proverbs 28 in the BONCB
Proverbs 28 in the BONLT
Proverbs 28 in the BONUT2
Proverbs 28 in the BOPLNT
Proverbs 28 in the BOSCB
Proverbs 28 in the BOSNC
Proverbs 28 in the BOTLNT
Proverbs 28 in the BOVCB
Proverbs 28 in the BOYCB
Proverbs 28 in the BPBB
Proverbs 28 in the BPH
Proverbs 28 in the BSB
Proverbs 28 in the CCB
Proverbs 28 in the CUV
Proverbs 28 in the CUVS
Proverbs 28 in the DBT
Proverbs 28 in the DGDNT
Proverbs 28 in the DHNT
Proverbs 28 in the DNT
Proverbs 28 in the ELBE
Proverbs 28 in the EMTV
Proverbs 28 in the ESV
Proverbs 28 in the FBV
Proverbs 28 in the FEB
Proverbs 28 in the GGMNT
Proverbs 28 in the GNT
Proverbs 28 in the HARY
Proverbs 28 in the HNT
Proverbs 28 in the IRVA
Proverbs 28 in the IRVB
Proverbs 28 in the IRVG
Proverbs 28 in the IRVH
Proverbs 28 in the IRVK
Proverbs 28 in the IRVM
Proverbs 28 in the IRVM2
Proverbs 28 in the IRVO
Proverbs 28 in the IRVP
Proverbs 28 in the IRVT
Proverbs 28 in the IRVT2
Proverbs 28 in the IRVU
Proverbs 28 in the ISVN
Proverbs 28 in the JSNT
Proverbs 28 in the KAPI
Proverbs 28 in the KBT1ETNIK
Proverbs 28 in the KBV
Proverbs 28 in the KJV
Proverbs 28 in the KNFD
Proverbs 28 in the LBA
Proverbs 28 in the LBLA
Proverbs 28 in the LNT
Proverbs 28 in the LSV
Proverbs 28 in the MAAL
Proverbs 28 in the MBV
Proverbs 28 in the MBV2
Proverbs 28 in the MHNT
Proverbs 28 in the MKNFD
Proverbs 28 in the MNG
Proverbs 28 in the MNT
Proverbs 28 in the MNT2
Proverbs 28 in the MRS1T
Proverbs 28 in the NAA
Proverbs 28 in the NASB
Proverbs 28 in the NBLA
Proverbs 28 in the NBS
Proverbs 28 in the NBVTP
Proverbs 28 in the NET2
Proverbs 28 in the NIV11
Proverbs 28 in the NNT
Proverbs 28 in the NNT2
Proverbs 28 in the NNT3
Proverbs 28 in the PDDPT
Proverbs 28 in the PFNT
Proverbs 28 in the RMNT
Proverbs 28 in the SBIAS
Proverbs 28 in the SBIBS
Proverbs 28 in the SBIBS2
Proverbs 28 in the SBICS
Proverbs 28 in the SBIDS
Proverbs 28 in the SBIGS
Proverbs 28 in the SBIHS
Proverbs 28 in the SBIIS
Proverbs 28 in the SBIIS2
Proverbs 28 in the SBIIS3
Proverbs 28 in the SBIKS
Proverbs 28 in the SBIKS2
Proverbs 28 in the SBIMS
Proverbs 28 in the SBIOS
Proverbs 28 in the SBIPS
Proverbs 28 in the SBISS
Proverbs 28 in the SBITS
Proverbs 28 in the SBITS2
Proverbs 28 in the SBITS3
Proverbs 28 in the SBITS4
Proverbs 28 in the SBIUS
Proverbs 28 in the SBIVS
Proverbs 28 in the SBT
Proverbs 28 in the SBT1E
Proverbs 28 in the SCHL
Proverbs 28 in the SNT
Proverbs 28 in the SUSU
Proverbs 28 in the SUSU2
Proverbs 28 in the SYNO
Proverbs 28 in the TBIAOTANT
Proverbs 28 in the TBT1E
Proverbs 28 in the TBT1E2
Proverbs 28 in the TFTIP
Proverbs 28 in the TFTU
Proverbs 28 in the TGNTATF3T
Proverbs 28 in the THAI
Proverbs 28 in the TNFD
Proverbs 28 in the TNT
Proverbs 28 in the TNTIK
Proverbs 28 in the TNTIL
Proverbs 28 in the TNTIN
Proverbs 28 in the TNTIP
Proverbs 28 in the TNTIZ
Proverbs 28 in the TOMA
Proverbs 28 in the TTENT
Proverbs 28 in the UBG
Proverbs 28 in the UGV
Proverbs 28 in the UGV2
Proverbs 28 in the UGV3
Proverbs 28 in the VBL
Proverbs 28 in the VDCC
Proverbs 28 in the YALU
Proverbs 28 in the YAPE
Proverbs 28 in the YBVTP
Proverbs 28 in the ZBP