Ecclesiastes 7 (BOGWICC)
1 Mbiri yabwino ndi yopambana mafuta onunkhira bwino,ndipo tsiku lomwalira ndi lopambana tsiku lobadwa. 2 Kuli bwino kupita ku nyumba yamalirokusiyana ndi kupita ku nyumba yamadyerero:Pakuti imfa ndiye mathero a munthu aliyense;anthu amoyo azichisunga chimenechi mʼmitima mwawo. 3 Chisoni nʼchabwino kusiyana ndi kuseka,pakuti nkhope yakugwa ndi yabwino chifukwa imakonza mtima. 4 Mtima wa munthu wanzeru nthawi zonse umalingalira za imfa,koma mitima ya zitsiru imalingalira za chisangalalo. 5 Kuli bwino kumva kudzudzula kwa munthu wanzerukusiyana ndi kumvera mayamiko a zitsiru. 6 Kuseka kwa zitsiru kuli ngatikuthetheka kwa moto kunsi kwa mʼphika,izinso ndi zopandapake. 7 Kuzunza ena kumasandutsa munthu wanzeru kukhala chitsiru,ndipo chiphuphu chimawononga mtima. 8 Mathero ake a chinthu ndi abwino kupambana chiyambi chake,ndipo kufatsa nʼkwabwino kupambana kudzikuza. 9 Usamafulumire kukwiya mu mtima mwako,pakuti mkwiyo ndi bwenzi la zitsiru. 10 Usamafunse kuti, “Nʼchifukwa chiyani masiku amakedzana anali abwino kupambana masiku ano?”pakuti si chinthu chanzeru kufunsa mafunso oterewa. 11 Nzeru ngati cholowa, ndi chinthu chabwinondipo imapindulitsa wamoyo aliyense pansi pano. 12 Nzeru ndi chitetezo,monganso ndalama zili chitetezo,koma phindu la chidziwitso ndi ili:kuti nzeru zimasunga moyo wa munthu amene ali nazo nzeruzo. 13 Taganizirani zimene Mulungu wazichita:ndani angathe kuwongola chinthuchimene Iye anachipanga chokhota? 14 Pamene zinthu zili bwino, sangalala;koma pamene zinthu sizili bwino, ganizira bwino:Mulungu ndiye anapanga nthawi yabwinoyo,ndiponso nthawi imene si yabwinoyo.Choncho munthu sangathe kuzindikirachilichonse cha mʼtsogolo mwake. 15 Pa moyo wanga wopanda phinduwu ndaona zinthu ziwiri izi:munthu wolungama akuwonongeka mʼchilungamo chake,ndipo munthu woyipa akukhala moyo wautali mʼzoyipa zake. 16 Usakhale wolungama kwambirikapena wanzeru kwambiri,udziwonongerenji wekha? 17 Usakhale woyipa kwambiri,ndipo usakhale chitsiru,uferenji nthawi yako isanakwane? 18 Nʼkwabwino kuti utsate njira imodzi,ndipo usataye njira inayo.Munthu amene amaopa Mulungu adzapewa zinthu ziwiri zonsezi. 19 Nzeru zimapereka mphamvu zambiri kwa munthu wanzerukupambana olamulira khumi a mu mzinda. 20 Palibe munthu wolungama pa dziko lapansiamene amachita zabwino zokhazokha ndipo sachimwa. 21 Usamamvetsere mawu onse amene anthu amayankhula,mwina udzamva wantchito wako akukutukwana, 22 pakuti iwe ukudziwa mu mtima mwakokuti nthawi zambiri iwenso unatukwanapo ena. 23 Zonsezi ndinaziyesa ndi nzeru zanga ndipo ndinati,“Ine ndatsimikiza mu mtima mwanga kuti ndikhale wanzeru,”koma nzeruyo inanditalikira. 24 Nzeru zimene zilipo,zili kutali ndipo ndi zozama kwambiri,ndani angathe kuzidziwa? 25 Kotero ndinayikapo mtima wanga kuti ndidziwe,ndifufuze ndi kumafunafuna nzeru ndi mmene zinthu zimakhalirandipo ndinafunanso kudziwa kuyipa kwa uchitsirundiponso kupusa kwake kwa misala. 26 Ndinapeza kanthu kowawa kupambana imfa,mkazi amene ali ngati khoka,amene mtima wake uli ngati khwekhwe,ndipo manja ake ali ngati maunyolo.Munthu amene amakondweretsa Mulungu adzathawa mkaziyo,koma mkaziyo adzakola munthu wochimwa. 27 Mlaliki akunena kuti, “Taonani, chimene ndinachipeza ndi ichi:“Kuwonjezera chinthu china pa china kuti ndidziwe mmene zinthu zimachitikira, 28 pamene ine ndinali kufufuzabekoma osapeza kanthu,ndinapeza munthu mmodzi wolungama pakati pa anthu 1,000,koma pakati pawo panalibepo mkazi mmodzi wolungama. 29 Chokhacho chimene ndinachipeza ndi ichi:Mulungu analenga munthu, anamupatsa mtima wolungama,koma anthu anatsatira njira zawozawo zambirimbiri.”
