Obadiah 1 (BOGWICC)

1 Masomphenya a Obadiya. Ambuye Yehova akunena kwa Edomu kuti,Tamva uthenga wochokera kwa Yehova:Nthumwi yatumidwa kupita kwa anthu a mitundu kukanena kuti,“Konzekani, tiyeni tikachite nkhondo ndi Edomu.” 2 “Taona, ndidzakuchepetsani pakati pa anthu a mitundu ina;udzanyozedwa kwambiri. 3 Kudzikuza kwa mtima wako kwakusocheretsa,iwe amene umakhala mʼmapanga a mʼmatanthwendipo umamanga nyumba zako pa mapiri ataliatali,iwe amene umanena mu mtima mwako kuti,‘Ndani anganditsitse pansi?’ 4 Koma ngakhale umawuluka ngati chiwombankhangandi kumanga chisa chako pakati pa nyenyezi,ndidzakutsitsa pansi kuchokera kumeneko,”akutero Yehova. 5 “Anthu akuba akanabwera kwa iwe,kapena anthu olanda zinthu akanafika usiku,aa, tsoka lanji limene likukudikira iwe!Kodi akanangotengako zimene akuzifuna zokha?Ngati anthu othyola mphesa akanafika,kodi akanakusiyiraniko mphesa pangʼono pokha? 6 Koma Esau adzalandidwa zinthu zonse,chuma chake chobisika chidzabedwa! 7 Anthu onse ogwirizana nawo adzakupirikitsira kumalire;abwenzi ako adzakunyenga ndi kukugonjetsa;amene amadya chakudya chako adzakutchera msampha,koma iwe sudzazindikira zimenezi.” 8 Yehova akunena kuti, “Tsiku limenelo,kodi sindidzawononga anthu onse anzeru a ku Edomu,anthu odziwa zinthu mʼmapiri a Esau? 9 Ankhondo ako, iwe Temani, adzachita mantha,ndipo aliyense amene ali mʼphiri la Esauadzaphedwa pa nkhondo. 10 Chifukwa cha nkhanza zimene unachitira mʼbale wako Yakobo,udzakhala wamanyazi;adzakuwononga mpaka muyaya. 11 Pamene adaniankamulanda chuma chakepamene alendo analowa pa zipata zakendi kuchita maere pa Yerusalemu,pa tsikulo iwe unali ngati mmodzi wa iwo. 12 Iwe sunayenera kunyoza mʼbale wakopa nthawi ya tsoka lake,kapena kunyogodola Ayudachifukwa cha chiwonongeko chawo,kapena kuwaseka pa nthawi yamavuto awo. 13 Iwe sunayenera kudutsa pa zipata za anthu angapa nthawi ya masautso awo,kapena kuwanyogodolapa tsiku la tsoka lawo,kapena kulanda chuma chawopa nthawi ya masautso awo. 14 Sunayenera kudikirira pamphambano ya misewukuti uphe Ayuda othawa,kapena kuwapereka kwa adani awo Ayuda opulumukapa nthawi ya mavuto awo.” 15 “Tsiku la Yehova layandikiralimene adzaweruza mitundu yonse ya anthu.Adzakuchitira zomwe unawachitira ena;zochita zako zidzakubwerera wekha. 16 Iwe unamwa pa phiri langa loyera,koteronso mitundu ina yonse idzamwa kosalekeza;iwo adzamwa ndi kudzandirandipo adzayiwalika pa mbiri ya dziko lapansi. 17 Koma pa Phiri la Ziyoni padzakhala chipulumutso;phirilo lidzakhala lopatulika,ndipo nyumba ya Yakoboidzalandira cholowa chake. 18 Nyumba ya Yakobo idzasanduka motondipo nyumba ya Yosefe idzasanduka lawi la moto;nyumba ya Esau idzasanduka chiputu,ndipo adzayitenthe pa moto ndi kuyipsereza.Sipadzakhala anthu opulumukakuchokera mʼnyumba ya Esau.”Yehova wayankhula. 19 Anthu ochokera ku Negevi adzakhalaku mapiri a Esau,ndipo anthu ochokera mʼmbali mwa mapiriadzatenga dziko la Afilisti.Adzakhala mʼminda ya Efereimu ndi Samariya,ndipo Benjamini adzatenga Giliyadi. 20 Aisraeli amene ali ku ukapoloadzalandira dziko la Kanaani mpaka ku Zarefati;a ku Yerusalemu amene ali ku ukapolo ku Sefaradiadzalandira mizinda ya ku Negevi. 21 Opulumukawo adzapita ku Phiri la Ziyonindipo adzalamulira mapiri a Esau.Koma ufumuwo udzakhala wa Yehova.

