Lamentations 2 (BOGWICC)

1 Haa, Ambuye waphimba mwana wamkazi wa Ziyonindi mtambo wa mkwiyo wake!Iye wataya pansi ulemerero wa Israelikuchoka kumwamba.Pa tsiku la mkwiyo wake Iye sanakumbukirensopopondapo mapazi ake. 2 Ambuye anawononga midzi yonse ya Yakobo mopanda chifundo;mu mkwiyo wake anagwetsamalinga a mwana wamkazi wa Yuda.Anagwetsa pansi mochititsa manyazimaufumu ndi akalonga ake. 3 Atakwiya kwambiri, Ambuye anathyolanyanga iliyonse ya Israeli.Anabweza dzanja lake lamanjapamene mdani anamuyandikira.Ambuye anatentha fuko la Yakobo ngati moto wonyeketsaumene umawononga zinthu zonse zomwe zili pafupi. 4 Wakokera uta wake pa ife ngati ndife adani;wayimiritsa dzanja lake pa ife ngati ndife adani,ndipo anapha onse amene tinkawayangʼana monyadira.Ukali wake ukuyaka ngati motopa tenti ya mwana wamkazi wa Ziyoni. 5 Ambuye ali ngati mdani;wawonongeratu Israeli;wawonongeratu nyumba zake zonse zaufumundipo wawononga malinga ake.Iye wachulukitsa kubuma ndi kulirakwa mwana wamkazi wa Yuda. 6 Wagwetsa malo ake okhalamo ngati khumbi la mʼmunda;wawononga malo ake a msonkhano.Yehova wayiwalitsa Ziyonimaphwando ake oyikika ndi masabata ake.Mokwiya kwambiri, Iye ananyozamfumu ndi wansembe. 7 Ambuye wakana guwa lake la nsembendipo wasiya malo ake opatulika.Iye wapereka makoma a nyumba zake zaufumukwa mdani wake;adaniwo anafuwula mʼnyumba ya Yehovangati kuti ndi pa tsiku la chikondwerero. 8 Yehova anatsimikiza kugwetsamakoma a mwana wamkazi wa Ziyoni.Anawayesa ndi chingwendipo sanafune kuleka kuwagwetsa.Analiritsa malinga ndi makoma;onse anawonongeka pamodzi. 9 Zipata za Yerusalemu zalowa pansi;wathyola ndi kuwononga mipiringidzo yake.Mfumu ndi akalonga ake agwidwa ukapolo pakati pa mitundu ya anthu,palibenso lamulo,ndipo aneneri ake sakupezamasomphenya kuchokera kwa Yehova. 10 Akuluakulu a mwana wamkazi wa Ziyoniakhala chete pansi;awaza fumbi pa mitu yawondipo avala ziguduli.Anamwali a Yerusalemuaweramitsa mitu yawo pansi. 11 Maso anga atopa ndi kulira,ndazunzika mʼmoyo mwanga,mtima wanga wadzaza ndi chisonichifukwa anthu anga akuwonongeka,chifukwa ana ndi makanda akukomokamʼmisewu ya mu mzinda. 12 Anawo akufunsa amayi awo kuti,“Kodi tirigu ndi vinyo zili kuti?”pamene akukomoka ngati anthu olasidwamʼmisewu ya mʼmizinda,pamene miyoyo yawo ikufowokamʼmanja mwa amayi awo. 13 Ndinganene chiyani za iwe?Ndingakufanizire ndi chiyani,iwe mwana wamkazi wa Yerusalemu?Kodi ndingakufanizire ndi yanikuti ndikutonthoze,iwe namwali wa Ziyoni?Chilonda chako ndi chozama ngati nyanja,kodi ndani angakuchiritse? 14 Masomphenya a aneneri akoanali abodza ndi achabechabe.Iwo sanakupulumutse kuti usapite ku ukapolopoyika poyera mphulupulu zako.Mauthenga amene anakupatsaanali achabechabe ndi osocheretsa. 15 Onse oyenda mʼnjira yakoakukuwombera mʼmanja;akugwedeza mitu yawo ndi kukunyodolaiwe mwana wamkazi wa Yerusalemu:“Kodi mzinda uja ndi uwu umene unkatchedwawokongola kotheratu,chimwemwe cha dziko lonse lapansi?” 16 Adani ako onse akutsekulira pakamwa ndi kukunyoza;iwo akunyogodola ndi kukukuta mano awo,ndipo akuti, “Tamumeza.Tsiku ili ndi lomwe timayembekezera;tili ndi moyo kuti tilione.” 17 Yehova wachita chimene anakonzeratu;wakwaniritsa mawu ake,amene anatsimikiza kale lomwe.Wakuwononga mopanda chifundo,walola mdani kuti akondwere chifukwa cha kugwa kwako,wakweza mphamvu za adani ako. 18 Mitima ya anthuikufuwulira Ambuye.Iwe khoma la mwana wamkazi wa Ziyoni,misozi yako itsike ngati mtsinjeusana ndi usiku;usadzipatse wekha mpumulo,maso ako asaleke kukhetsa misozi. 19 Dzuka, fuwula usiku,pamene alonda ayamba kulondera;khuthula mtima wako ngati madzipamaso pa Ambuye.Kweza manja ako kwa Iyechifukwa cha miyoyo ya ana ako,amene akukomoka ndi njalamʼmisewu yonse ya mu mzinda. 20 Inu Yehova, onani, ndipo ganizirani:kodi ndani amene mwamuchitirapo zinthu ngati izi?Kodi amayi adye ana awo,amene amawasamalira?Kodi ansembe ndi aneneri awapheremʼmalo opatulika a Ambuye? 21 Anyamata ndi okalamba aligone pamodzipa fumbi la mʼmisewu ya mu mzinda;anyamata anga ndi anamwali angaaphedwa ndi lupanga.Inu Yehova mwawapha pa tsiku la mkwiyo wanu;mwawapha mopanda chifundo. 22 Ngati momwe mumayitanira pa tsiku la phwando,chimodzimodzinso mwandiyitanira zoopsa mbali zonse.Pa tsiku limene Yehova wakwiyapalibe amene angathawe ndi kukhala ndi moyo;mdani wanga wawonongaonse amene ndinkawasamala ndi kuwalera.