In Other Versions
Ecclesiastes 7 in the ANGEFD
Ecclesiastes 7 in the ANTPNG2D
Ecclesiastes 7 in the AS21
Ecclesiastes 7 in the BAGH
Ecclesiastes 7 in the BBPNG
Ecclesiastes 7 in the BBT1E
Ecclesiastes 7 in the BDS
Ecclesiastes 7 in the BEV
Ecclesiastes 7 in the BHAD
Ecclesiastes 7 in the BIB
Ecclesiastes 7 in the BLPT
Ecclesiastes 7 in the BNT
Ecclesiastes 7 in the BNTABOOT
Ecclesiastes 7 in the BNTLV
Ecclesiastes 7 in the BOATCB
Ecclesiastes 7 in the BOATCB2
Ecclesiastes 7 in the BOBCV
Ecclesiastes 7 in the BOCNT
Ecclesiastes 7 in the BOECS
Ecclesiastes 7 in the BOHCB
Ecclesiastes 7 in the BOHCV
Ecclesiastes 7 in the BOHLNT
Ecclesiastes 7 in the BOHNTLTAL
Ecclesiastes 7 in the BOICB
Ecclesiastes 7 in the BOILNTAP
Ecclesiastes 7 in the BOITCV
Ecclesiastes 7 in the BOKCV
Ecclesiastes 7 in the BOKCV2
Ecclesiastes 7 in the BOKHWOG
Ecclesiastes 7 in the BOKSSV
Ecclesiastes 7 in the BOLCB
Ecclesiastes 7 in the BOLCB2
Ecclesiastes 7 in the BOMCV
Ecclesiastes 7 in the BONAV
Ecclesiastes 7 in the BONCB
Ecclesiastes 7 in the BONLT
Ecclesiastes 7 in the BONUT2
Ecclesiastes 7 in the BOPLNT
Ecclesiastes 7 in the BOSCB
Ecclesiastes 7 in the BOSNC
Ecclesiastes 7 in the BOTLNT
Ecclesiastes 7 in the BOVCB
Ecclesiastes 7 in the BOYCB
Ecclesiastes 7 in the BPBB
Ecclesiastes 7 in the BPH
Ecclesiastes 7 in the BSB
Ecclesiastes 7 in the CCB
Ecclesiastes 7 in the CUV
Ecclesiastes 7 in the CUVS
Ecclesiastes 7 in the DBT
Ecclesiastes 7 in the DGDNT
Ecclesiastes 7 in the DHNT
Ecclesiastes 7 in the DNT
Ecclesiastes 7 in the ELBE
Ecclesiastes 7 in the EMTV
Ecclesiastes 7 in the ESV
Ecclesiastes 7 in the FBV
Ecclesiastes 7 in the FEB
Ecclesiastes 7 in the GGMNT
Ecclesiastes 7 in the GNT
Ecclesiastes 7 in the HARY
Ecclesiastes 7 in the HNT
Ecclesiastes 7 in the IRVA
Ecclesiastes 7 in the IRVB
Ecclesiastes 7 in the IRVG
Ecclesiastes 7 in the IRVH
Ecclesiastes 7 in the IRVK
Ecclesiastes 7 in the IRVM
Ecclesiastes 7 in the IRVM2
Ecclesiastes 7 in the IRVO
Ecclesiastes 7 in the IRVP
Ecclesiastes 7 in the IRVT
Ecclesiastes 7 in the IRVT2
Ecclesiastes 7 in the IRVU
Ecclesiastes 7 in the ISVN
Ecclesiastes 7 in the JSNT
Ecclesiastes 7 in the KAPI
Ecclesiastes 7 in the KBT1ETNIK
Ecclesiastes 7 in the KBV
Ecclesiastes 7 in the KJV
