Ezekiel 30 (BOGWICC)

1 Yehova anandiyankhula kuti: 2 “Iwe mwana wa munthu, nenera ndipo ulengeze zimene Ine Ambuye Yehova ndikunena.“ ‘Ufuwule mawu awa akuti,‘Kalanga, tsiku lafika!’ 3 Pakuti tsiku layandikira,tsiku la Yehova lili pafupi,tsiku la mitambo yakuda,tsiku lachiwonongeko cha mitundu ya anthu. 4 Lupanga lidzabwera kudzalimbana ndi Iguptondipo mavuto adzafika pa Kusi.Pamene anthu ambiri adzaphedwa mu Igupto,chuma chake chidzatengedwandipo maziko ake adzagumuka. 5 Kusi, Puti, Ludi ndi Arabiya yense, Libiya ndiponso anthu a mʼdziko logwirizana naye adzaphedwa ndi lupanga pamodzi ndi Igupto. 6 “ ‘Ine Ambuye Yehova ndikuti:“ ‘Onse othandiza Igupto adzaphedwandipo kunyadira mphamvu zake kudzatheratu.Adzaphedwa ndi lupangakuyambira ku Migidoli mpaka ku mzinda wa Asiwani,’ ”ndikutero Ine Ambuye Yehova. 7 “ ‘Dziko la Igupto lidzasanduka bwinjakupambana mabwinja ena onse opasuka,ndipo mizinda yake idzakhala yopasukakupambana mizinda ina yonse. 8 Nditatha kutentha Iguptondi kupha onse omuthandiza,pamenepo adzadziwa kuti Ine ndine Yehova. 9 “ ‘Nthawi imeneyo ikadzafika, amithenga adzapita mofulumira kuchokera kwa Ine kukaopseza Kusi, iwowo osadziwako kanthu. Ndipo adzada nkhawa pa tsiku limene Igupto adzawonongedwa, chifukwa tsikulo lidzafika ndithu. 10 “ ‘Ine Ambuye Yehova ndikuti,“ ‘Ndidzagwiritsa ntchito Nebukadinezara, mfumu ya ku Babulonikuti ndithetse gulu lankhondo la Igupto. 11 Iye ndi gulu lake lankhondo, mtundu wa anthu ankhanza kwambiri ajaadzabwera kudzawononga dzikolo.Adzasolola malupanga awo kulimbana ndi Iguptondipo dziko lidzadzaza ndi mitembo. 12 Ndidzawumitsa mtsinje wa Nailondi kugulitsa dziko la Igupto kwa anthu oyipa.Ndidzagwiritsa ntchito anthu achilendo kuti ndiwononge dzikolopamodzi ndi zonse zili mʼmenemo.Ine Yehova ndayankhula. 13 “ ‘Ine Ambuye Yehova ndikuti,“ ‘Ndidzawononga mafanondi kuthetsa milungu yosema ya ku Mefisi.Simudzakhalanso mfumu mu Igupto,ndipo ndidzaopseza dziko lonse. 14 Ndidzasandutsa chipululu mzinda wa Patirosi,ndi kutentha mzinda wa Zowani.Ndidzalanga mzinda wa Thebesi. 15 Ndidzakhuthulira ukali wanga pa mzinda wa Peluziumu,linga lolimba la Igupto,ndi kuwononga gulu lankhondo la Thebesi. 16 Ndidzatentha ndi moto dziko la Igupto;Peluziumu adzazunzika ndi ululu.Malinga a Thebesi adzagumuka,ndipo mzindawo udzasefukira ndi madzi. 17 Anyamata a ku Oni ndi ku Pibesetiadzaphedwa ndi lupangandipo okhala mʼmizinda yake adzatengedwa ukapolo. 18 Ku Tehafinehezi kudzakhala mdimapamene ndidzathyola goli la Igupto;motero kunyada kwake kudzatha.Iye adzaphimbidwa ndi mitambo yakuda,ndipo okhala mʼmizinda yake adzapita ku ukapolo. 19 Kotero ndidzalanga dziko la Igupto,ndipo iwo adzadziwa kuti Ine ndine Yehova.’ ” 20 Pa tsiku lachisanu ndi chiwiri la mwezi woyamba wa chaka chakhumi ndi chimodzi, Yehova anandiyankhula kuti: 21 “Iwe mwana wa munthu, ndathyola dzanja la Farao mfumu ya Igupto. Taona, silinamangidwe kuti lipole, ngakhale kulilimbitsa ndi nsalu kuti lithe kugwiranso lupanga. 22 Nʼchifukwa chake Ine Ambuye Yehova ndikuti, Ine ndikudana ndi Farao mfumu ya Igupto. Ndidzathyola manja ake onse; dzanja labwino pamodzi ndi lothyokalo, ndipo lupanga lidzagwa mʼmanja mwake. 23 Ndidzamwaza Aigupto pakati pa mitundu ya anthu ndikuwabalalitsira ku mayiko ambiri. 24 Ndidzalimbitsa manja a mfumu ya ku Babuloni, ndipo mʼmanja mwake ndidzayikamo lupanga langa. Koma ndidzathyola manja a Farao, ndipo adzabuwula ngati wolasidwa koopsa pamaso pa mfumu ya ku Babuloniyo. 25 Ndidzalimbitsa manja a mfumu ya ku Babuloni, koma manja a Farao adzafowoka. Motero anthu adzadziwa kuti Ine ndine Yehova, ndikadzayika lupanga langa mʼmanja mwa mfumu ya ku Babuloni. Ndipo adzaligwiritsa ntchito pothira nkhondo dziko la Igupto. 26 Ndidzamwaza Aigupto pakati pa mitundu ya anthu, ndikuwabalalitsira ku mayiko ambiri. Motero adzadziwa kuti Ine ndine Yehova.”

