Joshua 5 (BOGWICC)
1 Mafumu onse a Aamori, a kummawa kwa Yorodani ndi mafumu onse a Akanaani a mʼmbali mwa Nyanja anamva momwe Yehova anawumitsira Yorodani pamene Aisraeli ankawoloka. Choncho anachita mantha ndi kutayiratu mtima chifukwa cha Aisraeliwo. 2 Tsono Yehova anati kwa Yoswa, “Panga mipeni ya miyala ndipo uchitenso mwambo wa mdulidwe pa Aisraeli.” 3 Choncho Yoswa anapanga mipeni ya miyala ndi kuchita mdulidwe Aisraeli ku Gibeyati Haaraloti. 4 Chifukwa chimene Yoswa anachitira izi ndi ichi: Onse amene anatuluka mʼdziko la Igupto, amuna onse amene anali oyenera kumenya nkhondo anatha kufa mʼchipululu atatuluka mʼdziko la Igupto. 5 Anthu onse amene anatuluka mʼdziko la Igupto anali atachita mwambo wa mdulidwe, koma onse amene anabadwira mʼchipululu, pa ulendo wochoka ku Igupto, sanachite. 6 Aisraeli anakhala akuyenda mʼchipululu kwa zaka makumi anayi mpaka amuna onse amene potuluka mʼdziko la Igupto anali a msinkhu woyenera kupita ku nkhondo anamwalira. Iwo anafa chifukwa sanamvere mawu a Yehova. Yehova anawalumbirira kuti sadzalowa konse mʼdziko loyenda mkaka ndi uchi limene analonjeza kwa makolo awo kuti adzatipatsa. 7 Koma ana awo amene analowa mʼmalo mwawo ndiwo amene Yoswa anawachita mdulidwe popeza sanachite pamene anali pa ulendo wawo mʼchipululu muja. 8 Atamaliza kuchita mdulidwe uja, anthu onse anakakhala ku misasa yawo kudikira kuti zilonda zipole. 9 Kenaka Yehova anati kwa Yoswa, “Kuyambira tsopano anthu a ku Igupto sadzakunyozaninso.” Nʼchifukwa chake malowa anatchedwa Giligala mpaka lero. 10 Akupumulabe ku Giligala kuja mʼchigwa cha Yeriko, Aisraeli anachita chikondwerero cha Paska madzulo pa tsiku la 14 la mwezi woyamba womwewo. 11 Mmawa mwake ndi pamene anayamba kudya zakudya za mʼdziko la Kanaani. Anaphika buledi wopanda yisiti ndi kukazinga tirigu tsiku lomwelo. 12 Atangodya chakudya cha mʼdzikomo, mana anasiya kugwa, ndipo sanapezekenso. Kuyambira nthawi imeneyo Aisraeli anayamba kudya chakudya cha mʼdziko la Kanaani. 13 Tsiku lina pamene Yoswa anali pafupi ndi Yeriko, anakweza maso ake ndipo mwadzidzidzi anaona munthu atayima patsogolo pake ndi lupanga losolola mʼdzanja lake. Yoswa anapita pamene panali munthuyo ndipo anamufunsa kuti, “Kodi uli mbali yathu kapena ya adani athu?” 14 Iye anayankha kuti “Sindili mbali iliyonse. Ndabwera monga mkulu wa asilikali a Yehova.” Pomwepo Yoswa anadzigwetsa chafufumimba kupereka ulemu, ndipo anamufunsa, “Kodi mbuye wanga muli ndi uthenga wotani kwa mtumiki wanu?” 15 Mkulu wa asilikali a Yehova uja anayankha kuti, “Vula nsapato zako, pakuti wayima pa malo wopatulika.” Ndipo Yoswa anachitadi zimene anawuzidwazo.
