Psalms 37 (BOGWICC)

undefined Salimo la Davide. 1 Usamavutike chifukwa cha anthu oyipakapena kuchitira nsanje amene akuchita cholakwa; 2 pakuti monga udzu iwo adzafota msanga,ngati mbewu zobiriwira adzanyala msanga. 3 Khulupirira Yehova ndipo uzichita zabwino;khazikika mʼdziko ndi kutsata zokhulupirika. 4 Udzikondweretse wekha mwa Yehovandipo Iye adzakupatsa zokhumba za mtima wako. 5 Pereka njira yako kwa Yehova;dalira Iye ndipo Iyeyo adzachita izi: 6 Iye adzachititsa chilungamo chako kuwala ngati mʼbandakucha,chiweruzo chako ngati dzuwa la masana. 7 Khala chete pamaso pa Yehova ndipo umudikire mofatsa;usavutike pamene anthu apambana mʼnjira zawo,pamene iwo achita zinthu zawo zoyipa. 8 Pewa kupsa mtima ndipo tembenuka kuchoka ku ukali,usavutike chifukwa zimenezi zimatsogolera ku zoyipa. 9 Pakuti anthu oyipa adzachotsedwa,koma iwo amene amayembekeza mwa Yehova adzalandira dziko. 10 Kwa kanthawi oyipa sadzapezekanso;ngakhale muwafunefune, sadzapezekanso. 11 Koma ofatsa adzalandira dzikondipo adzasangalala ndi mtendere waukulu. 12 Oyipa amakonza chiwembu kutsutsana ndi olungamandipo amawakukutira mano; 13 koma Ambuye amaseka oyipapakuti Iye amadziwa kuti tsiku lawo likubwera. 14 Oyipa amasolola lupangandi kupinda utakugwetsa osauka ndi osowa,kupha iwo amene njira zawo ndi zolungama. 15 Koma malupanga awo analasa mitima yawo yomwe,ndipo mauta awo anathyoka. 16 Zabwino zochepa zimene olungama ali nazoziposa chuma cha anthu oyipa ambiri; 17 pakuti mphamvu ya oyipa idzasweka,koma Yehova amasunga olungama. 18 Masiku a anthu osalakwa amadziwika ndi Yehova,ndipo cholowa chawo chidzakhala mpaka muyaya. 19 Pa nthawi ya mavuto iwo sadzafota;mʼmasiku a njala adzakhala ndi zinthu zambiri. 20 Koma oyipa adzawonongeka;adani a Yehova adzakhala ngati kukongola kwa kuthengo,iwo adzazimirira ngati utsi. 21 Oyipa amabwereka ndipo sabwezakoma olungama amapereka mowolowamanja. 22 Iwo amene Yehova amawadalitsa adzalandira dziko,koma amene Iye amawatemberera adzachotsedwa. 23 Ngati Yehova akondwera ndi njira ya munthu,amakhazikitsa mayendedwe ake; 24 ngakhale atapunthwa sadzagwa,pakuti Yehova amamutchinjiriza ndi dzanja lake. 25 Ine ndinali wamngʼono ndipo tsopano ndakalambakoma sindinaonepo olungama akusiyidwakapena ana awo akupempha chakudya. 26 Iwo ndi owolowamanja nthawi zonse ndipo amabwereketsa mwaufulu;ana awo adzadalitsika. 27 Tembenuka kuchoka ku zoyipa ndipo chita zabwino;pamenepo udzakhazikika mʼdziko kwamuyaya. 28 Pakuti Yehova amakonda wolungamandipo sadzasiya okhulupirika ake. Iwo adzatetezedwa kwamuyaya,koma zidzukulu za oyipa zidzachotsedwa; 29 olungama adzalandira dzikondipo adzakhazikikamo kwamuyaya. 30 Pakamwa pa munthu wolungama pamayankhula za nzeru,ndipo lilime lake limayankhula zolungama. 31 Lamulo la Mulungu wake lili mu mtima mwake;mapazi ake saterereka. 32 Oyipa amabisala kudikira olungama;kufunafuna miyoyo yawoyo; 33 koma Yehova sadzawasiya pansi pa mphamvu yawokapena kuti atsutsidwe pamene abweretsedwa pa milandu. 34 Khulupirira Yehova,ndipo sunga njira yake;Iye adzakukweza ndipo udzalandira dziko kuti likhale lako;udzaona anthu oyipa akuwonongeka. 35 Ine ndinaona munthu woyipa ndi munthu wopanda chifundoakupeza bwino ngati mtengo wobiriwira pa nthaka ya makolo ake. 36 Koma sanachedwe kumwalira ndipo sanaonekenso;ngakhale ndinamuyangʼanayangʼana, sanapezekenso. 37 Ganizira za munthu wosalakwa, yangʼanitsitsa munthu wolungama;udzaona kuti ali ndi tsogolo labwino ndipo ali ndi zidzukulu zambiri. 38 Koma anthu ochimwa adzawonongeka;iwowo pamodzi ndi zidzukulu zawo zomwe. 39 Chipulumutso cha olungama chimachokera kwa Yehova;Iye ndiye linga lawo pa nthawi ya masautso. 40 Yehova amawathandiza ndi kuwalanditsa;Iye amawalanditsa kwa oyipa ndi kuwapulumutsa,pakuti amathawira kwa Iye.

