Isaiah 22 (BOGWICC)

1 Uthenga wonena za Chigwa cha Masomphenya:Kodi chachitika nʼchiyani,kuti nonsenu mukwere pa madenga? 2 Iwe mzinda wodzaza ndi chisangalalo chodzaza tsaya,iwe mzinda waphokoso ndi wosokonekera?Anthu ako ophedwa aja sanaphedwe ndi lupanga,kapena kufera pa nkhondo. 3 Atsogoleri ako onse ngakhale anathawa limodzi;koma anagwidwa osadziteteza nʼkomwe.Inu munapezeka ndipo nonse pamodzi munatengedwa ukapolo,ngakhale munathawa pamene mdani akanali patali. 4 Nʼchifukwa chake Ine ndinati, “Chokani pamaso panga;ndilekeni ndilire ndi mtima wowawa.Musayesere kunditonthozachifukwa cha kuwonongeka kwa anthu anga.” 5 Lero Ambuye Yehova Wamphamvuzonse walola kuti tionemavuto ndi kugonjetsedwa ndiponso chisokonezomʼChigwa cha Masomphenya.Malinga agumuka,komanso anthu akanalira mofuwula ku mapiri. 6 Ankhondo a ku Elamu anadza pa magaletandi akavalo ali ndi mivi mʼmanja.Ankhondo a ku Kiri anakonzeka ndi zishango. 7 Zigwa zanu zachonde ndi zodzaza ndi magaleta,ndipo asilikali okwera pa akavalo ayikidwa pa zipata za mzinda; 8 zonse zoteteza Yuda zachotsedwa. Ndipo tsiku limenelo munayangʼanayangʼanazida zankhondo zomwe zinali mʼnyumba yaufumu ya nkhalango; 9 inu munaona kuti makoma ambiri a mzinda wa Davideanali ndi malo ambiri ogumuka;munasunga madzimu chidziwe chakumunsi. 10 Munawerenga nyumba zonse za mu Yerusalemundipo munagwetsa nyumba zina kuti mulimbitse linga logumuka lija. 11 Pakati pa makoma awiri munamanga chitsimechosungiramo madzi ochokera ku dziwe lakale,koma inu simunadalire Mulungu amene anapanga zimenezi,kapena kusamalako za Iye amene anazilenga kale lomwe. 12 Pa tsiku limenelo, Ambuye Yehova Wamphamvuzonseanakuyitanani kuti mulire ndi kukhetsa misozi;kumeta mutu wanu mpalandi kuvala ziguduli. 13 Koma mʼmalo mwake inu munakondwa ndi kusangalala;munapha ngʼombe ndi nkhosa;munadya nyama ndi kumwa vinyo.Inu mumati, “Tiyeni tidye ndi kumwapakuti mawa tifa!” 14 Yehova Wamphamvuzonse wandiwululira mondinongʼoneza kuti, “Tchimo limeneli sindidzakhululuka mpaka tsiku la kufa kwanu,” akutero Ambuye, Yehova Wamphamvuzonse. 15 Chimene Ambuye, Yehova Wamphamvuzonse akuti,“Pita, ukanene kwa Sabina kapitawo,amene amayangʼanira nyumba yaufumu: 16 Kodi ukuchita chiyani kuno, nanga ndani anakupatsa chilolezokuti udzikumbire manda kuno,kudzikumbira manda pa phirindi kudzisemera malo opumulira mʼthanthwe? 17 “Samalira, Yehova watsala pangʼono kukugwira zolimbandi kukuponya mwamphamvu, iwe munthu wamphamvu. 18 Iye adzakukulunga kwambiri ngati mpirandipo adzakuponyera mʼdziko lalikulu.Kumeneko ndiko ukaferendipo kumeneko ndiko kudzatsalire magaleta ako.Ndipo udzasanduka wochititsa manyazi nyumba ya mbuye wako. 19 Ine ndidzakuchotsa pa ukapitawo wakondipo ndidzakutsitsa pa udindo wako. 20 “Tsiku limenelo ndidzayitanitsa mtumiki wanga, Eliyakimu mwana wa Hilikiya. 21 Ndidzamuveka mkanjo wako ndi kumangira lamba wako mʼchiwuno mwake ndi kumupatsa ulamuliro wako. Iye adzakhala kholo la amene amakhala mu Yerusalemu ndiponso a fuko la Yuda. 22 Ndidzamupatsa ulamuliro wa banja la Davide. Adzatsekula ndipo palibe adzatseke, adzatseka popanda wina kutsekula. 23 Ufumu wake udzakhala wokhazikika ngati chikhomo chokhomedwa pa malo olimba. Anthu adzalemekeza nyumba ya abale ake chifukwa cha iye. 24 Ana ndi abale a nyumba ya abambo ake adzakhala ngati katundu pa iye ngati ziwiya zopanda ntchito zimene zapachikidwa pa chikhomo. 25 “Yehova Wamphamvuzonse akunena kuti, ‘Tsiku limeneli chikhomo chokhomedwa kwambiri chija sichidzalimbanso; chidzazuka ndipo chidzagwa ndipo zonse zopachikidwa zidzawonongedwa.’ ” Yehova wayankhula chomwechi.