In Other Versions
Joshua 5 in the ANGEFD
Joshua 5 in the ANTPNG2D
Joshua 5 in the AS21
Joshua 5 in the BAGH
Joshua 5 in the BBPNG
Joshua 5 in the BBT1E
Joshua 5 in the BDS
Joshua 5 in the BEV
Joshua 5 in the BHAD
Joshua 5 in the BIB
Joshua 5 in the BLPT
Joshua 5 in the BNT
Joshua 5 in the BNTABOOT
Joshua 5 in the BNTLV
Joshua 5 in the BOATCB
Joshua 5 in the BOATCB2
Joshua 5 in the BOBCV
Joshua 5 in the BOCNT
Joshua 5 in the BOECS
Joshua 5 in the BOHCB
Joshua 5 in the BOHCV
Joshua 5 in the BOHLNT
Joshua 5 in the BOHNTLTAL
Joshua 5 in the BOICB
Joshua 5 in the BOILNTAP
Joshua 5 in the BOITCV
Joshua 5 in the BOKCV
Joshua 5 in the BOKCV2
Joshua 5 in the BOKHWOG
Joshua 5 in the BOKSSV
Joshua 5 in the BOLCB
Joshua 5 in the BOLCB2
Joshua 5 in the BOMCV
Joshua 5 in the BONAV
Joshua 5 in the BONCB
Joshua 5 in the BONLT
Joshua 5 in the BONUT2
Joshua 5 in the BOPLNT
Joshua 5 in the BOSCB
Joshua 5 in the BOSNC
Joshua 5 in the BOTLNT
Joshua 5 in the BOVCB
Joshua 5 in the BOYCB
Joshua 5 in the BPBB
Joshua 5 in the BPH
Joshua 5 in the BSB
Joshua 5 in the CCB
Joshua 5 in the CUV
Joshua 5 in the CUVS
Joshua 5 in the DBT
Joshua 5 in the DGDNT
Joshua 5 in the DHNT
Joshua 5 in the DNT
Joshua 5 in the ELBE
Joshua 5 in the EMTV
Joshua 5 in the ESV
Joshua 5 in the FBV
Joshua 5 in the FEB
Joshua 5 in the GGMNT
Joshua 5 in the GNT
Joshua 5 in the HARY
Joshua 5 in the HNT
Joshua 5 in the IRVA
Joshua 5 in the IRVB
Joshua 5 in the IRVG
Joshua 5 in the IRVH
Joshua 5 in the IRVK
Joshua 5 in the IRVM
Joshua 5 in the IRVM2
Joshua 5 in the IRVO
Joshua 5 in the IRVP
Joshua 5 in the IRVT
Joshua 5 in the IRVT2
Joshua 5 in the IRVU
Joshua 5 in the ISVN
Joshua 5 in the JSNT
Joshua 5 in the KAPI
Joshua 5 in the KBT1ETNIK
Joshua 5 in the KBV
Joshua 5 in the KJV
Joshua 5 in the KNFD
Joshua 5 in the LBA
Joshua 5 in the LBLA
Joshua 5 in the LNT
Joshua 5 in the LSV
Joshua 5 in the MAAL
Joshua 5 in the MBV
Joshua 5 in the MBV2
Joshua 5 in the MHNT
Joshua 5 in the MKNFD
Joshua 5 in the MNG
Joshua 5 in the MNT
Joshua 5 in the MNT2
Joshua 5 in the MRS1T
Joshua 5 in the NAA
Joshua 5 in the NASB
Joshua 5 in the NBLA
Joshua 5 in the NBS
Joshua 5 in the NBVTP
Joshua 5 in the NET2
Joshua 5 in the NIV11
Joshua 5 in the NNT
Joshua 5 in the NNT2
Joshua 5 in the NNT3
Joshua 5 in the PDDPT
Joshua 5 in the PFNT
Joshua 5 in the RMNT
Joshua 5 in the SBIAS
Joshua 5 in the SBIBS
Joshua 5 in the SBIBS2
Joshua 5 in the SBICS
Joshua 5 in the SBIDS
Joshua 5 in the SBIGS
Joshua 5 in the SBIHS
Joshua 5 in the SBIIS
Joshua 5 in the SBIIS2
Joshua 5 in the SBIIS3
Joshua 5 in the SBIKS
Joshua 5 in the SBIKS2
Joshua 5 in the SBIMS
Joshua 5 in the SBIOS
Joshua 5 in the SBIPS
Joshua 5 in the SBISS
Joshua 5 in the SBITS
Joshua 5 in the SBITS2
Joshua 5 in the SBITS3
Joshua 5 in the SBITS4
Joshua 5 in the SBIUS
Joshua 5 in the SBIVS
Joshua 5 in the SBT
Joshua 5 in the SBT1E
Joshua 5 in the SCHL
Joshua 5 in the SNT
Joshua 5 in the SUSU
Joshua 5 in the SUSU2
Joshua 5 in the SYNO
Joshua 5 in the TBIAOTANT
Joshua 5 in the TBT1E
Joshua 5 in the TBT1E2
Joshua 5 in the TFTIP
Joshua 5 in the TFTU
Joshua 5 in the TGNTATF3T
Joshua 5 in the THAI
Joshua 5 in the TNFD
Joshua 5 in the TNT
Joshua 5 in the TNTIK
Joshua 5 in the TNTIL
Joshua 5 in the TNTIN
Joshua 5 in the TNTIP
Joshua 5 in the TNTIZ
Joshua 5 in the TOMA
Joshua 5 in the TTENT
Joshua 5 in the UBG
Joshua 5 in the UGV
Joshua 5 in the UGV2
Joshua 5 in the UGV3
Joshua 5 in the VBL
Joshua 5 in the VDCC
Joshua 5 in the YALU
Joshua 5 in the YAPE
Joshua 5 in the YBVTP
Joshua 5 in the ZBP