Jeremiah 8 (BOGWICC)
1 Yehova akuti, “ ‘Pa nthawi imeneyo, mafupa a mafumu ndi a akuluakulu a ku Yuda, mafupa a ansembe ndi a aneneri, ndiponso mafupa a anthu a ku Yerusalemu adzafukulidwa. 2 Adzawamwaza pa nthaka kuyangʼana dzuwa, mwezi ndi nyenyezi zonse zamlengalenga, zimene ankazikonda, kuzitumikira ndi kuzitsatira, kupemphako nzeru ndiponso kuzilambira. Mafupawo sadzawasonkhanitsa kapena kuwakwirira, koma adzakhala ngati ndowe pamwamba pa nthaka. 3 Otsala onse a mtundu woyipawu adzafuna imfa kopambana moyo kulikonse kumene ndidzawapirikitsirako, akutero Yehova Wamphamvuzonse.’ ” 4 “Tsono awuze anthuwa, ‘Yehova akuti:“ ‘Kodi anthu akagwa sangadzukenso?Munthu akasochera kodi sangathe kubwereranso? 5 Chifukwa chiyani nanga anthu awa akupitirirabe kuchimwa, osabwerera?Chifukwa chiyani Yerusalemu akubwerera mʼmbuyo?Iwo akangamira chinyengo;akukana kubwerera. 6 Ine ndinatchera khutu kumvetserakoma iwo sanayankhulepo zoona.Palibe woyipa amene analapapo zoyipa zake,nʼkumati, ‘Ine ndachita chiyani?’Aliyense akutsatira njira yakengati kavalo wothamangira nkhondo. 7 Mbalame yotchedwa kakowa ija imadziwanthawi yake mlengalenga.Koma nkhunda, namzeze ndi chingaluzimadziwa nthawi yonyamukira ulendo,koma anthu anga sadziwamalamulo a Yehova. 8 “ ‘Inu mukunena bwanji kuti,‘Ndife anzeru ndipo timasunga malamulo a Yehova?’Koma ndi alembi anuamene akulemba zabodza. 9 Anthu anzeru achita manyazi;athedwa nzeru ndipo agwidwa.Iwo anakana mawu a Yehova.Nanga tsono nzeru zawo ziwapinduliranji? 10 Nʼchifukwa chake akazi awo ndidzawapereka kwa amuna enandipo minda yawo ndidzayipereka kwa amene adzawagonjetse.Kuyambira wamngʼono mpaka wamkulu,onse ali ndi khalidwe lofuna kupeza chuma mwakuba.Aneneri pamodzi ndi ansembe omwe,onse amachita zachinyengo. 11 Iwo amapoletsa zilonda za anthu angapamwamba chabenʼkumati, ‘Mtendere, mtendere,’pamene palibe mtendere. 12 Kodi amachita manyazi akamachita zonyansazi?Ayi, alibe manyazi ndi pangʼono pomwe;iwo sadziwa nʼkugwetsa nkhope komwe.Choncho iwo adzagwera pakati pa anzawo amene agwa kale;adzagwa pansi tsiku limene ndidzawalanga,akutero Yehova. 13 “ ‘Ndidzatenga zokolola zawo,Sipadzakhalanso mphesa pa mpesakapena nkhuyu pa mkuyu,ndipo masamba ake adzawuma.Zinthu zimene ndinawapatsandidzawachotsera.’ ” 14 Koma amati, “Tikukhala pano chifukwa chiyani?Tiyeni tonse pamodzitithawire ku mizinda yotetezedwandi kukafera kumeneko.Pakuti Yehova Mulungu wathu watsimikiza kuti tiyenera kufa.Watipatsa madzi aululu kuti timwe,chifukwa tamuchimwira. 