Ecclesiastes 7 in the KNFD
Ecclesiastes 7 in the LBA
Ecclesiastes 7 in the LBLA
Ecclesiastes 7 in the LNT
Ecclesiastes 7 in the LSV
Ecclesiastes 7 in the MAAL
Ecclesiastes 7 in the MBV
Ecclesiastes 7 in the MBV2
Ecclesiastes 7 in the MHNT
Ecclesiastes 7 in the MKNFD
Ecclesiastes 7 in the MNG
Ecclesiastes 7 in the MNT
Ecclesiastes 7 in the MNT2
Ecclesiastes 7 in the MRS1T
Ecclesiastes 7 in the NAA
Ecclesiastes 7 in the NASB
Ecclesiastes 7 in the NBLA
Ecclesiastes 7 in the NBS
Ecclesiastes 7 in the NBVTP
Ecclesiastes 7 in the NET2
Ecclesiastes 7 in the NIV11
Ecclesiastes 7 in the NNT
Ecclesiastes 7 in the NNT2
Ecclesiastes 7 in the NNT3
Ecclesiastes 7 in the PDDPT
Ecclesiastes 7 in the PFNT
Ecclesiastes 7 in the RMNT
Ecclesiastes 7 in the SBIAS
Ecclesiastes 7 in the SBIBS
Ecclesiastes 7 in the SBIBS2
Ecclesiastes 7 in the SBICS
Ecclesiastes 7 in the SBIDS
Ecclesiastes 7 in the SBIGS
Ecclesiastes 7 in the SBIHS
Ecclesiastes 7 in the SBIIS
Ecclesiastes 7 in the SBIIS2
Ecclesiastes 7 in the SBIIS3
Ecclesiastes 7 in the SBIKS
Ecclesiastes 7 in the SBIKS2
Ecclesiastes 7 in the SBIMS
Ecclesiastes 7 in the SBIOS
Ecclesiastes 7 in the SBIPS
Ecclesiastes 7 in the SBISS
Ecclesiastes 7 in the SBITS
Ecclesiastes 7 in the SBITS2
Ecclesiastes 7 in the SBITS3
Ecclesiastes 7 in the SBITS4
Ecclesiastes 7 in the SBIUS
Ecclesiastes 7 in the SBIVS
Ecclesiastes 7 in the SBT
Ecclesiastes 7 in the SBT1E
Ecclesiastes 7 in the SCHL
Ecclesiastes 7 in the SNT
Ecclesiastes 7 in the SUSU
Ecclesiastes 7 in the SUSU2
Ecclesiastes 7 in the SYNO
Ecclesiastes 7 in the TBIAOTANT
Ecclesiastes 7 in the TBT1E
Ecclesiastes 7 in the TBT1E2
Ecclesiastes 7 in the TFTIP
Ecclesiastes 7 in the TFTU
Ecclesiastes 7 in the TGNTATF3T
Ecclesiastes 7 in the THAI
Ecclesiastes 7 in the TNFD
Ecclesiastes 7 in the TNT
Ecclesiastes 7 in the TNTIK
Ecclesiastes 7 in the TNTIL
Ecclesiastes 7 in the TNTIN
Ecclesiastes 7 in the TNTIP
Ecclesiastes 7 in the TNTIZ
Ecclesiastes 7 in the TOMA
Ecclesiastes 7 in the TTENT
Ecclesiastes 7 in the UBG
Ecclesiastes 7 in the UGV
Ecclesiastes 7 in the UGV2
Ecclesiastes 7 in the UGV3
Ecclesiastes 7 in the VBL
Ecclesiastes 7 in the VDCC
Ecclesiastes 7 in the YALU
Ecclesiastes 7 in the YAPE
Ecclesiastes 7 in the YBVTP
Ecclesiastes 7 in the ZBP