Isaiah 26 (BOGWICC)

1 Tsiku limenelo anthu a mʼdziko la Yuda adzayimba nyimbo iyi.Tili ndi mzinda wolimba.Mulungu amawuteteza ndi zipupandi malinga. 2 Tsekulani zipata za mzindakuti mtundu wolungamandi wokhulupirika ulowemo. 3 Inu mudzamupatsa munthuwa mtima wokhazikikamtendere weniweni. 4 Mudalireni Yehova mpaka muyaya,chifukwa Yehova Mulungu ndiye Thanthwe losatha. 5 Iye amatsitsa anthu amene amadziyika pamwamba,iye amagwetsa pansi mzinda wodzitukumula,amagumula makoma akendi kuwagwetsa pansi pa fumbi penipeni. 6 Mapazi a anthu akuwupondereza,mapazi a anthu oponderezedwa,mapazi anthu osauka. 7 Njira ya munthu wolungama ndi yosalaza,Inu Wolungamayo, mumasalaza njira ya wolungama. 8 Inde Yehova, timayenda mʼnjira zanu zolungama,ife timayembekezera Inu;mitima yathu imakhumba kukumbukirandi kulemekeza dzina lanu. 9 Moyo wanga umalakalaka Inu usiku wonse;nthawi yammawa ndimafunafuna Inu.Pamene muweruza dziko lapansianthu amaphunzira kuchita chilungamo. 10 Ngakhale mukomere mtima anthu oyipa,saphunzira chilungamo.Amachita zoyipa mʼdziko la chilungamo,ndipo sazindikira ululu wa Yehova. 11 Inu Yehova, mwatukula dzanja lanu kuti muwalange,koma iwo sakuliona dzanjalo.Aloleni anthu aone ndi kuchita manyazi poona mmene mukondera anthu anu;ndipo moto umene mwasonkhera adani anu uwapsereze. 12 Yehova, mumatipatsa mtendere;ndipo zonse zimene ife tinazichita munatichitira ndinu. 13 Inu Yehova Mulungu wathu, ngakhale takhala tikulamulidwa ndi ena mʼmalo mwanu,koma ife timalemekeza dzina lanu lokha. 14 Iwo tsopano sadzadzukanso;mizimu yawo sidzabwera kudzativutitsapakuti mwawalanga ndipo mwawawononga;palibenso amene amawakumbukira. 15 Inu Yehova, mwaukulitsa mtundu wathu;mwauchulukitsa ndithundipo mwalandirapo ulemu;mwaukuza mbali zonse za dziko. 16 Yehova, anthu anu anabwera kwa Inu pamene anali mʼmasautso;pamene munawalanga,iwo anapemphera kwa Inu. 17 Monga mayi woyembekezera pamene nthawi yake yobereka yayandikiraamamva kupweteka ndipo amalira ndi ululu,ifenso tinali chimodzimodzi pamaso panu, Inu Yehova. 18 Ife chimodzimodzi tinamva ululu, ngati mayi pa nthawi yobala mwana,koma sitinapindulepo kanthu,kapena kupulumutsa dziko lapansi;sitinabadwitse anthu atsopano pa dziko pano. 19 Koma anthu anu amene anafa adzakhalanso ndi moyo;matupi awo adzadzuka.Iwo amene ali ku fumbi tsopanoadzadzuka ndi kuyimba mosangalala.Monga mame amafewetsa pansi kutsitsimutsa zomera,momwenso Yehova adzaukitsa anthu amene anafa kale. 20 Abale anga, pitani mukalowe mʼnyumba zanundipo mukadzitsekere;mukabisale kwa kanthawi kochepampaka ukali wake utatha. 21 Taonani, Yehova akubwera kuchokera kumene amakhala;akubwera kudzalanga anthu a dziko lapansi chifukwa cha machimo awo.Dziko lapansi lidzawulula magazi amene anakhetsedwa pa dzikolo;dziko lapansi silidzabisanso mitembo ya anthu ophedwa.

