Revelation 19 (BOGWICC)

1 Zitatha izi, ndinamva chimene chinamveka ngati phokoso la gulu lalikulu mmwamba likufuwula kuti,“Haleluya!Chipulumutso ndi ulemerero ndi mphamvu ndi za Mulungu wathu, 2 pakuti chiweruzo chake ndi choona ndi cha chilungamo.Iye waweruza mkazi wadama wotchuka ujaamene anayipitsa dziko lonse lapansi ndi zigololo zake.Iye wabwezera pa mkaziyo magazi a atumiki ake.” 3 Ndipo anafuwulanso kuti,“Haleluya!Utsi wochokera kwa mkazi wadamayo udzakwera kumwamba mpaka muyaya.” 4 Akuluakulu 24 aja ndi zamoyo zinayi zija anadzigwetsa pansi kupembedza Mulungu amene anakhala pa mpando waufumu. Ndipo anafuwula kuti,“Ameni, Haleluya!” 5 Kenaka mawu anachoka ku mpando waufumu kuti,“Lemekezani Mulungu wathuinu nonse atumiki ake,inu amene mumamuopa,nonse angʼono ndi akulu!” 6 Kenaka ndinamva chimene chinamveka ngati gulu lalikulu, ngati mkokomo wamadzi othamanga ndipo ngati kugunda kwakukulu kwa bingu, ndipo anati,“Haleluya!Pakuti Ambuye Mulungu wathu Wamphamvuzonse akulamulira. 7 Tiyeni tisangalale ndi kukondwerandi kumutamanda!Pakuti nthawi ya ukwati wa Mwana Wankhosa yafika,ndipo Mkwatibwi wakonzekeratu. 8 Wapatsidwa nsalu yoyera kwambiri, yowala ndi yosadakuti avale.”(Nsalu yoyera kwambiri ikuyimira ntchito zolungama za oyera mtima). 9 Kenaka mngelo anandiwuza kuti, “Lemba kuti, Odala amene ayitanidwa ku phwando la ukwati wa Mwana Wankhosa.” Ndipo anatinso, “Awa ndiwo mawu woona a Mulungu.” 10 Pamenepo ndinadzigwetsa pa mapazi ake kumupembedza. Koma anandiwuza kuti, “Usatero ayi, ine ndine mtumiki mnzako ngati iwe yemwe, ndiponso ngati abale ako amene asunga umboni wa Yesu. Pembedza Mulungu. Pakuti umboni wa Yesu ndiye mzimu wa uneneri.” 11 Ndinaona kumwamba kutatsekuka ndipo patsogolo panga panali kavalo woyera, amene anakwerapo dzina lake linali Wokhulupirika ndiponso Woona. Poweruza ndi kuchita nkhondo, amachita molungama. 12 Maso ake anali ngati malawi amoto, ndipo pamutu pake panali zipewa zaufumu zambiri. Anali ndi dzina lolembedwa, lodziwika ndi Iye yekha, osati wina aliyense. 13 Iye anavala mkanjo woviyika mʼmagazi, ndipo dzina lake ndi Mawu a Mulungu. 14 Magulu ankhondo akumwamba ankamutsatira atakwera pa akavalo oyera, ndipo iwowo atavala nsalu zoyera kwambiri ndi zosada. 15 Mʼkamwa mwake munatuluka lupanga lakuthwa limene anati akaphe nalo mitundu ya anthu. Iye adzalamulira ndi ndodo yachitsulo. Iye anaponda choponderamo mphesa cha ukali wa Mulungu Wamphamvuzonse. 16 Pa chovala ndi pa ntchafu pake panalembedwa dzina ili:MFUMU YA MAFUMU NDI MBUYE WA AMBUYE. 17 Ndipo ndinaona mngelo atayimirira pa dzuwa amene anafuwula ndi mawu okweza kwa mbalame zonse zowuluka mlengalenga kuti, “Bwerani, sonkhanani pamodzi ku phwando lalikulu la Mulungu. 18 Kuti mudye mnofu wa mafumu, wa akulu a ankhondo, ndi wa anthu amphamvu, wa akavalo ndi okwerapo awo, ndi wa anthu onse, mfulu ndi akapolo, angʼono ndi aakulu.” 19 Kenaka ndinaona chirombo chija ndi mafumu a dziko lapansi ndi magulu ankhondo atasonkhana pamodzi kuti achite nkhondo ndi wokwera pa kavalo ndi ankhondo ake. 20 Koma chirombocho chinagwidwa pamodzi ndi mneneri wonyenga uja amene anachita zizindikiro zodabwitsa pamaso pake. Ndi zizindikirozi anasocheretsa amene analembedwa chizindikiro cha chirombocho napembedza fano lake. Onse awiri anaponyedwa amoyo mʼnyanja yamoto yasulufule wotentha. 21 Ena onse anaphedwa ndi lupanga lija linatuluka mʼkamwa mwa wokwera pa kavalo uja, ndipo mbalame zonse zinadya mokwanira mnofu wa anthu akufawo.