15 Tinkayembekezera mtenderekoma palibe chabwino chomwe chinachitika,tinkayembekezera kuchirakoma tinakumana ndi zoopsa zokhazokha. 16 Kulira kwa ngʼombe zazimuna za mdanikukumveka kuchokera ku Dani;dziko lonse likunjenjemerachifukwa cha kulira kwa akavalowo.Akubwera kudzawononga dzikondi zonse zimene zili mʼmenemo.Adzawononga mzinda ndi onse okhalamo.” 17 Yehova akuti, “Onani, ndikukutumizirani njoka zaululu,mphiri zimene munthu sangathe kuzilodza,ndipo zidzakulumani,” 18 Ndadzazidwa ndi chisoni kwambiri,mtima wanga walefukiratu. 19 Imvani kulira kwa anthu angakuchokera ku dziko lakutali:akuti, “Kodi Yehova sali ku Ziyoni?Kodi mfumu yake sili kumeneko?” “Chifukwa chiyani akundiputa ndi mafano awo osema,ndi milungu yawo yachilendo?” 20 “Nthawi yokolola yapita,chilimwe chapita,koma sitinapulumuke.” 21 Chifukwa cha mavuto a anthu anga, ine ndikumva kuwawa;ndikungolira ndipo mantha aakulu andigwira. 22 Kodi ku Giliyadi kulibe mankhwala ochiritsa?Kodi kumeneko kulibe singʼanga?Nanga chifukwa chiyani mabalaa anthu anga sanapole?
In Other Versions
Jeremiah 8 in the ANGEFD
Jeremiah 8 in the ANTPNG2D
Jeremiah 8 in the AS21
Jeremiah 8 in the BAGH
Jeremiah 8 in the BBPNG
Jeremiah 8 in the BBT1E
Jeremiah 8 in the BDS
Jeremiah 8 in the BEV
Jeremiah 8 in the BHAD
Jeremiah 8 in the BIB
Jeremiah 8 in the BLPT
Jeremiah 8 in the BNT
Jeremiah 8 in the BNTABOOT
Jeremiah 8 in the BNTLV
Jeremiah 8 in the BOATCB
Jeremiah 8 in the BOATCB2
Jeremiah 8 in the BOBCV
Jeremiah 8 in the BOCNT
Jeremiah 8 in the BOECS
Jeremiah 8 in the BOHCB
Jeremiah 8 in the BOHCV
Jeremiah 8 in the BOHLNT
Jeremiah 8 in the BOHNTLTAL
Jeremiah 8 in the BOICB
Jeremiah 8 in the BOILNTAP
Jeremiah 8 in the BOITCV
Jeremiah 8 in the BOKCV
Jeremiah 8 in the BOKCV2
Jeremiah 8 in the BOKHWOG
Jeremiah 8 in the BOKSSV
Jeremiah 8 in the BOLCB
Jeremiah 8 in the BOLCB2
Jeremiah 8 in the BOMCV
Jeremiah 8 in the BONAV
Jeremiah 8 in the BONCB
Jeremiah 8 in the BONLT
Jeremiah 8 in the BONUT2
Jeremiah 8 in the BOPLNT
Jeremiah 8 in the BOSCB
Jeremiah 8 in the BOSNC
Jeremiah 8 in the BOTLNT
Jeremiah 8 in the BOVCB
Jeremiah 8 in the BOYCB
Jeremiah 8 in the BPBB
Jeremiah 8 in the BPH
Jeremiah 8 in the BSB
Jeremiah 8 in the CCB
Jeremiah 8 in the CUV
Jeremiah 8 in the CUVS
Jeremiah 8 in the DBT
Jeremiah 8 in the DGDNT
Jeremiah 8 in the DHNT
Jeremiah 8 in the DNT
Jeremiah 8 in the ELBE
Jeremiah 8 in the EMTV
Jeremiah 8 in the ESV
Jeremiah 8 in the FBV