In Other Versions

Psalms 37 in the ANGEFD

Psalms 37 in the ANTPNG2D

Psalms 37 in the AS21

Psalms 37 in the BAGH

Psalms 37 in the BBPNG

Psalms 37 in the BBT1E

Psalms 37 in the BDS

Psalms 37 in the BEV

Psalms 37 in the BHAD

Psalms 37 in the BIB

Psalms 37 in the BLPT

Psalms 37 in the BNT

Psalms 37 in the BNTABOOT

Psalms 37 in the BNTLV

Psalms 37 in the BOATCB

Psalms 37 in the BOATCB2

Psalms 37 in the BOBCV

Psalms 37 in the BOCNT

Psalms 37 in the BOECS

Psalms 37 in the BOHCB

Psalms 37 in the BOHCV

Psalms 37 in the BOHLNT

Psalms 37 in the BOHNTLTAL

Psalms 37 in the BOICB

Psalms 37 in the BOILNTAP

Psalms 37 in the BOITCV

Psalms 37 in the BOKCV

Psalms 37 in the BOKCV2

Psalms 37 in the BOKHWOG

Psalms 37 in the BOKSSV

Psalms 37 in the BOLCB

Psalms 37 in the BOLCB2

Psalms 37 in the BOMCV

Psalms 37 in the BONAV

Psalms 37 in the BONCB

Psalms 37 in the BONLT

Psalms 37 in the BONUT2

Psalms 37 in the BOPLNT

Psalms 37 in the BOSCB

Psalms 37 in the BOSNC

Psalms 37 in the BOTLNT

Psalms 37 in the BOVCB

Psalms 37 in the BOYCB

Psalms 37 in the BPBB

Psalms 37 in the BPH

Psalms 37 in the BSB

Psalms 37 in the CCB

Psalms 37 in the CUV

Psalms 37 in the CUVS

Psalms 37 in the DBT

Psalms 37 in the DGDNT

Psalms 37 in the DHNT

Psalms 37 in the DNT

Psalms 37 in the ELBE

Psalms 37 in the EMTV

Psalms 37 in the ESV

Psalms 37 in the FBV

Psalms 37 in the FEB

Psalms 37 in the GGMNT

Psalms 37 in the GNT

Psalms 37 in the HARY

Psalms 37 in the HNT

Psalms 37 in the IRVA

Psalms 37 in the IRVB

Psalms 37 in the IRVG

Psalms 37 in the IRVH

Psalms 37 in the IRVK

Psalms 37 in the IRVM

Psalms 37 in the IRVM2

Psalms 37 in the IRVO

Psalms 37 in the IRVP

Psalms 37 in the IRVT

Psalms 37 in the IRVT2

Psalms 37 in the IRVU

Psalms 37 in the ISVN

Psalms 37 in the JSNT

Psalms 37 in the KAPI

Psalms 37 in the KBT1ETNIK

Psalms 37 in the KBV

Psalms 37 in the KJV

Psalms 37 in the KNFD

Psalms 37 in the LBA

Psalms 37 in the LBLA

Psalms 37 in the LNT

Psalms 37 in the LSV

Psalms 37 in the MAAL

Psalms 37 in the MBV

Psalms 37 in the MBV2

Psalms 37 in the MHNT

Psalms 37 in the MKNFD

Psalms 37 in the MNG

Psalms 37 in the MNT

Psalms 37 in the MNT2

Psalms 37 in the MRS1T

Psalms 37 in the NAA

Psalms 37 in the NASB

Psalms 37 in the NBLA

Psalms 37 in the NBS

Psalms 37 in the NBVTP

Psalms 37 in the NET2

Psalms 37 in the NIV11

Psalms 37 in the NNT

Psalms 37 in the NNT2

Psalms 37 in the NNT3

Psalms 37 in the PDDPT

Psalms 37 in the PFNT

Psalms 37 in the RMNT

Psalms 37 in the SBIAS

Psalms 37 in the SBIBS

Psalms 37 in the SBIBS2

Psalms 37 in the SBICS

Psalms 37 in the SBIDS

Psalms 37 in the SBIGS

Psalms 37 in the SBIHS

Psalms 37 in the SBIIS

Psalms 37 in the SBIIS2

Psalms 37 in the SBIIS3

Psalms 37 in the SBIKS

Psalms 37 in the SBIKS2

Psalms 37 in the SBIMS

Psalms 37 in the SBIOS

Psalms 37 in the SBIPS

Psalms 37 in the SBISS

Psalms 37 in the SBITS

Psalms 37 in the SBITS2

Psalms 37 in the SBITS3

Psalms 37 in the SBITS4

Psalms 37 in the SBIUS

Psalms 37 in the SBIVS

Psalms 37 in the SBT

Psalms 37 in the SBT1E

Psalms 37 in the SCHL

Psalms 37 in the SNT

Psalms 37 in the SUSU

Psalms 37 in the SUSU2

Psalms 37 in the SYNO

Psalms 37 in the TBIAOTANT

Psalms 37 in the TBT1E

Psalms 37 in the TBT1E2

Psalms 37 in the TFTIP

Psalms 37 in the TFTU

Psalms 37 in the TGNTATF3T

Psalms 37 in the THAI

Psalms 37 in the TNFD

Psalms 37 in the TNT

Psalms 37 in the TNTIK

Psalms 37 in the TNTIL

Psalms 37 in the TNTIN

Psalms 37 in the TNTIP

Psalms 37 in the TNTIZ

Psalms 37 in the TOMA

Psalms 37 in the TTENT

Psalms 37 in the UBG

Psalms 37 in the UGV

Psalms 37 in the UGV2

Psalms 37 in the UGV3

Psalms 37 in the VBL

Psalms 37 in the VDCC

Psalms 37 in the YALU

Psalms 37 in the YAPE

Psalms 37 in the YBVTP

Psalms 37 in the ZBP