In Other Versions

Revelation 19 in the ANGEFD

Revelation 19 in the ANTPNG2D

Revelation 19 in the AS21

Revelation 19 in the BAGH

Revelation 19 in the BBPNG

Revelation 19 in the BBT1E

Revelation 19 in the BDS

Revelation 19 in the BEV

Revelation 19 in the BHAD

Revelation 19 in the BIB

Revelation 19 in the BLPT

Revelation 19 in the BNT

Revelation 19 in the BNTABOOT

Revelation 19 in the BNTLV

Revelation 19 in the BOATCB

Revelation 19 in the BOATCB2

Revelation 19 in the BOBCV

Revelation 19 in the BOCNT

Revelation 19 in the BOECS

Revelation 19 in the BOHCB

Revelation 19 in the BOHCV

Revelation 19 in the BOHLNT

Revelation 19 in the BOHNTLTAL

Revelation 19 in the BOICB

Revelation 19 in the BOILNTAP

Revelation 19 in the BOITCV

Revelation 19 in the BOKCV

Revelation 19 in the BOKCV2

Revelation 19 in the BOKHWOG

Revelation 19 in the BOKSSV

Revelation 19 in the BOLCB

Revelation 19 in the BOLCB2

Revelation 19 in the BOMCV

Revelation 19 in the BONAV

Revelation 19 in the BONCB

Revelation 19 in the BONLT

Revelation 19 in the BONUT2

Revelation 19 in the BOPLNT

Revelation 19 in the BOSCB

Revelation 19 in the BOSNC

Revelation 19 in the BOTLNT

Revelation 19 in the BOVCB

Revelation 19 in the BOYCB

Revelation 19 in the BPBB

Revelation 19 in the BPH

Revelation 19 in the BSB

Revelation 19 in the CCB

Revelation 19 in the CUV

Revelation 19 in the CUVS

Revelation 19 in the DBT

Revelation 19 in the DGDNT

Revelation 19 in the DHNT

Revelation 19 in the DNT

Revelation 19 in the ELBE

Revelation 19 in the EMTV

Revelation 19 in the ESV

Revelation 19 in the FBV

Revelation 19 in the FEB

Revelation 19 in the GGMNT

Revelation 19 in the GNT

Revelation 19 in the HARY

Revelation 19 in the HNT

Revelation 19 in the IRVA

Revelation 19 in the IRVB

Revelation 19 in the IRVG

Revelation 19 in the IRVH

Revelation 19 in the IRVK

Revelation 19 in the IRVM

Revelation 19 in the IRVM2

Revelation 19 in the IRVO

Revelation 19 in the IRVP

Revelation 19 in the IRVT

Revelation 19 in the IRVT2

Revelation 19 in the IRVU

Revelation 19 in the ISVN

Revelation 19 in the JSNT

Revelation 19 in the KAPI

Revelation 19 in the KBT1ETNIK

Revelation 19 in the KBV

Revelation 19 in the KJV

Revelation 19 in the KNFD

Revelation 19 in the LBA

Revelation 19 in the LBLA

Revelation 19 in the LNT

Revelation 19 in the LSV

Revelation 19 in the MAAL

Revelation 19 in the MBV

Revelation 19 in the MBV2

Revelation 19 in the MHNT

Revelation 19 in the MKNFD

Revelation 19 in the MNG

Revelation 19 in the MNT

Revelation 19 in the MNT2

Revelation 19 in the MRS1T

Revelation 19 in the NAA

Revelation 19 in the NASB

Revelation 19 in the NBLA

Revelation 19 in the NBS

Revelation 19 in the NBVTP

Revelation 19 in the NET2

Revelation 19 in the NIV11

Revelation 19 in the NNT

Revelation 19 in the NNT2

Revelation 19 in the NNT3

Revelation 19 in the PDDPT

Revelation 19 in the PFNT

Revelation 19 in the RMNT

Revelation 19 in the SBIAS

Revelation 19 in the SBIBS

Revelation 19 in the SBIBS2

Revelation 19 in the SBICS

Revelation 19 in the SBIDS

Revelation 19 in the SBIGS

Revelation 19 in the SBIHS

Revelation 19 in the SBIIS

Revelation 19 in the SBIIS2

Revelation 19 in the SBIIS3

Revelation 19 in the SBIKS

Revelation 19 in the SBIKS2

Revelation 19 in the SBIMS

Revelation 19 in the SBIOS

Revelation 19 in the SBIPS

Revelation 19 in the SBISS

Revelation 19 in the SBITS

Revelation 19 in the SBITS2

Revelation 19 in the SBITS3

Revelation 19 in the SBITS4

Revelation 19 in the SBIUS

Revelation 19 in the SBIVS

Revelation 19 in the SBT

Revelation 19 in the SBT1E

Revelation 19 in the SCHL

Revelation 19 in the SNT

Revelation 19 in the SUSU

Revelation 19 in the SUSU2

Revelation 19 in the SYNO

Revelation 19 in the TBIAOTANT

Revelation 19 in the TBT1E

Revelation 19 in the TBT1E2

Revelation 19 in the TFTIP

Revelation 19 in the TFTU

Revelation 19 in the TGNTATF3T

Revelation 19 in the THAI

Revelation 19 in the TNFD

Revelation 19 in the TNT

Revelation 19 in the TNTIK

Revelation 19 in the TNTIL

Revelation 19 in the TNTIN

Revelation 19 in the TNTIP

Revelation 19 in the TNTIZ

Revelation 19 in the TOMA

Revelation 19 in the TTENT

Revelation 19 in the UBG

Revelation 19 in the UGV

Revelation 19 in the UGV2

Revelation 19 in the UGV3

Revelation 19 in the VBL

Revelation 19 in the VDCC

Revelation 19 in the YALU

Revelation 19 in the YAPE

Revelation 19 in the YBVTP

Revelation 19 in the ZBP