Isaiah 33 (BOGWICC)

1 Tsoka kwa iwe, iwe wowonongawe,amene sunawonongedwepo!Tsoka kwa iwe, iwe mthirakuwiri,iwe amene sunanyengedwepo!Iwe ukadzaleka kuwononga,udzawonongedwa,ukadzasiya umʼthirakuwiri, adzakuwononga,ndipo ukadzaleka kuchita zachinyengo adzakunyenga. 2 Inu Yehova, mutikomere mtima ife;tikulakalaka Inu.Tsiku ndi tsiku mutitchinjirize ndi mkono wanu,ndipo mutipulumutse pa nthawi ya masautso. 3 Mukatulutsa liwu lanu longa bingu mitundu ya anthu imathawa;pamene Inu mwadzambatuka mitundu ya anthu imabalalika. 4 Zofunkha za ku nkhondo za mitundu ina Aisraeli adzazisonkhanitsa ngati mmene limachitira dzombe.Iwo adzalumphira zofunkhazo monga mmene limachitira dzombe. 5 Yehova wakwezeka kwambiri pakuti amakhala pamwamba pa zonseadzadzaza Ziyoni ndi chilungamo ndi chipulumutso. 6 Iye adzakupatsani mtendere pa nthawi yanu,adzakupatsani chipulumutso chochuluka, nzeru zambiri ndi chidziwitso chochuluka;kuopa Yehova ngati madalitso. 7 Taonani, anthu awo amphamvu akulira mofuwula mʼmisewu;akazembe okhazikitsa mtendere akulira kwambiri. 8 Mʼmisewu yayikulu mulibe anthu,mʼmisewu mulibe anthu a paulendo.Mdaniyo ndi wosasunga pangano.Iye amanyoza mboni.Palibe kulemekezana. 9 Dziko likulira ndipo likunka likutha.Nkhalango ya Lebanoni ikuchita manyazi, yafota.Chigwa cha chonde cha Saroni chasanduka chachidalala.Masamba a mitengo ya ku Basani ndi Karimeli akuyoyoka. 10 Yehova akunena kuti, “Tsopano ndidzadzambatukandipo ndidzaonetsa mphamvu zanga,ndipo ndidzakwezedwa. 11 Zolingalira zanu nʼzachabechabengati udzu wamanyowa.Mpweya wamoto udzakupserezani. 12 Anthu a mitundu ina adzatenthedwa ngati miyala ya njereza;ndi ngati minga yodulidwa.” 13 Inu amene muli kutali, imvani zimene ndachita;inu amene muli pafupi, dziwani mphamvu zanga 14 Mu mzinda wa Ziyoni anthu ochimwa agwidwa ndi mantha;anthu osapembedza Mulungu akunjenjemera:Iwo akunena kuti, “Ndani wa ife angathe kukhala mʼmoto wonyeketsa?Ndani wa ife angathe kukhala moto wosatha?” 15 Angathe kuti ndi amene amachita zolungamandi kuyankhula zoona,amene amakana phindu lolipeza monyengandipo salola manja ake kulandira ziphuphu,amene amatseka makutu ake kuti angamve mawu opangana kupha anzawondipo amatsinzina kuti angaone zoyipa. 16 Munthu wotere ndiye adzakhale pa nsanja,kothawira kwake kudzakhala mʼmalinga a mʼmapiri.Azidzalandira chakudya chakendipo madzi sadzamusowa. 17 Nthawi imeneyo maso a ana adzaona mfumu ya maonekedwe wokongolandi kuona dziko lotambasukira kutali. 18 Mu mtima mwanu muzidzalingalira zoopsa zinachitika kale zija:“Ali kuti mkulu wa Asilikali uja?Ali kuti wokhometsa misonkho uja?Ali kuti mkulu woyangʼanira nsanja?” 19 Simudzawaonanso anthu odzikuza aja,anthu aja achiyankhulo chosadziwika,chachilendo ndi chosamveka. 20 Taonani Ziyoni, mzinda wa zikondwerero zachipembedzo chathu;maso anu adzaona Yerusalemu,mzinda wamtendere, tenti imene sidzachotsedwa,zikhomo zake sizidzazulidwa,kapena zingwe zake kuduka. 21 Kumeneko Yehova adzaonetsa ulemerero wakendipo mzindawo udzakhala kasupe wa mitsinje yayikulu.Ngalawa za zopalasa sizidzapitamo,sitima zapamadzi zikuluzikulu sizidzayendamo. 22 Pakuti Yehova ndi woweruza wathu,Yehova ndiye wotilamulira,Yehova ndiye mfumu yathu;ndipo ndiye amene adzatipulumutse. 23 Zingwe za sitima zapamadzi za adani athu zamasuka,sizikutha kulimbitsa mlongoti wake,matanga ake sakutheka kutambasuka.Ngakhale tidzagawana zofunkha zochuluka kwambirindipo ngakhale olumala adzatenga zofunkhazo. 24 Palibe ndi mmodzi yemwe wokhala mʼZiyoni adzanene kuti, “Ndikudwala”ndipo anthu onse okhala mʼmenemo machimo awo adzakhululukidwa.

