Isaiah 9 (BOGWICC)

1 Anthu amene anali ndi nkhawa, sadzakhalanso otaya mtima. Masiku amakedzana Mulungu ananyozetsa dziko la Zebuloni ndi dziko la Nafutali, koma kutsogolo kuno dera lonse la Galileya, limene lili dziko la anthu a mitundu ina, kuyambira ku nyanja yayikulu, mʼmbali mwa Yorodani, adzalisandutsa laulemu. 2 Anthu oyenda mu mdimaawona kuwala kwakukulu;kwa iwo okhala mʼdziko la mdima wandiweyanikuwunika kwawafikira. 3 Inu mwauchulukitsa mtundu wanundipo mwawonjezera chimwemwe chawo.Iwo akukondwa pamaso panu,ngati mmene anthu amakondwera nthawi yokolola,ngatinso mmene anthu amakondwerapamene akugawana zolanda ku nkhondo. 4 Monga munachitira pogonjetsa Amidiyani,inu mwathyola golilimene limawalemera,ndodo zimene amamenyera mapewa awo,ndiponso mikwapulo ya anthu owazunza. 5 Nsapato iliyonse ya munthu wankhondo,ndiponso chovala chilichonse chodonthekera magazizidzatenthedwa pa motongati nkhuni. 6 Chifukwa mwana watibadwira,mwana wamwamuna wapatsidwa kwa ife,ndipo ulamuliro udzakhala pa phewa lake.Ndipo adzamutcha dzina lake lakutiPhungu Wodabwitsa, Mulungu Wamphamvu,Atate Amuyaya, ndi Mfumu ya Mtendere. 7 Ulamuliro ndi mtendere wakezidzakhala zopanda malire.Iye adzalamulira ufumu wake ali pampando waufumu wa Davide,ndipo adzawukhazikitsa ndi kuwuchirikizamwa chiweruzo cholungama ndi pochita zachilungamokuyambira nthawi imeneyo mpaka muyaya.Ndi mtima wake wonse, Yehova Wamphamvuzonsewatsimikiza kuchita zimenezi. 8 Ambuye atumiza mawu otsutsa Yakobo;ndipo mawuwo agwera pa Israeli. 9 Anthu onse okhala muEfereimu ndi okhala mu Samariya,adzadziwa zimenezi.Iwo amayankhula modzikuza kuti, 10 “Ngakhale njerwa zagumuka,koma ife tidzamanga ndi miyala yosema.Mitanda ya mkuyu yagwetsedwa,koma ife tidzayika mitanda ya mkungudza mʼmalo mwake.” 11 Koma Yehova wadzutsa adani kuti alimbane nawondipo wawafulumiza adani awo kuti amenyane nawo. 12 Asiriya ochokera kummawa ndi Afilisti ochokera kumadzulo ndipoayasama pakamwa kuti adye a Israeli. Komabe, mkwiyo wake sunawachokere,mkono wake uli chitambasulire. 13 Koma anthu sanabwerere kwa amene anawakantha uja,ngakhale kufunafuna Yehova Wamphamvuzonse. 14 Choncho Yehova adzadula mutu wa Israeli pamodzi ndi mchira womwe,nthambi ya kanjedza ndi bango lomwe tsiku limodzi; 15 mutuwo ndiye akuluakulu ndi olemekezeka,mchira ndiye aneneri ophunzitsa zabodza. 16 Amene amatsogolera anthuwa ndiwo amawasocheretsa,ndipo otsogoleredwa amatayika. 17 Nʼchifukwa chake Ambuye adzakondwera nawo achinyamata,ngakhale kuwachitira chifundo ana amasiye ndi akazi amasiye,pakuti aliyense ndi wosapembedza Mulungu ndiponso ndi wochimwa ndipoaliyense amayankhula zopusa. Komabe, mkwiyo wake sunawachokere,mkono wake uli chitambasulire. 18 Ndithu kuyipa kwa anthuwo kumayaka ngati moto;moto wake umanyeketsa mkandankhuku ndi minga,umayatsa nkhalango yowirira,ndipo utsi wake umachita kuti toloo ngati mtambo. 19 Dziko lidzatenthedwa ndi ukali wa Yehova Wamphamvuzonse,dziko lidzatenthedwandipo anthu adzakhala ngati nkhuni zosonkhera moto;palibe munthu amene adzachitire chifundo mʼbale wake. 20 Kudzanja lamanja adzapeza chakudya nʼkudya,koma adzakhalabe ndi njala;kudzanja lamanzere adzapeza chakudya nʼkudya,koma sadzakhuta.Aliyense azidzadya ana ake omwe. 21 Manase adzadya Efereimu ndipo Efereimu adzadya Manase;onsewa pamodzi adzadya Yuda. Komabe pa zonsezi, mkwiyo wake sunawachokere,mkono wake uli chitambasulire.