In Other Versions

Obadiah 1 in the ANGEFD

Obadiah 1 in the ANTPNG2D

Obadiah 1 in the AS21

Obadiah 1 in the BAGH

Obadiah 1 in the BBPNG

Obadiah 1 in the BBT1E

Obadiah 1 in the BDS

Obadiah 1 in the BEV

Obadiah 1 in the BHAD

Obadiah 1 in the BIB

Obadiah 1 in the BLPT

Obadiah 1 in the BNT

Obadiah 1 in the BNTABOOT

Obadiah 1 in the BNTLV

Obadiah 1 in the BOATCB

Obadiah 1 in the BOATCB2

Obadiah 1 in the BOBCV

Obadiah 1 in the BOCNT

Obadiah 1 in the BOECS

Obadiah 1 in the BOHCB

Obadiah 1 in the BOHCV

Obadiah 1 in the BOHLNT

Obadiah 1 in the BOHNTLTAL

Obadiah 1 in the BOICB

Obadiah 1 in the BOILNTAP

Obadiah 1 in the BOITCV

Obadiah 1 in the BOKCV

Obadiah 1 in the BOKCV2

Obadiah 1 in the BOKHWOG

Obadiah 1 in the BOKSSV

Obadiah 1 in the BOLCB

Obadiah 1 in the BOLCB2

Obadiah 1 in the BOMCV

Obadiah 1 in the BONAV

Obadiah 1 in the BONCB

Obadiah 1 in the BONLT

Obadiah 1 in the BONUT2

Obadiah 1 in the BOPLNT

Obadiah 1 in the BOSCB

Obadiah 1 in the BOSNC

Obadiah 1 in the BOTLNT

Obadiah 1 in the BOVCB

Obadiah 1 in the BOYCB

Obadiah 1 in the BPBB

Obadiah 1 in the BPH

Obadiah 1 in the BSB

Obadiah 1 in the CCB

Obadiah 1 in the CUV

Obadiah 1 in the CUVS

Obadiah 1 in the DBT

Obadiah 1 in the DGDNT

Obadiah 1 in the DHNT

Obadiah 1 in the DNT

Obadiah 1 in the ELBE

Obadiah 1 in the EMTV

Obadiah 1 in the ESV

Obadiah 1 in the FBV

Obadiah 1 in the FEB

Obadiah 1 in the GGMNT

Obadiah 1 in the GNT

Obadiah 1 in the HARY

Obadiah 1 in the HNT

Obadiah 1 in the IRVA

Obadiah 1 in the IRVB

Obadiah 1 in the IRVG

Obadiah 1 in the IRVH

Obadiah 1 in the IRVK

Obadiah 1 in the IRVM

Obadiah 1 in the IRVM2

Obadiah 1 in the IRVO

Obadiah 1 in the IRVP

Obadiah 1 in the IRVT

Obadiah 1 in the IRVT2

Obadiah 1 in the IRVU

Obadiah 1 in the ISVN

Obadiah 1 in the JSNT

Obadiah 1 in the KAPI

Obadiah 1 in the KBT1ETNIK

Obadiah 1 in the KBV

Obadiah 1 in the KJV

Obadiah 1 in the KNFD

Obadiah 1 in the LBA

Obadiah 1 in the LBLA

Obadiah 1 in the LNT

Obadiah 1 in the LSV

Obadiah 1 in the MAAL

Obadiah 1 in the MBV

Obadiah 1 in the MBV2

Obadiah 1 in the MHNT

Obadiah 1 in the MKNFD

Obadiah 1 in the MNG

Obadiah 1 in the MNT

Obadiah 1 in the MNT2

Obadiah 1 in the MRS1T

Obadiah 1 in the NAA

Obadiah 1 in the NASB

Obadiah 1 in the NBLA

Obadiah 1 in the NBS

Obadiah 1 in the NBVTP

Obadiah 1 in the NET2

Obadiah 1 in the NIV11

Obadiah 1 in the NNT

Obadiah 1 in the NNT2

Obadiah 1 in the NNT3

Obadiah 1 in the PDDPT

Obadiah 1 in the PFNT

Obadiah 1 in the RMNT

Obadiah 1 in the SBIAS

Obadiah 1 in the SBIBS

Obadiah 1 in the SBIBS2

Obadiah 1 in the SBICS

Obadiah 1 in the SBIDS

Obadiah 1 in the SBIGS

Obadiah 1 in the SBIHS

Obadiah 1 in the SBIIS

Obadiah 1 in the SBIIS2

Obadiah 1 in the SBIIS3

Obadiah 1 in the SBIKS

Obadiah 1 in the SBIKS2

Obadiah 1 in the SBIMS

Obadiah 1 in the SBIOS

Obadiah 1 in the SBIPS

Obadiah 1 in the SBISS

Obadiah 1 in the SBITS

Obadiah 1 in the SBITS2

Obadiah 1 in the SBITS3

Obadiah 1 in the SBITS4

Obadiah 1 in the SBIUS

Obadiah 1 in the SBIVS

Obadiah 1 in the SBT

Obadiah 1 in the SBT1E

Obadiah 1 in the SCHL

Obadiah 1 in the SNT

Obadiah 1 in the SUSU

Obadiah 1 in the SUSU2

Obadiah 1 in the SYNO

Obadiah 1 in the TBIAOTANT

Obadiah 1 in the TBT1E

Obadiah 1 in the TBT1E2

Obadiah 1 in the TFTIP

Obadiah 1 in the TFTU

Obadiah 1 in the TGNTATF3T

Obadiah 1 in the THAI

Obadiah 1 in the TNFD

Obadiah 1 in the TNT

Obadiah 1 in the TNTIK

Obadiah 1 in the TNTIL

Obadiah 1 in the TNTIN

Obadiah 1 in the TNTIP

Obadiah 1 in the TNTIZ

Obadiah 1 in the TOMA

Obadiah 1 in the TTENT

Obadiah 1 in the UBG

Obadiah 1 in the UGV

Obadiah 1 in the UGV2

Obadiah 1 in the UGV3

Obadiah 1 in the VBL

Obadiah 1 in the VDCC

Obadiah 1 in the YALU

Obadiah 1 in the YAPE

Obadiah 1 in the YBVTP

Obadiah 1 in the ZBP