In Other Versions

Isaiah 26 in the ANGEFD

Isaiah 26 in the ANTPNG2D

Isaiah 26 in the AS21

Isaiah 26 in the BAGH

Isaiah 26 in the BBPNG

Isaiah 26 in the BBT1E

Isaiah 26 in the BDS

Isaiah 26 in the BEV

Isaiah 26 in the BHAD

Isaiah 26 in the BIB

Isaiah 26 in the BLPT

Isaiah 26 in the BNT

Isaiah 26 in the BNTABOOT

Isaiah 26 in the BNTLV

Isaiah 26 in the BOATCB

Isaiah 26 in the BOATCB2

Isaiah 26 in the BOBCV

Isaiah 26 in the BOCNT

Isaiah 26 in the BOECS

Isaiah 26 in the BOHCB

Isaiah 26 in the BOHCV

Isaiah 26 in the BOHLNT

Isaiah 26 in the BOHNTLTAL

Isaiah 26 in the BOICB

Isaiah 26 in the BOILNTAP

Isaiah 26 in the BOITCV

Isaiah 26 in the BOKCV

Isaiah 26 in the BOKCV2

Isaiah 26 in the BOKHWOG

Isaiah 26 in the BOKSSV

Isaiah 26 in the BOLCB

Isaiah 26 in the BOLCB2

Isaiah 26 in the BOMCV

Isaiah 26 in the BONAV

Isaiah 26 in the BONCB

Isaiah 26 in the BONLT

Isaiah 26 in the BONUT2

Isaiah 26 in the BOPLNT

Isaiah 26 in the BOSCB

Isaiah 26 in the BOSNC

Isaiah 26 in the BOTLNT

Isaiah 26 in the BOVCB

Isaiah 26 in the BOYCB

Isaiah 26 in the BPBB

Isaiah 26 in the BPH

Isaiah 26 in the BSB

Isaiah 26 in the CCB

Isaiah 26 in the CUV

Isaiah 26 in the CUVS

Isaiah 26 in the DBT

Isaiah 26 in the DGDNT

Isaiah 26 in the DHNT

Isaiah 26 in the DNT

Isaiah 26 in the ELBE

Isaiah 26 in the EMTV

Isaiah 26 in the ESV

Isaiah 26 in the FBV

Isaiah 26 in the FEB

Isaiah 26 in the GGMNT

Isaiah 26 in the GNT

Isaiah 26 in the HARY

Isaiah 26 in the HNT

Isaiah 26 in the IRVA

Isaiah 26 in the IRVB

Isaiah 26 in the IRVG

Isaiah 26 in the IRVH

Isaiah 26 in the IRVK

Isaiah 26 in the IRVM

Isaiah 26 in the IRVM2

Isaiah 26 in the IRVO

Isaiah 26 in the IRVP

Isaiah 26 in the IRVT

Isaiah 26 in the IRVT2

Isaiah 26 in the IRVU

Isaiah 26 in the ISVN

Isaiah 26 in the JSNT

Isaiah 26 in the KAPI

Isaiah 26 in the KBT1ETNIK

Isaiah 26 in the KBV

Isaiah 26 in the KJV

Isaiah 26 in the KNFD

Isaiah 26 in the LBA

Isaiah 26 in the LBLA

Isaiah 26 in the LNT

Isaiah 26 in the LSV

Isaiah 26 in the MAAL

Isaiah 26 in the MBV

Isaiah 26 in the MBV2

Isaiah 26 in the MHNT

Isaiah 26 in the MKNFD

Isaiah 26 in the MNG

Isaiah 26 in the MNT

Isaiah 26 in the MNT2

Isaiah 26 in the MRS1T

Isaiah 26 in the NAA

Isaiah 26 in the NASB

Isaiah 26 in the NBLA

Isaiah 26 in the NBS

Isaiah 26 in the NBVTP

Isaiah 26 in the NET2

Isaiah 26 in the NIV11

Isaiah 26 in the NNT

Isaiah 26 in the NNT2

Isaiah 26 in the NNT3

Isaiah 26 in the PDDPT

Isaiah 26 in the PFNT

Isaiah 26 in the RMNT

Isaiah 26 in the SBIAS

Isaiah 26 in the SBIBS

Isaiah 26 in the SBIBS2

Isaiah 26 in the SBICS

Isaiah 26 in the SBIDS

Isaiah 26 in the SBIGS

Isaiah 26 in the SBIHS

Isaiah 26 in the SBIIS

Isaiah 26 in the SBIIS2

Isaiah 26 in the SBIIS3

Isaiah 26 in the SBIKS

Isaiah 26 in the SBIKS2

Isaiah 26 in the SBIMS

Isaiah 26 in the SBIOS

Isaiah 26 in the SBIPS

Isaiah 26 in the SBISS

Isaiah 26 in the SBITS

Isaiah 26 in the SBITS2

Isaiah 26 in the SBITS3

Isaiah 26 in the SBITS4

Isaiah 26 in the SBIUS

Isaiah 26 in the SBIVS

Isaiah 26 in the SBT

Isaiah 26 in the SBT1E

Isaiah 26 in the SCHL

Isaiah 26 in the SNT

Isaiah 26 in the SUSU

Isaiah 26 in the SUSU2

Isaiah 26 in the SYNO

Isaiah 26 in the TBIAOTANT

Isaiah 26 in the TBT1E

Isaiah 26 in the TBT1E2

Isaiah 26 in the TFTIP

Isaiah 26 in the TFTU

Isaiah 26 in the TGNTATF3T

Isaiah 26 in the THAI

Isaiah 26 in the TNFD

Isaiah 26 in the TNT

Isaiah 26 in the TNTIK

Isaiah 26 in the TNTIL

Isaiah 26 in the TNTIN

Isaiah 26 in the TNTIP

Isaiah 26 in the TNTIZ

Isaiah 26 in the TOMA

Isaiah 26 in the TTENT

Isaiah 26 in the UBG

Isaiah 26 in the UGV

Isaiah 26 in the UGV2

Isaiah 26 in the UGV3

Isaiah 26 in the VBL

Isaiah 26 in the VDCC

Isaiah 26 in the YALU

Isaiah 26 in the YAPE

Isaiah 26 in the YBVTP

Isaiah 26 in the ZBP