In Other Versions

Isaiah 9 in the ANGEFD

Isaiah 9 in the ANTPNG2D

Isaiah 9 in the AS21

Isaiah 9 in the BAGH

Isaiah 9 in the BBPNG

Isaiah 9 in the BBT1E

Isaiah 9 in the BDS

Isaiah 9 in the BEV

Isaiah 9 in the BHAD

Isaiah 9 in the BIB

Isaiah 9 in the BLPT

Isaiah 9 in the BNT

Isaiah 9 in the BNTABOOT

Isaiah 9 in the BNTLV

Isaiah 9 in the BOATCB

Isaiah 9 in the BOATCB2

Isaiah 9 in the BOBCV

Isaiah 9 in the BOCNT

Isaiah 9 in the BOECS

Isaiah 9 in the BOHCB

Isaiah 9 in the BOHCV

Isaiah 9 in the BOHLNT

Isaiah 9 in the BOHNTLTAL

Isaiah 9 in the BOICB

Isaiah 9 in the BOILNTAP

Isaiah 9 in the BOITCV

Isaiah 9 in the BOKCV

Isaiah 9 in the BOKCV2

Isaiah 9 in the BOKHWOG

Isaiah 9 in the BOKSSV

Isaiah 9 in the BOLCB

Isaiah 9 in the BOLCB2

Isaiah 9 in the BOMCV

Isaiah 9 in the BONAV

Isaiah 9 in the BONCB

Isaiah 9 in the BONLT

Isaiah 9 in the BONUT2

Isaiah 9 in the BOPLNT

Isaiah 9 in the BOSCB

Isaiah 9 in the BOSNC

Isaiah 9 in the BOTLNT

Isaiah 9 in the BOVCB

Isaiah 9 in the BOYCB

Isaiah 9 in the BPBB

Isaiah 9 in the BPH

Isaiah 9 in the BSB

Isaiah 9 in the CCB

Isaiah 9 in the CUV

Isaiah 9 in the CUVS

Isaiah 9 in the DBT

Isaiah 9 in the DGDNT

Isaiah 9 in the DHNT

Isaiah 9 in the DNT

Isaiah 9 in the ELBE

Isaiah 9 in the EMTV

Isaiah 9 in the ESV

Isaiah 9 in the FBV

Isaiah 9 in the FEB

Isaiah 9 in the GGMNT

Isaiah 9 in the GNT

Isaiah 9 in the HARY

Isaiah 9 in the HNT

Isaiah 9 in the IRVA

Isaiah 9 in the IRVB

Isaiah 9 in the IRVG

Isaiah 9 in the IRVH

Isaiah 9 in the IRVK

Isaiah 9 in the IRVM

Isaiah 9 in the IRVM2

Isaiah 9 in the IRVO

Isaiah 9 in the IRVP

Isaiah 9 in the IRVT

Isaiah 9 in the IRVT2

Isaiah 9 in the IRVU

Isaiah 9 in the ISVN

Isaiah 9 in the JSNT

Isaiah 9 in the KAPI

Isaiah 9 in the KBT1ETNIK

Isaiah 9 in the KBV

Isaiah 9 in the KJV

Isaiah 9 in the KNFD

Isaiah 9 in the LBA

Isaiah 9 in the LBLA

Isaiah 9 in the LNT

Isaiah 9 in the LSV

Isaiah 9 in the MAAL

Isaiah 9 in the MBV

Isaiah 9 in the MBV2

Isaiah 9 in the MHNT

Isaiah 9 in the MKNFD

Isaiah 9 in the MNG

Isaiah 9 in the MNT

Isaiah 9 in the MNT2

Isaiah 9 in the MRS1T

Isaiah 9 in the NAA

Isaiah 9 in the NASB

Isaiah 9 in the NBLA

Isaiah 9 in the NBS

Isaiah 9 in the NBVTP

Isaiah 9 in the NET2

Isaiah 9 in the NIV11

Isaiah 9 in the NNT

Isaiah 9 in the NNT2

Isaiah 9 in the NNT3

Isaiah 9 in the PDDPT

Isaiah 9 in the PFNT

Isaiah 9 in the RMNT

Isaiah 9 in the SBIAS

Isaiah 9 in the SBIBS

Isaiah 9 in the SBIBS2

Isaiah 9 in the SBICS

Isaiah 9 in the SBIDS

Isaiah 9 in the SBIGS

Isaiah 9 in the SBIHS

Isaiah 9 in the SBIIS

Isaiah 9 in the SBIIS2

Isaiah 9 in the SBIIS3

Isaiah 9 in the SBIKS

Isaiah 9 in the SBIKS2

Isaiah 9 in the SBIMS

Isaiah 9 in the SBIOS

Isaiah 9 in the SBIPS

Isaiah 9 in the SBISS

Isaiah 9 in the SBITS

Isaiah 9 in the SBITS2

Isaiah 9 in the SBITS3

Isaiah 9 in the SBITS4

Isaiah 9 in the SBIUS

Isaiah 9 in the SBIVS

Isaiah 9 in the SBT

Isaiah 9 in the SBT1E

Isaiah 9 in the SCHL

Isaiah 9 in the SNT

Isaiah 9 in the SUSU

Isaiah 9 in the SUSU2

Isaiah 9 in the SYNO

Isaiah 9 in the TBIAOTANT

Isaiah 9 in the TBT1E

Isaiah 9 in the TBT1E2

Isaiah 9 in the TFTIP

Isaiah 9 in the TFTU

Isaiah 9 in the TGNTATF3T

Isaiah 9 in the THAI

Isaiah 9 in the TNFD

Isaiah 9 in the TNT

Isaiah 9 in the TNTIK

Isaiah 9 in the TNTIL

Isaiah 9 in the TNTIN

Isaiah 9 in the TNTIP

Isaiah 9 in the TNTIZ

Isaiah 9 in the TOMA

Isaiah 9 in the TTENT

Isaiah 9 in the UBG

Isaiah 9 in the UGV

Isaiah 9 in the UGV2

Isaiah 9 in the UGV3

Isaiah 9 in the VBL

Isaiah 9 in the VDCC

Isaiah 9 in the YALU

Isaiah 9 in the YAPE

Isaiah 9 in the YBVTP

Isaiah 9 in the ZBP