In Other Versions

Lamentations 2 in the ANGEFD

Lamentations 2 in the ANTPNG2D

Lamentations 2 in the AS21

Lamentations 2 in the BAGH

Lamentations 2 in the BBPNG

Lamentations 2 in the BBT1E

Lamentations 2 in the BDS

Lamentations 2 in the BEV

Lamentations 2 in the BHAD

Lamentations 2 in the BIB

Lamentations 2 in the BLPT

Lamentations 2 in the BNT

Lamentations 2 in the BNTABOOT

Lamentations 2 in the BNTLV

Lamentations 2 in the BOATCB

Lamentations 2 in the BOATCB2

Lamentations 2 in the BOBCV

Lamentations 2 in the BOCNT

Lamentations 2 in the BOECS

Lamentations 2 in the BOHCB

Lamentations 2 in the BOHCV

Lamentations 2 in the BOHLNT

Lamentations 2 in the BOHNTLTAL

Lamentations 2 in the BOICB

Lamentations 2 in the BOILNTAP

Lamentations 2 in the BOITCV

Lamentations 2 in the BOKCV

Lamentations 2 in the BOKCV2

Lamentations 2 in the BOKHWOG

Lamentations 2 in the BOKSSV

Lamentations 2 in the BOLCB

Lamentations 2 in the BOLCB2

Lamentations 2 in the BOMCV

Lamentations 2 in the BONAV

Lamentations 2 in the BONCB

Lamentations 2 in the BONLT

Lamentations 2 in the BONUT2

Lamentations 2 in the BOPLNT

Lamentations 2 in the BOSCB

Lamentations 2 in the BOSNC

Lamentations 2 in the BOTLNT

Lamentations 2 in the BOVCB

Lamentations 2 in the BOYCB

Lamentations 2 in the BPBB

Lamentations 2 in the BPH

Lamentations 2 in the BSB

Lamentations 2 in the CCB

Lamentations 2 in the CUV

Lamentations 2 in the CUVS

Lamentations 2 in the DBT

Lamentations 2 in the DGDNT

Lamentations 2 in the DHNT

Lamentations 2 in the DNT

Lamentations 2 in the ELBE

Lamentations 2 in the EMTV

Lamentations 2 in the ESV

Lamentations 2 in the FBV

Lamentations 2 in the FEB

Lamentations 2 in the GGMNT

Lamentations 2 in the GNT

Lamentations 2 in the HARY

Lamentations 2 in the HNT

Lamentations 2 in the IRVA

Lamentations 2 in the IRVB

Lamentations 2 in the IRVG

Lamentations 2 in the IRVH

Lamentations 2 in the IRVK

Lamentations 2 in the IRVM

Lamentations 2 in the IRVM2

Lamentations 2 in the IRVO

Lamentations 2 in the IRVP

Lamentations 2 in the IRVT

Lamentations 2 in the IRVT2

Lamentations 2 in the IRVU

Lamentations 2 in the ISVN

Lamentations 2 in the JSNT

Lamentations 2 in the KAPI

Lamentations 2 in the KBT1ETNIK

Lamentations 2 in the KBV

Lamentations 2 in the KJV

