Zechariah 8 (BOGWICC)

1 Awa ndi mawu amene Yehova Wamphamvuzonse ananena. 2 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Ine ndikuchitira nsanje yayikulu Ziyoni. Mtima wanga ukupweteka chifukwa cha nsanje pa iyeyo.” 3 Yehova akuti, “Ndidzabwerera ku Ziyoni ndi kukakhala ku Yerusalemu. Pamenepo Yerusalemu adzatchedwa Mzinda wa Choonadi ndipo phiri la Yehova Wamphamvuzonse lidzatchedwa Phiri Lopatulika.” 4 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Abambo ndi amayi okalamba adzakhalanso mʼmisewu ya mu Yerusalemu, aliyense ali ndi ndodo mʼmanja mwake chifukwa cha kuchuluka kwa masiku ake. 5 Ndipo misewu ya mu mzindamo idzadzaza ndi anyamata ndi atsikana akusewera.” 6 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Ngati zikuoneka kuti nʼzosatheka kwa anthu otsala pa nthawi ino, kodi zidzakhala zosathekanso kwa Ine?” akutero Yehova Wamphamvuzonse. 7 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Taonani ndidzapulumutsa anthu anga kuchokera ku mayiko a kummawa ndi kumadzulo. 8 Ndidzawabweretsa kuti adzakhale mu Yerusalemu; adzakhala anthu anga, ndipo Ine ndidzakhala Mulungu wawo, wokhulupirika ndi wolungama pakati pawo.” 9 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Inu amene tsopano mukumva mawu awa amene akuyankhula aneneri amene analipo pamene ankayika maziko a nyumba ya Yehova Wamphamvuzonse, ‘limbani mtima kuti mumange Nyumba ya Yehova.’ 10 Mpaka nthawi imeneyi panalibe munthu wolandira malipiro pa ntchito kapena ndalama zolipirira nyama zogwira ntchito. Panalibe munthu amene ankadzigwirira ntchito mwamtendere chifukwa choopa adani ake, pakuti Ine ndinkawayambanitsa. 11 Koma tsopano sindidzachitira otsala mwa anthu awa zomwe ndinachita kale,” akutero Yehova Wamphamvuzonse. 12 “Pakuti mbewu zidzamera bwino, mpesa udzabala zipatso zake, nthaka idzatulutsa zomera zake, ndi thambo lidzagwetsa mame. Ndidzapereka zonse kukhala cholowa cha otsala mwa anthu awa. 13 Monga mwakhala muli chinthu chotembereredwa pakati pa mitundu ina ya anthu, inu Yuda ndi Israeli, choncho ndidzakupulumutsani, ndipo mudzakhala dalitso. Musachite mantha, koma limbani mtima.” 14 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Monga ndinatsimikiza mtima kubweretsa choyipa pa inu, komanso osakuchitirani chisoni pamene makolo anu anandikwiyitsa,” akutero Yehova, 15 “Choncho tsopano ndatsimikiza mtima kuchitiranso zabwino Yerusalemu ndi Yuda. Musachite mantha. 16 Zinthu zoti muchite ndi izi: Muziwuzana zoona zokhazokha, muziweruza moona ndi mwachilungamo mʼmabwalo anu; 17 musamachitire mnzanu chiwembu, musamakonde kulumbira zonama. Zonsezi Ine ndimadana nazo,” akutero Yehova. 18 Yehova Wamphamvuzonse anayankhulanso nane. 19 Ndipo ananena kuti, “Kusala zakudya kwa pa mwezi wachinayi, chisanu, chisanu ndi chiwiri ndi wakhumi, kudzakhala nthawi yachimwemwe, ya chisangalalo ndi nthawi ya madyerero chikondwerero kwa Yuda. Nʼchifukwa chake muzikonda choonadi ndi mtendere.” 20 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Anthu a mitundu yambiri ndi anthu okhala mʼmizinda yambiri adzabwerabe, 21 ndipo nzika za mzinda wina zidzapita ku mzinda wina, kukanena kuti, ‘Tiyeni mwamsanga tikapemphe madalitso kwa Yehova ndi kukapembedza Yehova Wamphamvuzonse. Inenso ndikupita kumeneko.’ 22 Anthu ambiri ndiponso a ku mayiko amphamvu adzabwera ku Yerusalemu kudzapembedza Yehova Wamphamvuzonse ndi kudzapempha madalitso.” 23 Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Masiku amenewo anthu khumi ochokera ku mitundu ya anthu a ziyankhulo zosiyana adzagwira mkanjo wa Myuda ndi kunena kuti, ‘Tipite nawo, chifukwa tamva kuti Mulungu ali nanu.’ ”