In Other Versions

Ezekiel 30 in the ANGEFD

Ezekiel 30 in the ANTPNG2D

Ezekiel 30 in the AS21

Ezekiel 30 in the BAGH

Ezekiel 30 in the BBPNG

Ezekiel 30 in the BBT1E

Ezekiel 30 in the BDS

Ezekiel 30 in the BEV

Ezekiel 30 in the BHAD

Ezekiel 30 in the BIB

Ezekiel 30 in the BLPT

Ezekiel 30 in the BNT

Ezekiel 30 in the BNTABOOT

Ezekiel 30 in the BNTLV

Ezekiel 30 in the BOATCB

Ezekiel 30 in the BOATCB2

Ezekiel 30 in the BOBCV

Ezekiel 30 in the BOCNT

Ezekiel 30 in the BOECS

Ezekiel 30 in the BOHCB

Ezekiel 30 in the BOHCV

Ezekiel 30 in the BOHLNT

Ezekiel 30 in the BOHNTLTAL

Ezekiel 30 in the BOICB

Ezekiel 30 in the BOILNTAP

Ezekiel 30 in the BOITCV

Ezekiel 30 in the BOKCV

Ezekiel 30 in the BOKCV2

Ezekiel 30 in the BOKHWOG

Ezekiel 30 in the BOKSSV

Ezekiel 30 in the BOLCB

Ezekiel 30 in the BOLCB2

Ezekiel 30 in the BOMCV

Ezekiel 30 in the BONAV

Ezekiel 30 in the BONCB

Ezekiel 30 in the BONLT

Ezekiel 30 in the BONUT2

Ezekiel 30 in the BOPLNT

Ezekiel 30 in the BOSCB

Ezekiel 30 in the BOSNC

Ezekiel 30 in the BOTLNT

Ezekiel 30 in the BOVCB

Ezekiel 30 in the BOYCB

Ezekiel 30 in the BPBB

Ezekiel 30 in the BPH

Ezekiel 30 in the BSB

Ezekiel 30 in the CCB

Ezekiel 30 in the CUV

Ezekiel 30 in the CUVS

Ezekiel 30 in the DBT

Ezekiel 30 in the DGDNT

Ezekiel 30 in the DHNT

Ezekiel 30 in the DNT

Ezekiel 30 in the ELBE

Ezekiel 30 in the EMTV

Ezekiel 30 in the ESV

Ezekiel 30 in the FBV

Ezekiel 30 in the FEB

Ezekiel 30 in the GGMNT

Ezekiel 30 in the GNT

Ezekiel 30 in the HARY

Ezekiel 30 in the HNT

Ezekiel 30 in the IRVA

Ezekiel 30 in the IRVB

Ezekiel 30 in the IRVG

Ezekiel 30 in the IRVH

Ezekiel 30 in the IRVK

Ezekiel 30 in the IRVM

Ezekiel 30 in the IRVM2

Ezekiel 30 in the IRVO

Ezekiel 30 in the IRVP

Ezekiel 30 in the IRVT

Ezekiel 30 in the IRVT2

Ezekiel 30 in the IRVU

Ezekiel 30 in the ISVN

Ezekiel 30 in the JSNT

Ezekiel 30 in the KAPI

Ezekiel 30 in the KBT1ETNIK

Ezekiel 30 in the KBV

Ezekiel 30 in the KJV