Lamentations 2 in the KNFD

Lamentations 2 in the LBA

Lamentations 2 in the LBLA

Lamentations 2 in the LNT

Lamentations 2 in the LSV

Lamentations 2 in the MAAL

Lamentations 2 in the MBV

Lamentations 2 in the MBV2

Lamentations 2 in the MHNT

Lamentations 2 in the MKNFD

Lamentations 2 in the MNG

Lamentations 2 in the MNT

Lamentations 2 in the MNT2

Lamentations 2 in the MRS1T

Lamentations 2 in the NAA

Lamentations 2 in the NASB

Lamentations 2 in the NBLA

Lamentations 2 in the NBS

Lamentations 2 in the NBVTP

Lamentations 2 in the NET2

Lamentations 2 in the NIV11

Lamentations 2 in the NNT

Lamentations 2 in the NNT2

Lamentations 2 in the NNT3

Lamentations 2 in the PDDPT

Lamentations 2 in the PFNT

Lamentations 2 in the RMNT

Lamentations 2 in the SBIAS

Lamentations 2 in the SBIBS

Lamentations 2 in the SBIBS2

Lamentations 2 in the SBICS

Lamentations 2 in the SBIDS

Lamentations 2 in the SBIGS

Lamentations 2 in the SBIHS

Lamentations 2 in the SBIIS

Lamentations 2 in the SBIIS2

Lamentations 2 in the SBIIS3

Lamentations 2 in the SBIKS

Lamentations 2 in the SBIKS2

Lamentations 2 in the SBIMS

Lamentations 2 in the SBIOS

Lamentations 2 in the SBIPS

Lamentations 2 in the SBISS

Lamentations 2 in the SBITS

Lamentations 2 in the SBITS2

Lamentations 2 in the SBITS3

Lamentations 2 in the SBITS4

Lamentations 2 in the SBIUS

Lamentations 2 in the SBIVS

Lamentations 2 in the SBT

Lamentations 2 in the SBT1E

Lamentations 2 in the SCHL

Lamentations 2 in the SNT

Lamentations 2 in the SUSU

Lamentations 2 in the SUSU2

Lamentations 2 in the SYNO

Lamentations 2 in the TBIAOTANT

Lamentations 2 in the TBT1E

Lamentations 2 in the TBT1E2

Lamentations 2 in the TFTIP

Lamentations 2 in the TFTU

Lamentations 2 in the TGNTATF3T

Lamentations 2 in the THAI

Lamentations 2 in the TNFD

Lamentations 2 in the TNT

Lamentations 2 in the TNTIK

Lamentations 2 in the TNTIL

Lamentations 2 in the TNTIN

Lamentations 2 in the TNTIP

Lamentations 2 in the TNTIZ

Lamentations 2 in the TOMA

Lamentations 2 in the TTENT

Lamentations 2 in the UBG

Lamentations 2 in the UGV

Lamentations 2 in the UGV2

Lamentations 2 in the UGV3

Lamentations 2 in the VBL

Lamentations 2 in the VDCC

Lamentations 2 in the YALU

Lamentations 2 in the YAPE

Lamentations 2 in the YBVTP

Lamentations 2 in the ZBP