In Other Versions

Isaiah 33 in the ANGEFD

Isaiah 33 in the ANTPNG2D

Isaiah 33 in the AS21

Isaiah 33 in the BAGH

Isaiah 33 in the BBPNG

Isaiah 33 in the BBT1E

Isaiah 33 in the BDS

Isaiah 33 in the BEV

Isaiah 33 in the BHAD

Isaiah 33 in the BIB

Isaiah 33 in the BLPT

Isaiah 33 in the BNT

Isaiah 33 in the BNTABOOT

Isaiah 33 in the BNTLV

Isaiah 33 in the BOATCB

Isaiah 33 in the BOATCB2

Isaiah 33 in the BOBCV

Isaiah 33 in the BOCNT

Isaiah 33 in the BOECS

Isaiah 33 in the BOHCB

Isaiah 33 in the BOHCV

Isaiah 33 in the BOHLNT

Isaiah 33 in the BOHNTLTAL

Isaiah 33 in the BOICB

Isaiah 33 in the BOILNTAP

Isaiah 33 in the BOITCV

Isaiah 33 in the BOKCV

Isaiah 33 in the BOKCV2

Isaiah 33 in the BOKHWOG

Isaiah 33 in the BOKSSV

Isaiah 33 in the BOLCB

Isaiah 33 in the BOLCB2

Isaiah 33 in the BOMCV

Isaiah 33 in the BONAV

Isaiah 33 in the BONCB

Isaiah 33 in the BONLT

Isaiah 33 in the BONUT2

Isaiah 33 in the BOPLNT

Isaiah 33 in the BOSCB

Isaiah 33 in the BOSNC

Isaiah 33 in the BOTLNT

Isaiah 33 in the BOVCB

Isaiah 33 in the BOYCB

Isaiah 33 in the BPBB

Isaiah 33 in the BPH

Isaiah 33 in the BSB

Isaiah 33 in the CCB

Isaiah 33 in the CUV

Isaiah 33 in the CUVS

Isaiah 33 in the DBT

Isaiah 33 in the DGDNT

Isaiah 33 in the DHNT

Isaiah 33 in the DNT

Isaiah 33 in the ELBE

Isaiah 33 in the EMTV

Isaiah 33 in the ESV

Isaiah 33 in the FBV

Isaiah 33 in the FEB

Isaiah 33 in the GGMNT

Isaiah 33 in the GNT

Isaiah 33 in the HARY

Isaiah 33 in the HNT

Isaiah 33 in the IRVA

Isaiah 33 in the IRVB

Isaiah 33 in the IRVG

Isaiah 33 in the IRVH

Isaiah 33 in the IRVK

Isaiah 33 in the IRVM

Isaiah 33 in the IRVM2

Isaiah 33 in the IRVO

Isaiah 33 in the IRVP

Isaiah 33 in the IRVT

Isaiah 33 in the IRVT2

Isaiah 33 in the IRVU

Isaiah 33 in the ISVN

Isaiah 33 in the JSNT

Isaiah 33 in the KAPI

Isaiah 33 in the KBT1ETNIK

Isaiah 33 in the KBV

Isaiah 33 in the KJV

Isaiah 33 in the KNFD

Isaiah 33 in the LBA

Isaiah 33 in the LBLA

Isaiah 33 in the LNT

Isaiah 33 in the LSV

Isaiah 33 in the MAAL

Isaiah 33 in the MBV

Isaiah 33 in the MBV2

Isaiah 33 in the MHNT

Isaiah 33 in the MKNFD

Isaiah 33 in the MNG

Isaiah 33 in the MNT

Isaiah 33 in the MNT2

Isaiah 33 in the MRS1T

Isaiah 33 in the NAA

Isaiah 33 in the NASB

Isaiah 33 in the NBLA

Isaiah 33 in the NBS

Isaiah 33 in the NBVTP

Isaiah 33 in the NET2

Isaiah 33 in the NIV11

Isaiah 33 in the NNT

Isaiah 33 in the NNT2

Isaiah 33 in the NNT3

Isaiah 33 in the PDDPT

Isaiah 33 in the PFNT

Isaiah 33 in the RMNT

Isaiah 33 in the SBIAS

Isaiah 33 in the SBIBS

Isaiah 33 in the SBIBS2

Isaiah 33 in the SBICS

Isaiah 33 in the SBIDS

Isaiah 33 in the SBIGS

Isaiah 33 in the SBIHS

Isaiah 33 in the SBIIS

Isaiah 33 in the SBIIS2

Isaiah 33 in the SBIIS3

Isaiah 33 in the SBIKS

Isaiah 33 in the SBIKS2

Isaiah 33 in the SBIMS

Isaiah 33 in the SBIOS

Isaiah 33 in the SBIPS

Isaiah 33 in the SBISS

Isaiah 33 in the SBITS

Isaiah 33 in the SBITS2

Isaiah 33 in the SBITS3

Isaiah 33 in the SBITS4

Isaiah 33 in the SBIUS

Isaiah 33 in the SBIVS

Isaiah 33 in the SBT

Isaiah 33 in the SBT1E

Isaiah 33 in the SCHL

Isaiah 33 in the SNT

Isaiah 33 in the SUSU

Isaiah 33 in the SUSU2

Isaiah 33 in the SYNO

Isaiah 33 in the TBIAOTANT

Isaiah 33 in the TBT1E

Isaiah 33 in the TBT1E2

Isaiah 33 in the TFTIP

Isaiah 33 in the TFTU

Isaiah 33 in the TGNTATF3T

Isaiah 33 in the THAI

Isaiah 33 in the TNFD

Isaiah 33 in the TNT

Isaiah 33 in the TNTIK

Isaiah 33 in the TNTIL

Isaiah 33 in the TNTIN

Isaiah 33 in the TNTIP

Isaiah 33 in the TNTIZ

Isaiah 33 in the TOMA

Isaiah 33 in the TTENT

Isaiah 33 in the UBG

Isaiah 33 in the UGV

Isaiah 33 in the UGV2

Isaiah 33 in the UGV3

Isaiah 33 in the VBL

Isaiah 33 in the VDCC

Isaiah 33 in the YALU

Isaiah 33 in the YAPE

Isaiah 33 in the YBVTP

Isaiah 33 in the ZBP