Jeremiah 8 in the FEB
Jeremiah 8 in the GGMNT
Jeremiah 8 in the GNT
Jeremiah 8 in the HARY
Jeremiah 8 in the HNT
Jeremiah 8 in the IRVA
Jeremiah 8 in the IRVB
Jeremiah 8 in the IRVG
Jeremiah 8 in the IRVH
Jeremiah 8 in the IRVK
Jeremiah 8 in the IRVM
Jeremiah 8 in the IRVM2
Jeremiah 8 in the IRVO
Jeremiah 8 in the IRVP
Jeremiah 8 in the IRVT
Jeremiah 8 in the IRVT2
Jeremiah 8 in the IRVU
Jeremiah 8 in the ISVN
Jeremiah 8 in the JSNT
Jeremiah 8 in the KAPI
Jeremiah 8 in the KBT1ETNIK
Jeremiah 8 in the KBV
Jeremiah 8 in the KJV
Jeremiah 8 in the KNFD
Jeremiah 8 in the LBA
Jeremiah 8 in the LBLA
Jeremiah 8 in the LNT
Jeremiah 8 in the LSV
Jeremiah 8 in the MAAL
Jeremiah 8 in the MBV
Jeremiah 8 in the MBV2
Jeremiah 8 in the MHNT
Jeremiah 8 in the MKNFD
Jeremiah 8 in the MNG
Jeremiah 8 in the MNT
Jeremiah 8 in the MNT2
Jeremiah 8 in the MRS1T
Jeremiah 8 in the NAA
Jeremiah 8 in the NASB
Jeremiah 8 in the NBLA
Jeremiah 8 in the NBS
Jeremiah 8 in the NBVTP
Jeremiah 8 in the NET2
Jeremiah 8 in the NIV11
Jeremiah 8 in the NNT
Jeremiah 8 in the NNT2
Jeremiah 8 in the NNT3
Jeremiah 8 in the PDDPT
Jeremiah 8 in the PFNT
Jeremiah 8 in the RMNT
Jeremiah 8 in the SBIAS
Jeremiah 8 in the SBIBS
Jeremiah 8 in the SBIBS2
Jeremiah 8 in the SBICS
Jeremiah 8 in the SBIDS
Jeremiah 8 in the SBIGS
Jeremiah 8 in the SBIHS
Jeremiah 8 in the SBIIS
Jeremiah 8 in the SBIIS2
Jeremiah 8 in the SBIIS3
Jeremiah 8 in the SBIKS
Jeremiah 8 in the SBIKS2
Jeremiah 8 in the SBIMS
Jeremiah 8 in the SBIOS
Jeremiah 8 in the SBIPS
Jeremiah 8 in the SBISS
Jeremiah 8 in the SBITS
Jeremiah 8 in the SBITS2
Jeremiah 8 in the SBITS3
Jeremiah 8 in the SBITS4
Jeremiah 8 in the SBIUS
Jeremiah 8 in the SBIVS
Jeremiah 8 in the SBT
Jeremiah 8 in the SBT1E
Jeremiah 8 in the SCHL
Jeremiah 8 in the SNT
Jeremiah 8 in the SUSU
Jeremiah 8 in the SUSU2
Jeremiah 8 in the SYNO
Jeremiah 8 in the TBIAOTANT
Jeremiah 8 in the TBT1E
Jeremiah 8 in the TBT1E2
Jeremiah 8 in the TFTIP
Jeremiah 8 in the TFTU
Jeremiah 8 in the TGNTATF3T
Jeremiah 8 in the THAI
Jeremiah 8 in the TNFD
Jeremiah 8 in the TNT
Jeremiah 8 in the TNTIK
Jeremiah 8 in the TNTIL
Jeremiah 8 in the TNTIN
Jeremiah 8 in the TNTIP
Jeremiah 8 in the TNTIZ
Jeremiah 8 in the TOMA
Jeremiah 8 in the TTENT
Jeremiah 8 in the UBG
Jeremiah 8 in the UGV
Jeremiah 8 in the UGV2
Jeremiah 8 in the UGV3
Jeremiah 8 in the VBL
Jeremiah 8 in the VDCC
Jeremiah 8 in the YALU
Jeremiah 8 in the YAPE
Jeremiah 8 in the YBVTP
Jeremiah 8 in the ZBP