Isaiah 23 (BOGWICC)

1 Uthenga wonena za Turo:Lirani mofuwula, inu oyendetsa sitima za pa madzi za ku Tarisisi:pakuti mzinda wa Turo wawonongedwandipo mulibe nyumba kapena dooko.Zimenezi anazimvapochokera ku Kitimu. 2 Khalani chete inu anthu okhala mʼmbali mwa nyanja,inu amalonda a ku Sidoni,iwe amene unalemera ndi anthu oyenda pa nyanja. 3 Pa nyanja zazikulupanabwera tirigu wa ku Sihori;zokolola za ku Nailo, ndipo munachita malondandi anthu a mitundu ina. 4 Chita manyazi, iwe Sidimupakuti nyanja yayankhula, linga la ku nyanja (Turo) layankhula kuti,“Sindinamvepo zowawa za kubereka kapena kuberekapo mwana;sindinalerepo ana aamuna kapena kulera ana aakazi.” 5 Mawuwa akadzamveka ku Igupto,iwo adzachita mantha akadzamva kuti Turo wawonongeka. 6 Wolokerani ku Tarisisi,lirani mofuwula, inu anthu okhala mʼmbali mwa nyanja. 7 Kodi uwu si mzinda wachisangalalo uja,mzinda wakalekale,umene anthu ake ankapitakukakhala ku mayiko akutali? 8 Kodi ndani anakonza zimenezi kuti zigwere Turo, mzinda umene unakhazikitsa mizinda ina,mzinda umene amalonda ake ndi akalongandi otchukapa dziko lapansi? 9 Yehova Wamphamvuzonse anakonza zimenezikuti athetse kunyada kwawondi kutsitsa anthu otchuka a pa dziko lapansi. 10 Mubalalike mʼdziko mwanu ngati mtsinje wa Nailoinu anthu a ku Tarisisi,pakuti mulibenso chokutetezani. 11 Yehova watambasula dzanja lake kuloza ku nyanjandipo wagwedeza maufumu ake.Iye walamula kuti Kanaaniagwetse malinga ake. 12 Iye anati, “Simudzakondwanso konse,inu anthu opanikizidwa a ku Sidoni, tsopano wamphwanyidwa! “Ngakhale muwolokere ku Kitimu,kumeneko simukapezako mpumulo.” 13 Onani dziko la Ababuloni,anthu amenewa tsopano atheratu!Asiriya asandutsa Turo kukhalamalo a zirombo za ku chipululu;anamanga nsanja zawo za nkhondo,anagumula malinga akendipo anawasandutsa bwinja. 14 Lirani mofuwula, inu anthu oyendetsa sitima za pa madzi za ku Tarisisi;chifukwa malinga ako agwetsedwa! 15 Pa nthawi imeneyo Turo adzayiwalika pa zaka 70, amene ndi masiku a moyo wa mfumu. Koma potsiriza pa zaka 70 zimenezi, Turo adzakhala ngati mkazi wachiwerewere woyimbidwa mu nyimbo: 16 “Tenga zeze wako uzungulire mzinda,iwe mkazi wachiwerewere woyiwalika;imba zeze mokometsera, imba nyimbo zambiri,kuti anthu akukumbukire.” 17 Pakutha pa zaka 70, Yehova adzachitapo kanthu pa Turo. Iye adzabwerera ku ntchito yake yakale monga mkazi wachiwerewere ndipo adzachita zachiwerewere ndi maufumu onse a dziko lapansi. 18 Koma phindu lake ndi malipiro ake adzazipereka kwa Yehova; sadzazikundika kapena kuzisunga. Phindu lake lidzapita kwa mtumiki wa Yehova kuti agule zakudya zambiri ndi zovala zokongola.

