Song of Songs 5 (BOGWICC)

1 Ndalowa mʼmunda mwanga, iwe mlongo wanga, iwe mkwatibwi wanga;ndasonkhanitsa mure wanga ndi zokometsera zakudya zanga.Ndadya uchi wanga pamodzi ndi zisa zake zomwe;ndamwa vinyo wanga ndi mkaka wanga.Idyani abwenzi anga, imwani;Inu okondana, imwani kwambiri. 2 Ndinagona tulo koma mtima wanga unali maso.Tamverani, bwenzi langa akugogoda:“Nditsekulire, mlongo wanga, bwenzi langa,nkhunda yanga, wangwiro wanga.Mutu wanga wanyowa ndi mame,tsitsi langa lanyowa chifukwa cha nkhungu ya usiku.” 3 Ndavula kale zovala zanga,kodi ndizivalenso?Ndasamba kale mapazi angakodi ndiwadetsenso? 4 Bwenzi langa anapisa dzanja lake pa chibowo cha pa chitseko;mtima wanga unagunda chifukwa cha iye. 5 Ndinanyamuka kukamutsekulira wachikondi wangayo,ndipo manja anga anali noninoni ndi mure,zala zanga zinali mure chuchuchu,pa zogwirira za chotsekera. 6 Ndinamutsekulira wachikondi wanga,koma nʼkuti wachikondi wangayo atachoka; iye anali atapita.Mtima wanga unafumuka chifukwa cha kuchoka kwake.Ndinamuyangʼanayangʼana koma sindinamupeze.Ndinamuyitana koma sanandiyankhe. 7 Alonda anandipezapamene ankayendera mzindawo.Anandimenya ndipo anandipweteka;iwo anandilanda mwinjiro wanga,alonda a pa khoma aja! 8 Inu akazi a ku Yerusalemu ndithu ndikukupemphani,mukapeza wokondedwa wangayo,kodi mudzamuwuza chiyani?Muwuzeni kuti ine ndadwala nacho chikondi. 9 Iwe wokongola kuposa akazi onsewa,kodi wokondedwa wakoyo ndi wopambana wina aliyense bwanji?Kodi wokondedwa wakoyo ndi wopambana ena onse chotanikuti uzichita kutipempha motere? 10 Wokondedwa wangayo ndi wowala kwambiri ndi wathanzipakati pa anthu 1,000. 11 Mutu wake ndi golide woyengeka bwino;tsitsi lake ndi lopotanapotana,ndiponso lakuda bwino ngati khwangwala. 12 Maso ake ali ngati nkhundamʼmbali mwa mitsinje ya madzi,ngati nkhunda zitasamba mu mkaka,zitayima ngati miyala yamtengowapatali. 13 Masaya ake ali ngati timinda ta mbewu zokometsera zakudyazopatsa fungo lokoma.Milomo yake ili ngati maluwa okongolaamene akuchucha mure. 14 Manja ake ali ngati ndodo zagolidezokongoletsedwa ndi miyala yamtengowapatali.Thupi lake ndi losalala ngati mnyanga wanjovuwoyikamo miyala ya safiro. 15 Miyendo yake ili ngati mizati yamwala,yokhazikika pa maziko a golide.Maonekedwe ake ali ngati Lebanoni,abwino kwambiri ngati mkungudza. 16 Milomo yake ndi yosangalatsa kwambiri;munthuyo ndi wokongola kwambiri!Uyu ndiye wachikondi wanga ndi bwenzi langa,inu akazi a ku Yerusalemu.