In Other Versions

Isaiah 22 in the ANGEFD

Isaiah 22 in the ANTPNG2D

Isaiah 22 in the AS21

Isaiah 22 in the BAGH

Isaiah 22 in the BBPNG

Isaiah 22 in the BBT1E

Isaiah 22 in the BDS

Isaiah 22 in the BEV

Isaiah 22 in the BHAD

Isaiah 22 in the BIB

Isaiah 22 in the BLPT

Isaiah 22 in the BNT

Isaiah 22 in the BNTABOOT

Isaiah 22 in the BNTLV

Isaiah 22 in the BOATCB

Isaiah 22 in the BOATCB2

Isaiah 22 in the BOBCV

Isaiah 22 in the BOCNT

Isaiah 22 in the BOECS

Isaiah 22 in the BOHCB

Isaiah 22 in the BOHCV

Isaiah 22 in the BOHLNT

Isaiah 22 in the BOHNTLTAL

Isaiah 22 in the BOICB

Isaiah 22 in the BOILNTAP

Isaiah 22 in the BOITCV

Isaiah 22 in the BOKCV

Isaiah 22 in the BOKCV2

Isaiah 22 in the BOKHWOG

Isaiah 22 in the BOKSSV

Isaiah 22 in the BOLCB

Isaiah 22 in the BOLCB2

Isaiah 22 in the BOMCV

Isaiah 22 in the BONAV

Isaiah 22 in the BONCB

Isaiah 22 in the BONLT

Isaiah 22 in the BONUT2

Isaiah 22 in the BOPLNT

Isaiah 22 in the BOSCB

Isaiah 22 in the BOSNC

Isaiah 22 in the BOTLNT

Isaiah 22 in the BOVCB

Isaiah 22 in the BOYCB

Isaiah 22 in the BPBB

Isaiah 22 in the BPH

Isaiah 22 in the BSB

Isaiah 22 in the CCB

Isaiah 22 in the CUV

Isaiah 22 in the CUVS

Isaiah 22 in the DBT

Isaiah 22 in the DGDNT

Isaiah 22 in the DHNT

Isaiah 22 in the DNT

Isaiah 22 in the ELBE

Isaiah 22 in the EMTV

Isaiah 22 in the ESV

Isaiah 22 in the FBV

Isaiah 22 in the FEB

Isaiah 22 in the GGMNT

Isaiah 22 in the GNT

Isaiah 22 in the HARY

Isaiah 22 in the HNT

Isaiah 22 in the IRVA

Isaiah 22 in the IRVB

Isaiah 22 in the IRVG

Isaiah 22 in the IRVH

Isaiah 22 in the IRVK

Isaiah 22 in the IRVM

Isaiah 22 in the IRVM2

Isaiah 22 in the IRVO

Isaiah 22 in the IRVP

Isaiah 22 in the IRVT

Isaiah 22 in the IRVT2

Isaiah 22 in the IRVU

Isaiah 22 in the ISVN

Isaiah 22 in the JSNT

Isaiah 22 in the KAPI

Isaiah 22 in the KBT1ETNIK

Isaiah 22 in the KBV

Isaiah 22 in the KJV

Isaiah 22 in the KNFD

Isaiah 22 in the LBA

Isaiah 22 in the LBLA

Isaiah 22 in the LNT

Isaiah 22 in the LSV

Isaiah 22 in the MAAL

Isaiah 22 in the MBV

Isaiah 22 in the MBV2

Isaiah 22 in the MHNT

Isaiah 22 in the MKNFD

Isaiah 22 in the MNG

Isaiah 22 in the MNT

Isaiah 22 in the MNT2

Isaiah 22 in the MRS1T

Isaiah 22 in the NAA

Isaiah 22 in the NASB

Isaiah 22 in the NBLA

Isaiah 22 in the NBS

Isaiah 22 in the NBVTP

Isaiah 22 in the NET2

Isaiah 22 in the NIV11

Isaiah 22 in the NNT

Isaiah 22 in the NNT2

Isaiah 22 in the NNT3

Isaiah 22 in the PDDPT

Isaiah 22 in the PFNT

Isaiah 22 in the RMNT

Isaiah 22 in the SBIAS

Isaiah 22 in the SBIBS

Isaiah 22 in the SBIBS2

Isaiah 22 in the SBICS

Isaiah 22 in the SBIDS

Isaiah 22 in the SBIGS

Isaiah 22 in the SBIHS

Isaiah 22 in the SBIIS

Isaiah 22 in the SBIIS2

Isaiah 22 in the SBIIS3

Isaiah 22 in the SBIKS

Isaiah 22 in the SBIKS2

Isaiah 22 in the SBIMS

Isaiah 22 in the SBIOS

Isaiah 22 in the SBIPS

Isaiah 22 in the SBISS

Isaiah 22 in the SBITS

Isaiah 22 in the SBITS2

Isaiah 22 in the SBITS3

Isaiah 22 in the SBITS4

Isaiah 22 in the SBIUS

Isaiah 22 in the SBIVS

Isaiah 22 in the SBT

Isaiah 22 in the SBT1E

Isaiah 22 in the SCHL

Isaiah 22 in the SNT

Isaiah 22 in the SUSU

Isaiah 22 in the SUSU2

Isaiah 22 in the SYNO

Isaiah 22 in the TBIAOTANT

Isaiah 22 in the TBT1E

Isaiah 22 in the TBT1E2

Isaiah 22 in the TFTIP

Isaiah 22 in the TFTU

Isaiah 22 in the TGNTATF3T

Isaiah 22 in the THAI

Isaiah 22 in the TNFD

Isaiah 22 in the TNT

Isaiah 22 in the TNTIK

Isaiah 22 in the TNTIL

Isaiah 22 in the TNTIN

Isaiah 22 in the TNTIP

Isaiah 22 in the TNTIZ

Isaiah 22 in the TOMA

Isaiah 22 in the TTENT

Isaiah 22 in the UBG

Isaiah 22 in the UGV

Isaiah 22 in the UGV2

Isaiah 22 in the UGV3

Isaiah 22 in the VBL

Isaiah 22 in the VDCC

Isaiah 22 in the YALU

Isaiah 22 in the YAPE

Isaiah 22 in the YBVTP

Isaiah 22 in the ZBP