Ezekiel 30 in the KNFD

Ezekiel 30 in the LBA

Ezekiel 30 in the LBLA

Ezekiel 30 in the LNT

Ezekiel 30 in the LSV

Ezekiel 30 in the MAAL

Ezekiel 30 in the MBV

Ezekiel 30 in the MBV2

Ezekiel 30 in the MHNT

Ezekiel 30 in the MKNFD

Ezekiel 30 in the MNG

Ezekiel 30 in the MNT

Ezekiel 30 in the MNT2

Ezekiel 30 in the MRS1T

Ezekiel 30 in the NAA

Ezekiel 30 in the NASB

Ezekiel 30 in the NBLA

Ezekiel 30 in the NBS

Ezekiel 30 in the NBVTP

Ezekiel 30 in the NET2

Ezekiel 30 in the NIV11

Ezekiel 30 in the NNT

Ezekiel 30 in the NNT2

Ezekiel 30 in the NNT3

Ezekiel 30 in the PDDPT

Ezekiel 30 in the PFNT

Ezekiel 30 in the RMNT

Ezekiel 30 in the SBIAS

Ezekiel 30 in the SBIBS

Ezekiel 30 in the SBIBS2

Ezekiel 30 in the SBICS

Ezekiel 30 in the SBIDS

Ezekiel 30 in the SBIGS

Ezekiel 30 in the SBIHS

Ezekiel 30 in the SBIIS

Ezekiel 30 in the SBIIS2

Ezekiel 30 in the SBIIS3

Ezekiel 30 in the SBIKS

Ezekiel 30 in the SBIKS2

Ezekiel 30 in the SBIMS

Ezekiel 30 in the SBIOS

Ezekiel 30 in the SBIPS

Ezekiel 30 in the SBISS

Ezekiel 30 in the SBITS

Ezekiel 30 in the SBITS2

Ezekiel 30 in the SBITS3

Ezekiel 30 in the SBITS4

Ezekiel 30 in the SBIUS

Ezekiel 30 in the SBIVS

Ezekiel 30 in the SBT

Ezekiel 30 in the SBT1E

Ezekiel 30 in the SCHL

Ezekiel 30 in the SNT

Ezekiel 30 in the SUSU

Ezekiel 30 in the SUSU2

Ezekiel 30 in the SYNO

Ezekiel 30 in the TBIAOTANT

Ezekiel 30 in the TBT1E

Ezekiel 30 in the TBT1E2

Ezekiel 30 in the TFTIP

Ezekiel 30 in the TFTU

Ezekiel 30 in the TGNTATF3T

Ezekiel 30 in the THAI

Ezekiel 30 in the TNFD

Ezekiel 30 in the TNT

Ezekiel 30 in the TNTIK

Ezekiel 30 in the TNTIL

Ezekiel 30 in the TNTIN

Ezekiel 30 in the TNTIP

Ezekiel 30 in the TNTIZ

Ezekiel 30 in the TOMA

Ezekiel 30 in the TTENT

Ezekiel 30 in the UBG

Ezekiel 30 in the UGV

Ezekiel 30 in the UGV2

Ezekiel 30 in the UGV3

Ezekiel 30 in the VBL

Ezekiel 30 in the VDCC

Ezekiel 30 in the YALU

Ezekiel 30 in the YAPE

Ezekiel 30 in the YBVTP

Ezekiel 30 in the ZBP