In Other Versions

Zechariah 8 in the ANGEFD

Zechariah 8 in the ANTPNG2D

Zechariah 8 in the AS21

Zechariah 8 in the BAGH

Zechariah 8 in the BBPNG

Zechariah 8 in the BBT1E

Zechariah 8 in the BDS

Zechariah 8 in the BEV

Zechariah 8 in the BHAD

Zechariah 8 in the BIB

Zechariah 8 in the BLPT

Zechariah 8 in the BNT

Zechariah 8 in the BNTABOOT

Zechariah 8 in the BNTLV

Zechariah 8 in the BOATCB

Zechariah 8 in the BOATCB2

Zechariah 8 in the BOBCV

Zechariah 8 in the BOCNT

Zechariah 8 in the BOECS

Zechariah 8 in the BOHCB

Zechariah 8 in the BOHCV

Zechariah 8 in the BOHLNT

Zechariah 8 in the BOHNTLTAL

Zechariah 8 in the BOICB

Zechariah 8 in the BOILNTAP

Zechariah 8 in the BOITCV

Zechariah 8 in the BOKCV

Zechariah 8 in the BOKCV2

Zechariah 8 in the BOKHWOG

Zechariah 8 in the BOKSSV

Zechariah 8 in the BOLCB

Zechariah 8 in the BOLCB2

Zechariah 8 in the BOMCV

Zechariah 8 in the BONAV

Zechariah 8 in the BONCB

Zechariah 8 in the BONLT

Zechariah 8 in the BONUT2

Zechariah 8 in the BOPLNT

Zechariah 8 in the BOSCB

Zechariah 8 in the BOSNC

Zechariah 8 in the BOTLNT

Zechariah 8 in the BOVCB

Zechariah 8 in the BOYCB

Zechariah 8 in the BPBB

Zechariah 8 in the BPH

Zechariah 8 in the BSB

Zechariah 8 in the CCB

Zechariah 8 in the CUV

Zechariah 8 in the CUVS

Zechariah 8 in the DBT

Zechariah 8 in the DGDNT

Zechariah 8 in the DHNT

Zechariah 8 in the DNT

Zechariah 8 in the ELBE

Zechariah 8 in the EMTV

Zechariah 8 in the ESV

Zechariah 8 in the FBV

Zechariah 8 in the FEB

Zechariah 8 in the GGMNT

Zechariah 8 in the GNT

Zechariah 8 in the HARY

Zechariah 8 in the HNT

Zechariah 8 in the IRVA

Zechariah 8 in the IRVB

Zechariah 8 in the IRVG

Zechariah 8 in the IRVH

Zechariah 8 in the IRVK

Zechariah 8 in the IRVM

Zechariah 8 in the IRVM2

Zechariah 8 in the IRVO

Zechariah 8 in the IRVP

Zechariah 8 in the IRVT

Zechariah 8 in the IRVT2

Zechariah 8 in the IRVU

Zechariah 8 in the ISVN

Zechariah 8 in the JSNT

Zechariah 8 in the KAPI

Zechariah 8 in the KBT1ETNIK

Zechariah 8 in the KBV

Zechariah 8 in the KJV

Zechariah 8 in the KNFD

Zechariah 8 in the LBA

Zechariah 8 in the LBLA

Zechariah 8 in the LNT

Zechariah 8 in the LSV

Zechariah 8 in the MAAL

Zechariah 8 in the MBV

Zechariah 8 in the MBV2

Zechariah 8 in the MHNT

Zechariah 8 in the MKNFD

Zechariah 8 in the MNG

Zechariah 8 in the MNT

Zechariah 8 in the MNT2

Zechariah 8 in the MRS1T

Zechariah 8 in the NAA

Zechariah 8 in the NASB

Zechariah 8 in the NBLA

Zechariah 8 in the NBS

Zechariah 8 in the NBVTP

Zechariah 8 in the NET2

Zechariah 8 in the NIV11

Zechariah 8 in the NNT

Zechariah 8 in the NNT2

Zechariah 8 in the NNT3

Zechariah 8 in the PDDPT

Zechariah 8 in the PFNT

Zechariah 8 in the RMNT

Zechariah 8 in the SBIAS

Zechariah 8 in the SBIBS

Zechariah 8 in the SBIBS2

Zechariah 8 in the SBICS

Zechariah 8 in the SBIDS

Zechariah 8 in the SBIGS

Zechariah 8 in the SBIHS

Zechariah 8 in the SBIIS

Zechariah 8 in the SBIIS2

Zechariah 8 in the SBIIS3

Zechariah 8 in the SBIKS

Zechariah 8 in the SBIKS2

Zechariah 8 in the SBIMS

Zechariah 8 in the SBIOS

Zechariah 8 in the SBIPS

Zechariah 8 in the SBISS

Zechariah 8 in the SBITS

Zechariah 8 in the SBITS2

Zechariah 8 in the SBITS3

Zechariah 8 in the SBITS4

Zechariah 8 in the SBIUS

Zechariah 8 in the SBIVS

Zechariah 8 in the SBT

Zechariah 8 in the SBT1E

Zechariah 8 in the SCHL

Zechariah 8 in the SNT

Zechariah 8 in the SUSU

Zechariah 8 in the SUSU2

Zechariah 8 in the SYNO

Zechariah 8 in the TBIAOTANT

Zechariah 8 in the TBT1E

Zechariah 8 in the TBT1E2

Zechariah 8 in the TFTIP

Zechariah 8 in the TFTU

Zechariah 8 in the TGNTATF3T

Zechariah 8 in the THAI

Zechariah 8 in the TNFD

Zechariah 8 in the TNT

Zechariah 8 in the TNTIK

Zechariah 8 in the TNTIL

Zechariah 8 in the TNTIN

Zechariah 8 in the TNTIP

Zechariah 8 in the TNTIZ

Zechariah 8 in the TOMA

Zechariah 8 in the TTENT

Zechariah 8 in the UBG

Zechariah 8 in the UGV

Zechariah 8 in the UGV2

Zechariah 8 in the UGV3

Zechariah 8 in the VBL

Zechariah 8 in the VDCC

Zechariah 8 in the YALU

Zechariah 8 in the YAPE

Zechariah 8 in the YBVTP

Zechariah 8 in the ZBP