In Other Versions

Isaiah 23 in the ANGEFD

Isaiah 23 in the ANTPNG2D

Isaiah 23 in the AS21

Isaiah 23 in the BAGH

Isaiah 23 in the BBPNG

Isaiah 23 in the BBT1E

Isaiah 23 in the BDS

Isaiah 23 in the BEV

Isaiah 23 in the BHAD

Isaiah 23 in the BIB

Isaiah 23 in the BLPT

Isaiah 23 in the BNT

Isaiah 23 in the BNTABOOT

Isaiah 23 in the BNTLV

Isaiah 23 in the BOATCB

Isaiah 23 in the BOATCB2

Isaiah 23 in the BOBCV

Isaiah 23 in the BOCNT

Isaiah 23 in the BOECS

Isaiah 23 in the BOHCB

Isaiah 23 in the BOHCV

Isaiah 23 in the BOHLNT

Isaiah 23 in the BOHNTLTAL

Isaiah 23 in the BOICB

Isaiah 23 in the BOILNTAP

Isaiah 23 in the BOITCV

Isaiah 23 in the BOKCV

Isaiah 23 in the BOKCV2

Isaiah 23 in the BOKHWOG

Isaiah 23 in the BOKSSV

Isaiah 23 in the BOLCB

Isaiah 23 in the BOLCB2

Isaiah 23 in the BOMCV

Isaiah 23 in the BONAV

Isaiah 23 in the BONCB

Isaiah 23 in the BONLT

Isaiah 23 in the BONUT2

Isaiah 23 in the BOPLNT

Isaiah 23 in the BOSCB

Isaiah 23 in the BOSNC

Isaiah 23 in the BOTLNT

Isaiah 23 in the BOVCB

Isaiah 23 in the BOYCB

Isaiah 23 in the BPBB

Isaiah 23 in the BPH

Isaiah 23 in the BSB

Isaiah 23 in the CCB

Isaiah 23 in the CUV

Isaiah 23 in the CUVS

Isaiah 23 in the DBT

Isaiah 23 in the DGDNT

Isaiah 23 in the DHNT

Isaiah 23 in the DNT

Isaiah 23 in the ELBE

Isaiah 23 in the EMTV

Isaiah 23 in the ESV

Isaiah 23 in the FBV

Isaiah 23 in the FEB

Isaiah 23 in the GGMNT

Isaiah 23 in the GNT

Isaiah 23 in the HARY

Isaiah 23 in the HNT

Isaiah 23 in the IRVA

Isaiah 23 in the IRVB

Isaiah 23 in the IRVG

Isaiah 23 in the IRVH

Isaiah 23 in the IRVK

Isaiah 23 in the IRVM

Isaiah 23 in the IRVM2

Isaiah 23 in the IRVO

Isaiah 23 in the IRVP

Isaiah 23 in the IRVT

Isaiah 23 in the IRVT2

Isaiah 23 in the IRVU

Isaiah 23 in the ISVN

Isaiah 23 in the JSNT

Isaiah 23 in the KAPI

Isaiah 23 in the KBT1ETNIK

Isaiah 23 in the KBV

Isaiah 23 in the KJV

Isaiah 23 in the KNFD

Isaiah 23 in the LBA

Isaiah 23 in the LBLA

Isaiah 23 in the LNT

Isaiah 23 in the LSV

Isaiah 23 in the MAAL

Isaiah 23 in the MBV

Isaiah 23 in the MBV2

Isaiah 23 in the MHNT

Isaiah 23 in the MKNFD

Isaiah 23 in the MNG

Isaiah 23 in the MNT

Isaiah 23 in the MNT2

Isaiah 23 in the MRS1T

Isaiah 23 in the NAA

Isaiah 23 in the NASB

Isaiah 23 in the NBLA

Isaiah 23 in the NBS

Isaiah 23 in the NBVTP

Isaiah 23 in the NET2

Isaiah 23 in the NIV11

Isaiah 23 in the NNT

Isaiah 23 in the NNT2

Isaiah 23 in the NNT3

Isaiah 23 in the PDDPT

Isaiah 23 in the PFNT

Isaiah 23 in the RMNT

Isaiah 23 in the SBIAS

Isaiah 23 in the SBIBS

Isaiah 23 in the SBIBS2

Isaiah 23 in the SBICS

Isaiah 23 in the SBIDS

Isaiah 23 in the SBIGS

Isaiah 23 in the SBIHS

Isaiah 23 in the SBIIS

Isaiah 23 in the SBIIS2

Isaiah 23 in the SBIIS3

Isaiah 23 in the SBIKS

Isaiah 23 in the SBIKS2

Isaiah 23 in the SBIMS

Isaiah 23 in the SBIOS

Isaiah 23 in the SBIPS

Isaiah 23 in the SBISS

Isaiah 23 in the SBITS

Isaiah 23 in the SBITS2

Isaiah 23 in the SBITS3

Isaiah 23 in the SBITS4

Isaiah 23 in the SBIUS

Isaiah 23 in the SBIVS

Isaiah 23 in the SBT

Isaiah 23 in the SBT1E

Isaiah 23 in the SCHL

Isaiah 23 in the SNT

Isaiah 23 in the SUSU

Isaiah 23 in the SUSU2

Isaiah 23 in the SYNO

Isaiah 23 in the TBIAOTANT

Isaiah 23 in the TBT1E

Isaiah 23 in the TBT1E2

Isaiah 23 in the TFTIP

Isaiah 23 in the TFTU

Isaiah 23 in the TGNTATF3T

Isaiah 23 in the THAI

Isaiah 23 in the TNFD

Isaiah 23 in the TNT

Isaiah 23 in the TNTIK

Isaiah 23 in the TNTIL

Isaiah 23 in the TNTIN

Isaiah 23 in the TNTIP

Isaiah 23 in the TNTIZ

Isaiah 23 in the TOMA

Isaiah 23 in the TTENT

Isaiah 23 in the UBG

Isaiah 23 in the UGV

Isaiah 23 in the UGV2

Isaiah 23 in the UGV3

Isaiah 23 in the VBL

Isaiah 23 in the VDCC

Isaiah 23 in the YALU

Isaiah 23 in the YAPE

Isaiah 23 in the YBVTP

Isaiah 23 in the ZBP