In Other Versions

Song of Songs 5 in the ANGEFD

Song of Songs 5 in the ANTPNG2D

Song of Songs 5 in the AS21

Song of Songs 5 in the BAGH

Song of Songs 5 in the BBPNG

Song of Songs 5 in the BBT1E

Song of Songs 5 in the BDS

Song of Songs 5 in the BEV

Song of Songs 5 in the BHAD

Song of Songs 5 in the BIB

Song of Songs 5 in the BLPT

Song of Songs 5 in the BNT

Song of Songs 5 in the BNTABOOT

Song of Songs 5 in the BNTLV

Song of Songs 5 in the BOATCB

Song of Songs 5 in the BOATCB2

Song of Songs 5 in the BOBCV

Song of Songs 5 in the BOCNT

Song of Songs 5 in the BOECS

Song of Songs 5 in the BOHCB

Song of Songs 5 in the BOHCV

Song of Songs 5 in the BOHLNT

Song of Songs 5 in the BOHNTLTAL

Song of Songs 5 in the BOICB

Song of Songs 5 in the BOILNTAP

Song of Songs 5 in the BOITCV

Song of Songs 5 in the BOKCV

Song of Songs 5 in the BOKCV2

Song of Songs 5 in the BOKHWOG

Song of Songs 5 in the BOKSSV

Song of Songs 5 in the BOLCB

Song of Songs 5 in the BOLCB2

Song of Songs 5 in the BOMCV

Song of Songs 5 in the BONAV

Song of Songs 5 in the BONCB

Song of Songs 5 in the BONLT

Song of Songs 5 in the BONUT2

Song of Songs 5 in the BOPLNT

Song of Songs 5 in the BOSCB

Song of Songs 5 in the BOSNC

Song of Songs 5 in the BOTLNT

Song of Songs 5 in the BOVCB

Song of Songs 5 in the BOYCB

Song of Songs 5 in the BPBB

Song of Songs 5 in the BPH

Song of Songs 5 in the BSB

Song of Songs 5 in the CCB

Song of Songs 5 in the CUV

Song of Songs 5 in the CUVS

Song of Songs 5 in the DBT

Song of Songs 5 in the DGDNT

Song of Songs 5 in the DHNT

Song of Songs 5 in the DNT

Song of Songs 5 in the ELBE

Song of Songs 5 in the EMTV

Song of Songs 5 in the ESV

Song of Songs 5 in the FBV

Song of Songs 5 in the FEB

Song of Songs 5 in the GGMNT

Song of Songs 5 in the GNT

Song of Songs 5 in the HARY

Song of Songs 5 in the HNT

Song of Songs 5 in the IRVA

Song of Songs 5 in the IRVB

Song of Songs 5 in the IRVG

Song of Songs 5 in the IRVH

Song of Songs 5 in the IRVK

Song of Songs 5 in the IRVM

Song of Songs 5 in the IRVM2

Song of Songs 5 in the IRVO

Song of Songs 5 in the IRVP

Song of Songs 5 in the IRVT

Song of Songs 5 in the IRVT2

Song of Songs 5 in the IRVU

Song of Songs 5 in the ISVN

Song of Songs 5 in the JSNT

Song of Songs 5 in the KAPI

Song of Songs 5 in the KBT1ETNIK

Song of Songs 5 in the KBV

Song of Songs 5 in the KJV

Song of Songs 5 in the KNFD

Song of Songs 5 in the LBA

Song of Songs 5 in the LBLA

Song of Songs 5 in the LNT

Song of Songs 5 in the LSV

Song of Songs 5 in the MAAL

Song of Songs 5 in the MBV

Song of Songs 5 in the MBV2

Song of Songs 5 in the MHNT

Song of Songs 5 in the MKNFD

Song of Songs 5 in the MNG

Song of Songs 5 in the MNT

Song of Songs 5 in the MNT2

Song of Songs 5 in the MRS1T

Song of Songs 5 in the NAA

Song of Songs 5 in the NASB

Song of Songs 5 in the NBLA

Song of Songs 5 in the NBS

Song of Songs 5 in the NBVTP

Song of Songs 5 in the NET2

Song of Songs 5 in the NIV11

Song of Songs 5 in the NNT

Song of Songs 5 in the NNT2

Song of Songs 5 in the NNT3

Song of Songs 5 in the PDDPT

Song of Songs 5 in the PFNT

Song of Songs 5 in the RMNT

Song of Songs 5 in the SBIAS

Song of Songs 5 in the SBIBS

Song of Songs 5 in the SBIBS2

Song of Songs 5 in the SBICS

Song of Songs 5 in the SBIDS

Song of Songs 5 in the SBIGS

Song of Songs 5 in the SBIHS

Song of Songs 5 in the SBIIS

Song of Songs 5 in the SBIIS2

Song of Songs 5 in the SBIIS3

Song of Songs 5 in the SBIKS

Song of Songs 5 in the SBIKS2

Song of Songs 5 in the SBIMS

Song of Songs 5 in the SBIOS

Song of Songs 5 in the SBIPS

Song of Songs 5 in the SBISS

Song of Songs 5 in the SBITS

Song of Songs 5 in the SBITS2

Song of Songs 5 in the SBITS3

Song of Songs 5 in the SBITS4

Song of Songs 5 in the SBIUS

Song of Songs 5 in the SBIVS

Song of Songs 5 in the SBT

Song of Songs 5 in the SBT1E

Song of Songs 5 in the SCHL

Song of Songs 5 in the SNT

Song of Songs 5 in the SUSU

Song of Songs 5 in the SUSU2

Song of Songs 5 in the SYNO

Song of Songs 5 in the TBIAOTANT

Song of Songs 5 in the TBT1E

Song of Songs 5 in the TBT1E2

Song of Songs 5 in the TFTIP

Song of Songs 5 in the TFTU

Song of Songs 5 in the TGNTATF3T

Song of Songs 5 in the THAI

Song of Songs 5 in the TNFD

Song of Songs 5 in the TNT

Song of Songs 5 in the TNTIK

Song of Songs 5 in the TNTIL

Song of Songs 5 in the TNTIN

Song of Songs 5 in the TNTIP

Song of Songs 5 in the TNTIZ

Song of Songs 5 in the TOMA

Song of Songs 5 in the TTENT

Song of Songs 5 in the UBG

Song of Songs 5 in the UGV

Song of Songs 5 in the UGV2

Song of Songs 5 in the UGV3

Song of Songs 5 in the VBL

Song of Songs 5 in the VDCC

Song of Songs 5 in the YALU

Song of Songs 5 in the YAPE

Song of Songs 5 in the YBVTP

Song of Songs 5 in the ZBP